< Yesaya 13 >

1 Uthenga onena za Babuloni umene Yesaya mwana wa Amozi anawulandira:
Obubaka bwa Babulooni Isaaya mutabani wa Amozi bwe yalaba.
2 Kwezani mbendera yankhondo pa phiri loti see, muwafuwulire ankhondo; muwakodole kuti adzalowe pa zipata za anthu olemekezeka.
Muwanike bbendera ku lusozi olutaliiko bantu, mubakaabirire mubawenye bayingire mu miryango gy’abakungu.
3 Ine Yehova, ndalamulira ankhondo anga; ndasonkhanitsa ankhondo anga kuti akhale zida zanga zolangira amene amadzikuza ndi chipambano changa.
Nze Mukama ndagidde abatukuvu bange mpise abalwanyi bange ab’amaanyi, babonereze abo abeeyisaawo abeemanyi.
4 Tamvani phokoso ku mapiri, likumveka ngati phokoso la gulu lalikulu la anthu! Tamvani phokoso pakati pa maufumu, ngati kuti mitundu ya anthu ikusonkhana pamodzi! Yehova Wamphamvuzonse akukhazika asilikali ake mokonzekera kuchita nkhondo.
Muwulirize oluyoogaano lw’ekibiina ku nsozi, nga luwulikika ng’olw’ogubiina ogunene! Wuliriza, oluyoogaano lw’obwakabaka, olw’amawanga ag’ekuŋŋaanyizza awamu! Mukama Katonda ow’Eggye ateekateeka eggye lye okulwana.
5 Iwo akuchokera ku mayiko akutali, kuchokera kumalekezero a dziko Yehova ali ndi zida zake za nkhondo kuti adzawononge dziko la Babuloni.
Bava wala mu nsi ezeewala ennya okuva ku nkomerero y’eggulu. Mu busungu bwe Mukama Katonda aleese ebyokulwanyisa eby’okuzikiriza ensi yonna.
6 Lirani mofuwula, pakuti tsiku la Yehova layandikira; lidzabwera ngati chiwonongeko chochokera kwa Wamphamvuzonse.
Mukungubage, kubanga olunaku lwa Mukama luli kumpi, lulijja ng’okuzikirira okuva eri Mukama Katonda bwe kuba!
7 Zimenezi zinafowoketsa manja onse, mtima wa munthu aliyense udzachokamo.
Emikono gyonna kyegiriva giggwaamu amaanyi, na buli mutima gwa muntu gulisaanuuka;
8 Anthu adzagwidwa ndi mantha aakulu, zowawa ndi masautso zidzawagwera; adzamva zowawa zonga amamva mayi pobereka. Adzayangʼanana mwamantha, nkhope zawo zikufiira ngati malawi amoto.
era bakeŋŋentererwe n’okubalagala kulibakwata, balyoke balumwe ng’omukazi alumwa okuzaala. Balitunulaganako nga bawuniikiridde amaaso gaabwe nga gatangaalirira.
9 Taonani, tsiku la Yehova likubwera, tsiku lopanda chisoni, lawukali ndi lamkwiyo; kudzasandutsa dziko kuti likhale chipululu ndi kuwononga anthu ochimwa a mʼmenemo.
Laba olunaku lwa Mukama lujja, olunaku olubi ennyo olw’ekiruyi n’obusungu obubuubuuka okufuula ensi amatongo, n’okuzikiriza abakozi b’ebibi okubamalamu.
10 Nyenyezi zakumwamba ndiponso zonse zamlengalenga sizidzaonetsa kuwala kwawo. Dzuwa lidzada potuluka, ndipo mwezi sudzawala konse.
Kubanga emmunyeenye ez’omu ggulu n’ebibiina byazo tebiryaka; enjuba nayo teryaka nga bw’ekola bulijjo, n’omwezi nagwo tegulyaka.
11 Ndidzalanga dziko lonse chifukwa cha zolakwa zake, anthu oyipa ndidzawalanga chifukwa cha machimo awo. Ndidzathetsa kunyada kwa odzikuza, ndipo ndidzatsitsa kudzitukumula kwa anthu ankhanza.
