< Yesaya 14 >

1 Yehova adzachitira chifundo Yakobo; adzasankhanso Israeli ndi kuwalola kuti akhalenso mʼdziko lawo. Alendo adzabwera kudzakhala nawo ndi kudziphatika okha kukhala ngati a mʼnyumba ya Yakobo.
Bangkongtetpawiteh, BAWIPA ni Jakop imthung hah a pahren dawkvah, Isarelnaw hah bout a rawi teh, amamae ram dawk ahnimanaw hah a hmuen a poe han. Ramlouknaw ni ahnimouh koe ao awh van han.
2 Anthu a mitundu ina adzaperekeza a Israeli ku dziko lawo. Tsono Aisraeli adzasandutsa anthu a mitundu ina aja kukhala antchito awo aamuna ndi aakazi mʼdziko la Yehova. Ndiye kuti Aisraeli adzasandutsa akapolo anthu amene kale anali ambuye awo. Iwo adzasandutsa akapolo anthu amene kale ankawalamulira ndi kuwazunza.
Miphunnaw ni ahnimouh teh, amamae ram dawk a thokhai awh han. Isarelnaw ni miphunnaw e napui tongpanaw hah san lah a tawn awh han. Ahnimouh ni ahnimouh kamankungnaw hah a man awh han. Ahnimouh ka rektap e naw hai a uk awh han.
3 Yehova akadzakupumitsani ku zowawa ndi mavuto, ndiponso kuntchito yakalavulagaga imene ankakugwiritsani,
BAWIPA ni nange patawnae, temdengnae, ka ru e thaw na tawk saknae koehoi nang hlout sak nahan lah BAWIPA e hnin teh a tho han.
4 mudzayankhula monyogodola mfumu ya Babuloni kuti, Wopsinja uja watha! Ukali wake uja watha!
Hattoteh, nangmouh ni Babilon siangpahrang hanelah hettelah bangnuenae na dei awh han, talai ka rektap e teh hete tami nahoehmaw, a uknaeram teh a rawp bo toung vaw.
5 Yehova wathyola chikwapu cha anthu oyipa, Iye waphwanya ndodo ya olamulira.
BAWIPA teh tamikathoutnaw e sonron, ukkungnaw e tahroe hah a khoe pouh.
6 Mfumu ya ku Babuloni inkakantha mitundu ya anthu mwaukali powamenya kosalekeza, Iyo inkagonjetsa anthu a mitundu ina mwaukali ndikuwazunza kosalekeza.
Hote ni pout laipalah hemnae hoiyah taminaw hah lungkhueknae hoi a hem. Pahrennae awm laipalah, rektap teh lungkhueknae miphunnaw hah a uk
7 Koma tsopano mayiko onse ali pa mpumulo ndi pa mtendere; ndipo akuyimba mokondwa.
Talaivan pueng teh duem a kâhat teh, la sak lawk ni a katin.
8 Ngakhale mitengo ya payini ndi mikungudza ya ku Lebanoni ikuyimba za iwe mokondwa ndipo ikuti, “Chigwetsedwere chako pansi, palibe wina anabwera kudzatigwetsa.”
Hmaica thingnaw ni nang koe a lunghawi awh. Lebanon mon kaawm e sidar thingnaw ni, nang na rawp hnukkhu, kaimouh na ka tâtueng hane luen takhang hoeh toe ati awh.
9 Ku manda kwatekeseka kuti akulandire ukamabwera; mizimu ya anthu akufa, aja amene anali atsogoleri a dziko lapansi, yadzutsidwa. Onse amene anali mafumu a mitundu ya anthu ayimiritsidwa pa mipando yawo. (Sheol h7585)
Nang na tho toteh dawn hanelah, tami kadout kho teh a kâcai. Talai ukkungnaw pueng a hroecoe teh, ram tangkuem e siangpahrangnaw pueng hai amamae bawitungkhung dawk hoi a thaw sak. (Sheol h7585)
10 Onse adzayankha; adzanena kwa iwe kuti, “Iwenso watheratu mphamvu ngati ife; Iwe wafanana ndi ife.”
Ahnimouh pueng ni na pathungnae lah a dei awh e teh, nang hai kaimouh patetlah na tha a youn teh, kaimouh hoi rei na kâvan bo vaw
11 Ulemerero wako wonse walowa mʼmanda, pamodzi ndi nyimbo za azeze ako; mphutsi zayalana pogona pako ndipo chofunda chako ndi nyongolotsi. (Sheol h7585)
Nange raim onae, nange ratoung lawk teh tami kadout kho a cei awh toe. Pârinaw teh na yan nahanelah ao teh, ahrinaw teh na kâkhu e lah ao. (Sheol h7585)
12 Wagwa pansi bwanji kuchoka kumwamba, iwe nthanda, mwana wa mʼbandakucha! Wagwetsedwa pansi pa dziko lapansi, Iwe amene unagonjetsapo mitundu ya anthu!
