< Yesaya 28 >

1 Tsoka ufumu wonyada wa zidakwa za ku Efereimu. Tsoka kwa ulemerero wake wokongola umene ukufota ngati duwa limene lili pa mutu pa anthu oledzera a mʼchigwa chachonde.
Mano kaka unune malit un osimbo mar jomer man Efraim, maber mare malich biro rumo ka maua maner, mopidhi ei holo momiyo mana kaka josunga malwokore gi kongʼo!
2 Taonani, ambuye ali naye wina wamphamvu ndi nyonga. Iye adzabwera ngati mkuntho wamatalala ndi namondwe wowononga, ngati madzi amphamvu osefukira a mvula yamkuntho; ndipo adzawagwetsa pansi mwankhanza.
Ne, Ruoth Nyasaye nigi ngʼato man kod loch gi teko. Mana kaka pe kod yamo maketho piny, e kaka obiro kelo koth machwe mabubni giteko matiek gik moko duto manie lowo.
3 Ulamuliro wa atsogoleri oledzera a ku Efereimu adzawuthetsa.
Osimbo ma jomer man Efraim sungorego ibiro nyono gi tielo.
4 Ndipo ulemerero wokongola wa mzinda umene uli ngati duwa lofota pamutu pa anthu oledzera a mʼchigwa chachonde uja, udzakhala ngati nkhuyu yoyambirira kupsa imene munthu akangoyiona amayithyola nthawi yokolola isanakwane.
Berne malich norum mana ka maua maner, mopidhi ei holo momiyo, mi nochal ka olemb ngʼowu mokwongo chiek, ngʼato angʼata monene pone, kendo chame ka rikni morum chuth.
5 Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonse adzakhala ngati nkhata yaufumu, chipewa chokongola kwa anthu ake otsala.
E kindeno Jehova Nyasaye Maratego nobedi kaka osimbo mar duongʼ maber ne joge manok modongʼ.
6 Iye adzapereka mtima wachilungamo kwa oweruza, adzakhala chilimbikitso kwa amene amabweza adani pa zipata za mzinda.
Enobed e chuny jangʼad bura mowinjore kendo enojiw jolwenjeu makedo, e dhorangeyeu obed gichir kendo olochi.
7 Nawonso awa ali dzandidzandi chifukwa cha vinyo ndipo akusochera chifukwa cha mowa: ansembe ndi aneneri akudzandira chifukwa cha mowa ndipo akusokonezeka chifukwa cha vinyo; akusochera chifukwa cha mowa, akudzandira pamene akuona masomphenya, kupunthwa pamene akupereka chigamulo.
To jogi bende kwangʼ nikech divai kendo gibayo nikech kongʼo: Jodolo kod jonabi mer makwangʼ nikech kongʼo kendo gitagore nikech divai, githembo ka gineno fweny, gichwanyore ka gingʼado bura.
8 Pa matebulo onse pali masanzi okhaokha ndipo palibenso malo wopanda zonyansa.
Mesa duto opongʼ gi ngʼok, onge kamoro amora ma ok dungʼ tik marach.
9 Iwo akuti, “Kodi munthu ameneyu akufuna aphunzitse ndani? Uthengawu akufuna kufotokozera yani? Ndi kwa ana amene aleka kuyamwa, kwa makanda ongowachotsa kumene ku bere?
“En ngʼa motemo puonjo? To koso en ngʼa ma otemo yarone tiend wachne? Ne nyithindo mogolie chak, koso ne joma koro eka ogolie thuno?
10 Akuyesa kumatiphunzitsa pangʼonopangʼono lemba ndi lemba, mzere ndi mzere, phunziro ndi phunziro. Zonsezi akungoti apa pangʼono apa pangʼono.”
Onyisowa weche mak winjre ka mag jomomer ni: Tim ma, tim macha kendo tim ma, tim macha.”
11 Mulungu adzayankhula kwa anthu ake kudzera mwa anthu aziyankhulo zachilendo, ziyankhulo zosamveka bwino. Mulungu adzayankhula kwa anthu awa, amene
To kata kamano Nyasaye biro wuoyo gi jogi gi dho welo kod dhok mayoreyore.
12 anakuwuzani kuti, “Malo opumulira ndi ano, otopa apumule, malo owusira ndi ano.” Koma inu simunamvere.
Mowachone niya, “Ma en kar yweyo, joma ool mondo oywe.” Kendo niya, “Ma en kar kwe,” to ne ok ginyal winjo.
13 Choncho Yehova adzakuphunzitsani pangʼonopangʼono lemba ndi lemba, mzere ndi mzere, phunziro ndi phunziro. Kotero mudzayenda ndi kugwa chambuyo, adzapweteka ndi kukodwa mu msampha ndipo adzakutengani ku ukapolo.
Kuom mano, wach Jehova Nyasaye biro chalonegi mana ka wach awacha mar joma omer niya: Tim ma, tim macha, kendo tim ma, tim macha, matin ka, matin kacha, mamiyo gikwangʼ koni gi koni mi gipodhi kendo gihinyre ma makgi e obadho.
14 Nʼchifukwa chake imvani mawu a Yehova, inu anthu achipongwe amene mumalamulira anthu awa mu Yerusalemu.
Kuom mano winjuru wach Jehova Nyasaye un joma jaro ji ma, jotend ogandani modak Jerusalem.
