< Yesaya 21 >
1 Uthenga wonena za chipululu cha mʼmbali mwa Nyanja. Ankhondo a ku Elamu ndi Mediya adzabwera ngati kamvuluvulu amene akuwomba modutsa mʼmbali ya nyanja, kuchokera ku chipululu, dziko lochititsa mantha.
Utsaga om Öknen vid havet. Likasom en storm som far fram i Sydlandet kommer det från öknen, från det fruktansvärda landet.
2 Ine ndaona zinthu zoopsa mʼmasomphenya: Wonyenga akunyenga, wofunkha akufunkha komanso owononga akuwononga. Elamu, yambani nkhondo! Mediya, zingani mzinda! Ine ndidzathetsa mavuto onse amene anayambitsa Ababuloni.
En gruvlig syn har blivit mig kungjord: »Härjare härja, rövare röva. Drag upp, du Elam! Träng på, du Mediens folk! På all suckan vill jag göra slut.»
3 Chifukwa cha zimenezi thupi langa likunjenjemera ndi mantha, ndikumva ululu ngati wa mayi amene akubereka; ndikuvutika kwambiri ndi zimene ndikumva, ndathedwa nzeru ndi zimene ndikuziona.
Fördenskull darra nu mina länder, ångest griper mig, lik en barnaföderskas ångest; förvirring kommer över mig, så att jag icke kan höra, förskräckelse fattar mig, så att jag icke kan se.
4 Mtima wanga ukugunda, ndipo ndikunjenjemera ndi mantha; chisisira chimene ndakhala ndikuchifuna chasanduka chinthu choopsa kwa ine.
Mitt hjärta är utom sig, jag kväljes av förfäran; skymningen, som jag längtade efter, vållar mig nu skräck.
5 Ankhondo a ku Elamu ndi Mediya akukonza matebulo, akuyala mphasa, akudya komanso kumwa! Mwadzidzidzi anamva mawu akuti, “Dzukani inu ankhondo, pakani mafuta zishango zanu!”
Man dukar bord, man breder ut täcken, man äter och dricker. Nej, stån upp, I furstar; smörjen edra sköldar!
6 Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi; “Pita, kayike mlonda kuti azinena zimene akuziona.
Ty så har Herren sagt till mig: »Gå och ställ ut en väktare; vad han får se, det må han förkunna.
7 Taonani, anthu akubwera ali pa akavalo ndipo akuyenda awiriawiri, okwera pa bulu kapena okwera pa ngamira, mlondayo akhale tcheru kwambiri.”
Och om han ser ett tåg, ryttare par efter par, ett tåg av åsnor, ett tåg av kameler, då må han giva akt, noga giva akt.»
8 Ndipo mlondayo anafuwula kuti, “Ambuye anga, tsiku ndi tsiku ndimakhala pa nsanja yolondera; Usiku uliwonse ndimakhala pa malo anga olondera.
Och denne ropade, såsom ett lejon ryter: »Herre, här står jag på vakt beständigt, dagen igenom, och jag förbliver här på min post natt efter natt.
9 Taonani, uyo munthu akubwera atakwera pa galeta ali ndi gulu la akavalo. Mmodzi wa iwo akuti, ‘Babuloni wagwa, wagwa! Mafano onse a milungu yake agwa pansi ndipo aphwanyika!’”
Och se, nu kommer här ett tåg av män, ryttare par efter par!» Och åter talade han och sade: »Fallet, fallet är Babel! Alla dess gudabeläten äro nedbrutna till jorden.»
10 Inu anthu anga opunthidwa ndi kupetedwa ngati tirigu, ine ndikukuwuzani zimene ndamva ndikukuwuzani Uthenga wochokera kwa Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli.
O du mitt krossade, mitt söndertröskade folk, vad jag har hört av HERREN Sebaot, Israels Gud, det har jag förkunnat för eder.
11 Uthenga wonena za Duma: Munthu wina akundiyitana kuchokera ku Seiri kuti, “Iwe mlonda, usikuwu utha liti? Iwe mlonda, utha liti kodi usikuwu?”
Utsaga om Duma. Man ropar till mig från Seir: »Väktare, vad lider natten? Väktare, vad lider natten?»
12 Mlonda akuyankha kuti, “Kukucha, koma kudanso. Ngati ukufuna kufunsa, funsa tsopano; ndipo ubwerenso udzafunse.”
Väktaren svarar: »Morgon har kommit, och likväl är det natt. Viljen I fråga mer, så frågen; kommen tillbaka igen.»
13 Uthenga wonena za Arabiya: Inu anthu amalonda a ku Dedani, amene usiku mumagona mʼzithukuluzi za ku Arabiya,
Utsaga över Arabien. Tagen natthärbärge i Arabiens vildmark, I karavaner från Dedan.
14 perekani madzi kwa anthu aludzu. Inu anthu a ku Tema perekani chakudya kwa anthu othawa nkhondo.
Må man komma emot de törstande och giva dem vatten. Ja, inbyggarna i Temas land gå de flyktande till mötes med bröd.
15 Iwo akuthawa malupanga, lupanga losololedwa, akuthawa uta wokokakoka ndiponso nkhondo yoopsa.
Ty de fly undan svärd, undan draget svärd, och undan spänd båge och undan krigets tunga.
16 Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi: “Chaka chimodzi chisanathe, potsata mmene amawerengera munthu waganyu, ulemerero wonse wa Kedara udzatheratu.
Ty så har Herren sagt till mig: Om ett år, såsom dagakarlen räknar året, skall all Kedars härlighet vara förgången,
17 Mwa anthu okoka uta, ankhondo a ku Kedara opulumuka adzakhala owerengeka.” Wayankhula ndi Yehova Mulungu wa Israeli.
och föga skall då vara kvar av Kedars hjältars bågar, så många de äro. Ty så har HERREN, Israels Gud, talat.