Oe Khosei capa (Lucifer), amom tempalo, kalvan hoi na bo toe. Ram pueng na kata e, nang teh talai dawk rek na taben toe khe.
13 Mu mtima mwako unkanena kuti, “Ndidzakwera mpaka kumwamba; ndidzakhazika mpando wanga waufumu pamwamba pa nyenyezi za Mulungu; ndidzakhala pa mpando waufumu pa phiri losonkhanirako, pamwamba penipeni pa phiri la kumpoto.
Nama ni teh na lungthung hoi hettelah na dei. Kalvan vah ka luen han. Cathut e âsinaw lathueng vah, ka tahungnae bawitungkhung ka rasang sak han. Atunglah kaawm e kamkhuengnae mon dawk ka tahung han.
14 Ndidzakwera pamwamba pa mitambo; ndidzafanana ndi Wammwambamwamba.”
Tâmainaw e lathueng ka luen han. Lathueng Poung e Cathut patetlah ka kâsak han.
15 Koma watsitsidwa mʼmanda pansi penipeni pa dzenje. (Sheol h7585)
Hatei, nang teh tami kadout kho, kadung poung e tangkom thung na bo toe. (Sheol h7585)
16 Anthu akufa adzakupenyetsetsa nadzamalingalira za iwe nʼkumati, “Kodi uyu ndi munthu uja anagwedeza dziko lapansi ndi kunjenjemeretsa maufumu,
Nang na kahmawt e naw ni nang hah na khet awh teh, talai kâhuen sak e tami, ram pueng kâhuen sak e tami,
17 munthu amene anasandutsa dziko lonse chipululu, amene anagwetsa mizinda yake ndipo sankalola kuti anthu ogwidwa abwerere kwawo?”
talaivan heh kahrawngum patetlah ka coung sak niteh, khopuinaw hah ka raphoe e, a man e naw hah ama im bout ban sak hanelah kâ ka poe hoeh e teh hete tami han namaw, na ti pouh awh han.
18 Mafumu onse a mitundu ya anthu akugona mwaulemu aliyense mʼmanda akeake.
Ram tangkuem e siangpahrangnaw pueng teh, amamae tangkom dawk bawilennae hoi a yan awh.
19 Koma iwe watayidwa kunja kwa manda ako, ngati nthambi yowola ndi yonyansa. Mtembo wako waphimbidwa ndi anthu ophedwa; amene anabayidwa ndi lupanga, anatsikira mʼdzenje lamiyala ngati mtembo woponderezedwa.
Hatei, nang teh panuettho e thingkang patetlah na tangkom dawk hoi takhoe lah na o toe. Thei lah kaawm e, tahloi hoi thut lah kaawm e, talung tangkom thung ka cet e naw hoi ramuk lah na o teh, khok hoi coungroe e ro patetlah doeh na o toe.
20 Sudzayikidwa nawo mʼmanda mwaulemu, chifukwa unawononga dziko lako ndi kupha anthu ako. Zidzukulu za anthu oyipa sizidzakumbukika nʼpangʼono pomwe.
Nang teh ahnimouh hoi rei pakawp mahoeh. Bangkongtetpawiteh, nang teh, nama e ram hah na raphoe teh, na taminaw hah na thei toe. Hawihoehnae ka sak e a catounnaw teh nâtuek hai a min bout dei mahoeh toe.
21 Konzani malo woti muphere ana ake aamuna chifukwa cha machimo a makolo awo; kuti angadzuke ndi kulanda dziko lapansi ndi kulidzaza dziko lonselo ndi mizinda yawo.
Ahnimae a canaw teh, amamae napanaw e yon kecu dawkvah, thei nahane hmuen hah rakueng awh. Ahnimouh thung hoi apihai talai ukkung awm mahoeh toe. Talaivan kho hai kangdout sak awh mahoeh toe.
22 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndidzathira nkhondo mzinda wa Babuloni. Ndidzachotseratu mu Babuloni dzina lake ndi onse otsaliramo. Ndiye kuti sipadzakhala ana kapena zidzukulu,” akutero Yehova.
