< Hoseya 4 >

1 Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova, chifukwa Yehova ali ndi mlandu ndi inu amene mumakhala mʼdzikoli: “Mʼdziko mwanu mulibe kukhulupirika, mulibe chikondi mulibe kulabadira za Mulungu.
Pakai thusei ngaiyuvin, O Israel mite! Ajeh chu Pakaiyin gamsunga chengte toh kinelna khat aneiye. “Kitahna aumpoi, kikhotona jong aumpoi, nagamsunguva Pathen hetna jong aumpoi.
2 Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha. Kuba ndi kuchita chigololo; machimo achita kunyanya ndipo akungokhalira kuphana.
Kihahselna jeng alengin, jouthu jeng akiseiyin, na kithatun chule naguchauvin, jonthanhoi nabollun, muntin jousea nakisatun, khatle khat nakithat touvin ahi.
3 Chifukwa chake dziko likulira ndipo onse amene amakhalamo akuvutika; zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga ndiponso nsomba zamʼnyanja zikufa.
Hijeh chun nagamsungu hi mihem lunghem bangin alunghemtan, gamsunga cheng miho jong alunggimsoh tauve. Chule mijousen phat namoh mansahuvin, gamlaha gamsaho jeng jong alunghem sohtauvin, chunga leng vachate jengjong alunghem gamtauve. Twilaha nga ho jeng jong, aum gam tapouve.
4 “Koma wina asapeze mnzake chifukwa, wina aliyense asayimbe mlandu mnzake, pakuti anthu ako ali ngati anthu amene amayimba mlandu wansembe.
Koimacha nakhutjungin koh hihin, chule akiheh tojong koima umda jenghen! Ajeh chu keitoh kinelkal, nangjoh nahi, vo thempu.
5 Mumapunthwa usana ndi usiku ndipo aneneri amapunthwa nanu pamodzi. Choncho ndidzawononga amayi anu.
Hijeha chu sunlai changa jong nakipal lhuh ding, jan tengle themgao pa jong nakipal lhuh tha ding ahi.
6 Anthu anga akuwonongeka chifukwa chosadziwa. “Pakuti mwakana kudziwa, Inenso ndidzakukanani monga ansembe anga; chifukwa mwayiwala lamulo la Mulungu wanu, Inenso ndidzayiwala ana anu.
Kamite chu hetna alhahsam jeh'un amang gam tauve.
7 Ansembe ankati akachuluka iwo ankandichimwiranso kwambiri; iwo anasinthanitsa ulemerero wawo ndi chinthu china chonyansa.
Thempu atam chenin, chonse kei douding atame.
8 Amalemererapo pa machimo a anthu anga ndipo amafunitsitsa kuti anthuwo azipitiriza kuchimwa.
Miten chonset thilto ahin pohlut chanin, thempuho athaouve.
9 Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe. Ndidzawalanga onsewo chifukwa cha njira zawo, ndidzawabwezera chifukwa cha machitidwe awo.
Chule thempun bolkhat aneile, mipiten jong abolluve.
10 “Iwo azidzadya koma sadzakhuta; azidzachita zachiwerewere koma sadzachulukana, chifukwa anasiya Yehova kuti adzipereke
Amahon neuvintin, ahijeng vanga gilkel ding ahiuve. Notin panguvin tin hinlah pungthei lou ding ahiuve. Ajeh chu Pakai dalhan notia pang dingin, donlouvin akoitauve.
11 ku zachiwerewere, ku vinyo wakale ndi watsopano, zimene zimachotsa nzeru zomvetsa zinthu
Ju jeng, juthah jeng adonuvin, jun kamite aguhmang ahitai.
12 za anthu anga. Anthu anga amapempha nzeru ku fano lamtengo ndipo ndodo yawo yamtengo imawayankha. Mzimu wachiwerewere umawasocheretsa; iwo sakukhulupirika kwa Mulungu wawo.
Amahon thing khat pou adongun, molkang khattouvin akhonung thu-u aseipeh theiding atahsanun ahi. Milim doihou angaichat chun, angolsah-u ahitai. Amahon noti hi akichepnauvin, pathen dang ajenun ahi.
13 Amapereka nsembe pamwamba pa mapiri ndi kufukiza lubani pa zitunda, pa tsinde pa mtengo wa thundu, mnjale ndi mkundi, pamene pali mthunzi wabwino. Nʼchifukwa chake ana anu aakazi akuchita zachiwerewere ndipo akazi a ana anu akuchita zigololo.
Amahon molsangvumah, kilhainan gan athatuve. Amaho lhangvumah akaltouvun, gimnamtwi ahaluve.
14 “Ine sindidzalanga ana anu aakazi pamene iwo adzachita zachiwerewere, kapena akazi a ana anu pamene adzachita zigololo. Paja inu nomwe amunanu mumayenda ndi akazi achiwerewere, ndipo mumapereka nsembe pamodzi ndi akazi achiwerewere a ku malo opembedzerako. Anthu amene alibe nzeru adzawonongeka ndithu!
Ahinlah ibola kagimbol dingham natia apanu leh ajon thanhoi jeh-a? O hetna lhasam mingol ho! thil hetkhanna nanotthap tauve. Namiten jong amaho bol bang bang abolluvin ahi.
15 “Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli, Yuda asapezeke ndi mlandu wotere. “Usapite ku Giligala. Usapite ku Beti-Aveni. Ndipo usalumbire kuti, ‘Pali Yehova wamoyo!’
Israel, nang notin pangjeng jongle chun, Juda vang themmo chansah loujenin. Gilgal khopia hunglut dan, Beth-aven a jong hung lutdan.
16 Aisraeli ndi nkhutukumve, ngosamva ngati ana angʼombe. Kodi Yehova angathe kuwaweta bwanji ngati ana ankhosa pa msipu wabwino?
Bongla gol louchal bangin Israel hi alou challe. Pakaiyin hamhing gam lentaha kelngoi avah banga, Israelte hi avah jing jeng ding hinam ong?
17 Efereimu waphathana ndi mafano; mulekeni!
Israel hi achangin dalhan, ajeh chu amahi jonthanhoi toh kicheng ahitai.
18 Ngakhale pamene zakumwa zawo zatha, amapitiriza kuchita zachiwerewere; atsogoleri awo amakonda kwambiri njira zawo zochititsa manyazi.
Jukham hon khat chu noti ho toh alumkhomtauve. Aloupi diu sangin ajachat diu adeijouve.
19 Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zawo.
Khoppi huijin alhaving tenin achun chah kheh in Maicham hijat asemthu jouse jeh'a hi kijumso diu ahi.

< Hoseya 4 >