Ndibonereza ensi olw’okwonoona kw’ayo, n’abakozi b’ebibi olw’ebyonoono byabwe. Era ndimalawo okweyisa kw’ab’amalala era nzikakkanya okwenyumiriza kw’abo abakambwe.
12 Ndidzasandutsa anthu kukhala ovuta kupeza kuposa mmene amasowera golide wabwino. Iwo sazidzapezekapezeka kuposa mmene amasowera golide wa ku Ofiri.
Abantu ndibafuula abebbula okusinga zaabu ennongoose eya ofiri.
13 Tsono ndidzagwedeza miyamba ndipo dziko lapansi lidzachoka pa maziko ake. Izi zidzachitika chifukwa cha ukali wa Wamphamvuzonse pa tsiku la mkwiyo wake woopsa.
Noolwekyo ndikankanya eggulu, era n’ensi ngiyuuguumye okuva mu kifo kyayo, olw’obusungu bwa Mukama Katonda ow’Eggye, ku lunaku lw’obusungu bwe obungi.
14 Ngati mbawala zosakidwa, ngati nkhosa zopanda wozikusa, munthu aliyense adzabwerera kwa anthu akwawo, aliyense adzathawira ku dziko lake.
Era ng’empeewo eyiggibwa, ng’endiga eteriiko agirunda, buli muntu aliddukira eri abantu be buli muntu aliddukira mu nsi y’ewaabwe.
15 Aliyense amene atadzapezeke ndi kugwidwa adzaphedwa momubaya ndi lupanga.
Buli anaalabwangako ng’ekitala kimuyitamu, buli gwe banaakwatangako ng’attibwa n’ekitala.
16 Ana awo akhanda adzaphwanyidwa iwo akuona; nyumba zawo zidzafunkhidwa ndipo akazi awo adzagwiriridwa.
N’abaana baabwe abawere banabetenterwanga mu maaso gaabwe nga balaba; ennyumba zaabwe zinyagibwe, n’abakazi baabwe bakwatibwe olw’empaka.
17 Taona, Ine ndidzadzutsa Amedi amene safuna siliva ndipo sasangalatsidwa ndi golide, kuti amenyane ndi Ababuloni.
Laba, ndibayimbulira Abameedi, abatafa ku ffeeza era abateeguya zaabu.
18 Adzapha anyamata ndi mauta awo; sadzachitira chifundo ana ngakhale kumvera chisoni ana akhanda.
Emitego gyabwe girikuba abavubuka era tebaliba na kisa eri abawere. Amaaso gaabwe tegalisaasira baana bato.
19 Babuloni, ufumu wake ndi waulemerero kuposa mafumu onse. Anthu ake amawunyadira. Koma Yehova adzawuwononga ngati mmene anawonongera Sodomu ndi Gomora.
Ne Babulooni, ekitiibwa eky’obwakabaka, obulungi obw’okwemanya kw’Abakaludaaya, kiriba nga Sodomu ne Ggomola Katonda bye yawamba.
20 Anthu sadzakhalamonso kapena kukhazikikamo pa mibado yonse; palibe Mwarabu amene adzayimike tenti yake, palibe mʼbusa amene adzawetamo ziweto zake.
Tekiriddamu kusulwamu ennaku zonna, so tekiribeerwamu emirembe n’emirembe, so teri Muwalabu alisimbayo weema ye, teri musumba aligalamizaayo ggana lye kuwummulirayo.
21 Koma nyama zakuthengo ndizo zidzakhale kumeneko, nyumba zake zidzadzaza ndi nkhandwe; mu mzindamo muzidzakhala akadzidzi, ndipo atonde akuthengo azidzalumphalumphamo.
Naye ensolo enkambwe ez’omu ddungu ze zinaagalamirangayo; ennyumba zijjule ebintu ebiwoowoola; bammaaya banaabeeranga eyo, n’ebikulekule bibuukire eyo.
22 Mu nsanja zake muzidzalira afisi, mʼnyumba zake zokongola muzidzalira nkhandwe. Nthawi yake yayandikira ndipo masiku ake ali pafupi kutha.
N’empisi zinaakaabiranga mu bigulumu by’ebigo byabwe, ebibe bikaabire mu mbiri zaabwe ezitemagana. Ekiseera kyakyo kinaatera okutuuka, ennaku ze teziryongerwako.

< Yesaya 13 >