Rasahu BAWIPA ni, ahnimouh hoi kâtaran lah ka o han. Babilon kho dawk hoi ahnie min hoi kacawie naw thoseh, a ca catounnaw hai thoseh ka raphoe han telah ati.
23 “Ndidzawusandutsa mzindawo malo okhalamo anungu ndiponso dambo lamatope; ndidzawusesa ndi tsache lowononga,” akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Babilon kho teh sambuem lah ka o sak vaiteh, bukbu onae lah ka ta han. Raphoenae sampho hoi ka pâthoun han telah ransahu BAWIPA ni a pathang.
24 Yehova Wamphamvuzonse walumbira kuti, “Ndithudi, monga ndaganizira ndidzachitadi choncho, ndipo monga momwe ndatsimikizira zidzakhala momwemo ndithu.
Rasahu BAWIPA ni, ka pouk e patetlah ao han. Ka noe e patetlah ka sak han.
25 Ndidzawawononga Asiriya mʼdziko langa; ndidzawapondereza ndi mapazi pa mapiri anga; ndidzachotsa goli lawo pa anthu anga, ndipo ndidzachotsa katundu wawo pa mapewa awo.”
Assirianaw hah ka ram dawk rek ka hem vaiteh, kama e monnaw dawkvah, rep ka coungroe han. Ahnie yawcu hah ka takhoe pouh vaiteh, a hno hah a loung dawk hoi ka takhoe pouh han telah thoe a kâbo teh a dei.
26 Izi ndizo ndakonza kuti zichitike pa dziko lonse lapansi, ndatambasula dzanja pa anthu a mitundu yonse.
Hethateh, talai van puenghoi kâkuen e ka noenae doeh. Hathateh, ram pueng koe ka dâw e kut doeh
27 Pakuti Yehova Wamphamvuzonse watsimikiza, ndipo ndani angamuletse? Dzanja lake latambasulidwa ndipo ndani angalibweze?
Bangkongtetpawiteh, ransahu BAWIPA ni a noe toe. Apinimouh a oun thai han. BAWIPA e kut teh a dâw toe. Apinimouh a hno sak thai han.
28 Uthenga uwu unabwera chaka chimene mfumu Ahazi anamwalira:
Ahaz siangpahrang a duenae kum dawk hete lawk teh a tho.
29 Musakondwere inu Afilisti nonse kuti Asiriya amene anali ngati ndodo yokukanthani anathedwa; chifukwa kuchokera ku njoka yomweyi (mfumu ya Aasiriya) mudzatuluka mphiri, ndipo chipatso chake chidzakhala njoka yaliwiro ndiponso yaululu.
Filistin khocanaw, nangmouh na hemnae bongpai a lawt dawk na lunghawi awh hanh. Bangkongtetpawiteh, tahrun phun dawk hoi hrunthoe a khe awh han. Hote a canaw hai kamleng thai e hmaitahrun lah ao awh han.
30 Osaukitsitsa adzapeza chakudya ndipo amphawi adzakhala mwamtendere. Koma anthu ako ndidzawawononga ndi njala, ndipo njalayo idzapha ngakhale opulumuka ako.
Mathoenaw e caminnaw hai kawkhik lah ao han. Mathoemaranaw hai kahawicalah a i awh han. Hatei, nange tangpha teh takang hoi ka thei han. Kacawie naw hai thei lah ao han.
31 Lirani kwambiri, anthu a pa chipata! Fuwulani kwambiri, anthu a mu mzinda! Njenjemerani ndi mantha, inu Afilisti nonse! Mtambo wa utsi ukuchokera kumpoto, ndipo palibe wamantha pakati pa ankhondo ake.
Oe kho longkha, cingou haw. Oe khopui, khuikap haw. Filistinnaw pueng teh taki hoi a pâyaw awh. Bangkongtetpawiteh, atunglah hoi hmaikhu a tâco. Hote ransahu dawkvah, kampek e awm hoeh.
32 Kodi tidzawayankha chiyani amithenga a ku Filisitiya? “Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo mu mzinda wakewu, anthu ozunzika apeza populumukira.”
Ahnimouh ni, ram tangkuem e patounenaw koe bangtelamaw a dei pouh han vai. BAWIPA ni Zion kho hah a kangdue sak teh, mathoenaw ni hote kho dawk a kângue awh han.

< Yesaya 14 >