< Hoseya 6 >

1 “Bwerani, tiyeni tibwerere kwa Yehova. Iye watikhadzula, koma adzatichiritsa. Iye wativulaza, koma adzamanga mabala athu.
Дойдете, да се върнем при Господа; Защото той разкъсна, и той ще ни изцели, Порази, и ще превърже раната ни.
2 Pakapita masiku awiri adzatitsitsimutsa; pa tsiku lachitatu Iye adzatiukitsa kuti tikhale ndi moyo pamaso pake.
Подир два деня ще ни съживи, На третия ден ще ни въздигне; И ще живеем пред него.
3 Tiyeni timudziwe Yehova, tiyeni tilimbike kumudziwa Iye. Adzabwera kwa ife mosakayikira konse ngati kutuluka kwa dzuwa; adzabwera kwa ife ngati mvula ya mʼchilimwe, ngati mvula ya nthawi yamphukira imene imakhathamiritsa nthaka.”
Да! нека познаем Господа, нека следваме да го познаваме; Той ще се появи сигурно, както зората, И ще дойде при нас, както дъжда, Както пролетният дъжд, който пои земята.
4 Iwe Efereimu, kodi ndichite nawe chiyani? Kodi ndichite nawe chiyani, iwe Yuda? Chikondi chanu chili ngati nkhungu yammawa, ngati mame a mmamawa amene amakamuka msanga.
Що да ти сторя Ефреме? Що да ти сторя, Юдо? Защото добротата ви е като утринния облак, И като росата, която рано прехожда.
5 Choncho ndakuwazani ngati nkhuni kudzera mwa aneneri anga, ndakuphani ndi mawu a pakamwa panga; chigamulo changa chinangʼanima ngati mphenzi pa inu.
За това, ги изсякох чрез пророците, Убих ги с думите на устата си; И съдбите ми се явяват като светлината.
6 Pakuti Ine ndimafuna chifundo osati nsembe, ndi kudziwa Mulungu kulekana ndi nsembe zopsereza.
Защото милозливост искам, а не жертва, И познаване Бога, повече от всеизгаряния.
7 Monga Adamu, anthuwa aphwanya pangano langa, iwo sanakhulupirike kwa Ine.
Те, обаче, както Адам, престъпиха завета; Там постъпиха коварно към Мене.
8 Giliyadi ndi mzinda wa anthu ochita zoyipa, okhala ndi zizindikiro za kuphana.
Галаад е град на ония, които струват беззаконие, Опетнен е с кръв.
9 Monga momwe mbala zimadikirira anthu, magulu a ansembe amachitanso motero; iwo amapha anthu pa njira yopita ku Sekemu, kupalamula milandu yochititsa manyazi.
И както разбойнически чети причакват човека, Така дружината свещеници убива по пътя към Сихем; Да! те вършат безчестие.
10 Ndaona chinthu choopsa kwambiri mʼnyumba ya Israeli. Kumeneko Efereimu akuchita zachiwerewere, ndipo Israeli wadzidetsa.
В Израилевия дом видях ужас; Там се намира блудство у Ефрема, И Израил е осквернен.
11 “Kunenanso za iwe Yuda, udzakolola chilango. “Pamene ndiwabwezere anthu anga zinthu zabwino.”
И за тебе, Юдо, се определи жетва, Когато върна людете си от плен.

< Hoseya 6 >