15 Inu mumayankhula monyada kuti, “Ife tinachita pangano ndi imfa, ife tachita mgwirizano ndi manda. Pamene mliri woopsa ukadzafika sudzatikhudza ife, chifukwa timadalira bodza ngati pothawirapo pathu ndi chinyengo ngati malo anthu obisalapo.” (Sheol h7585)
Usungoru niya, “Wasetimo singruok gi tho wasedonjo e winjruok gi liete omiyo, ka masira miwachono nolandre e piny to ok nomulwa, nimar waseketo miriambo ragengʼ-wa, kendo wuondruok ka kar pondo.” (Sheol h7585)
16 Tsono zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi: “Taonani, ndikuyika mwala wovomerezeka ndi amisiri ngati maziko mu Ziyoni, mwala wapangodya, wamtengowapatali wopanga maziko amphamvu; munthu amene awukhulupirira sadzagwedezeka.
Ma e gima Jehova Nyasaye Manyalo Gik Moko Duto wacho, “Ne, aketo kidi e Sayun, ma en kidi moyier, en kidi motegno, ma nengone tek, moriwo kor ot kendo man-gi mise mongirore; ma ngʼat moyie kuome ok nobam.
17 Ntchito zolungama zidzakhala ngati chingwe choyezera maziko ake, ndipo chilungamo chidzakhala chowongolera mzere; matalala adzawononga malo anu othawirapo, amene ndi mabodza, ndipo madzi adzamiza malo anu obisalako.
Abiro miyo adiera bedo tol mipimogo kendo tim makare kaka rapim mirieyogo ot; to kodh pe biro yweyo karu mar pondo, un jo-miriambo kendo pi biro pongʼo kuondeu mag tony.
18 Pangano limene munachita ndi imfa lidzathetsedwa; mgwirizano wanu ndi manda udzachotsedwa. Pakuti mliri woopsa udzafika, ndipo udzakugonjetsani. (Sheol h7585)
Singruok maru gi tho nobed maonge; kendo winjruok mane utimo gi liete ok nobedi. Ka masira nomwomre, to mano ema nochwadu piny. (Sheol h7585)
19 Ndipo ukadzangofika udzakutengani. Udzafika mmawa uliwonse, usiku ndi usana.” Anthu akadzamvetsetsa uthenga umenewu adzaopsedwa kwambiri.
E kinde duto ma masira nobi enotieku; noyweu okinyi ka okinyi kendo odiechiengʼ gotieno.” Ka wachni nodonjne ji, to ginibed gi bwok maduongʼ.
20 Mudzakhala ngati munthu wogona pa bedi lalifupi kwambiri kuti sangathe kutambalitsapo miyendo; ndiponso mudzakhala ngati munthu amene wafunda bulangeti lochepa kwambiri kuti sangathe nʼkufunda komwe.
Kitanda nobed machiek ma ok nyal rieye tielo tir, kendo onget nobed matin ma ok nyal umo ngʼato maber.
21 Yehova adzamenya nkhondo monga anachitira ku phiri la Perazimu adzakalipa monga anachitira ku chigwa cha Gibiyoni; adzagwira ntchito yake yooneka ngati yachilendo, ndipo zimene ati adzachite zidzakhala ngati zodabwitsa.
To Jehova Nyasaye biro aa malo mana kaka notimo e Got Perazim, mirimbe nowuogi kaka ne otimore e Holo mar Gibeon, mondo oti tichne, tichne mayoreyore ma ji kia kendo timne mar wich teko.
22 Tsopano lekani kunyoza, mukapanda kutero maunyolo anu adzakuthinani kwambiri; Ambuye, Yehova Wamphamvuzonse wandiwuza kuti, “Ndagamula kuti ndidzawononga dziko lapansi.”
Koro weuru ajara mondo kik tol motweugo ridre, nimar Ruoth Nyasaye ma en Jehova Nyasaye Maratego, osenyisa wach mar kethruok mabiro kwako piny duto.
23 Tcherani khutu ndipo mumve mawu anga; mvetserani ndipo mumve zimene ndikunena.
Chik iti kendo iwinj dwonda, keturu chunyu mondo uwinj weche mawacho.
24 Kodi mlimi wofuna kudzala mbewu amangokhalira kutipula kokhakokha? Kodi amangokhalira kugawula ndi kugalawuza kokhakokha?
Ka japur puro puodho mondo okom to bende osiko ka opuro apura? Koso bende osiko ka obuso abusa?
25 Pamene iye wasalaza mundawo, kodi samafesa mawere ndi chitowe? Kodi suja samadzala tirigu ndi barele mʼmizere yake, nadzala mchewere mʼphepete mwa mundawo?
Kosetieko loso puothe donge ochwoyo kothe mopogore opogore kendo okiro kal? To donge opidho shairi kanyo kod ngano e bath puodho?
26 Mulungu wake amamulangiza ndi kumuphunzitsa njira yabwino.
Nyasache nyise yo monego oluw kendo puonje yo maber.
27 Mawere sapunthira chopunthira cha galeta lopanda mikombero, kapena chitowe sapuntha popondetsapo mikombero ya galeta; mawere amapuntha ndi ndodo ndipo chitowe amapuntha ndi kamtengo.
Cham moko ok din gi twor to bende kal ok wuothie wiye gi gari; moko to idino gi luth kendo kal itengʼo gi kede.
28 Tirigu ayenera kusinjidwa kuti apangire buledi, komabe munthu samangokhalira kupuntha tiriguyo osalekeza, kuopa kuti angatekedzeke. Ngakhale kuti amapuntha tiriguyo poyendetsapo mikombero ya galeta, koma akavalo ake satekedza tiriguyo.
Ngano nyaka regi mondo olos makati; omiyo ok dine amingʼa. Kata obedo ni oywayo gache mar dino kuome, to faresene ok rege.
29 Izinso zimachokera kwa Yehova Wamphamvuzonse, wa uphungu wodabwitsa ndi wa nzeru zopambana.
Magi duto bende oa kuom Jehova Nyasaye Maratego, ma jangʼad rieko mowinjore, kendo ma parone ber ahinya.

< Yesaya 28 >