< Yesaya 12 >

1 Tsiku limenelo aliyense wa inu adzati: “Ndikukuyamikani, Inu Yehova; chifukwa ngakhale munandipsera mtima, mkwiyo wanu wachoka, ndipo mwanditonthoza.
Nianang adlawa moingon kamo, “Pasalamatan ko ikaw, Yahweh. Kay bisan nasuko ka kanako, nawala ang imong kapungot, ug gihupay mo ako.
2 Zoonadi, Mulungu ndiye Mpulumutsi wanga; ndidzamudalira ndipo sindidzachita mantha. Yehova ndiye mphamvu yanga ndi nyimbo yanga; Iye wakhala chipulumutso changa.”
Tan-awa, ang Dios maoy akong kaluwasan; mosalig ako ug dili mahadlok, kay si Yahweh, oo, si Yahweh ang akong kusog ug awit. Siya ang nahimo nakong kaluwasan.”
3 Mudzakondwera popeza Yehova ali ngati chitsime cha chipulumutso chanu.
Inubanan sa kalipay magsag-ob kamo ug tubig gikan sa mga atabay sa kaluwasan.
4 Tsiku limenelo mudzati: “Yamikani Yehova, tamandani dzina lake; mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu, ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.
Moingon kamo nianang adlawa, “Pasalamati si Yahweh ug sangpita ang iyang ngalan; ipahayag ang iyang mga buhat ngadto sa katawhan, imantala nga gipasidunggan ang iyang ngalan.
5 Imbirani Yehova, pakuti wachita ntchito zazikulu; zimenezi zidziwike pa dziko lonse lapansi.
Awiti si Yahweh, kay naghimo siya ug mahimayaong mga butang; ipahibalo kini ngadto sa tibuok kalibotan.
6 Fuwulani ndi kuyimba mwachimwemwe, inu anthu a ku Ziyoni; pakuti Woyerayo wa Israeli ndi wamkulu pakati panu.”
Paghugyaw ug singgit alang sa kalipay, kamong lumolupyo sa Zion, kay bantogan ang Usa ka Balaan sa Israel nga anaa sa inyong taliwala.”

< Yesaya 12 >