< Hoseya 3 >

1 Yehova anati kwa ine, “Pita kamukondenso mkazi wako, ngakhale ali pa chibwenzi ndi wina ndi kuti ndi wachigololo. Mukonde iyeyo monga momwe Yehova amakondera Aisraeli, ngakhale iwo amapita kukapembedza milungu ina ndi kukonda nsembe za keke zamphesa zowuma.”
Und Jehovah sprach zu mir: Gehe abermals hin, liebe ein Weib, das von einem Genossen geliebt wird und Ehebruch treibt, wie Jehovah die Söhne Israels liebt, sie aber wenden sich anderen Göttern zu und lieben Kuchen von Weinbeeren.
2 Motero ndinamukwatira popereka ndalama khumi ndi zisanu zasiliva, ndiponso mitanga isanu ndi iwiri ya barele.
Und ich erkaufte sie mir um fünfzehn Silberlinge und einen Chomer Gerste und einen Lethech Gerste.
3 Kenaka ndinamuwuza mkaziyo kuti, “Ukhale nane masiku ambiri; usachitenso zachiwerewere kapena chigololo ndi munthu wina, ndipo ine ndidzakhala nawe.”
Und ich sprach zu ihr: Viele Tage sollst du bei mir wohnen; du sollst nicht buhlen und sollst keines Mannes sein, und auch ich will dein sein.
4 Pakuti Aisraeli adzakhala masiku ambiri opanda mfumu kapena kalonga, osapereka nsembe kapena kuyimika miyala yachipembedzo, wopanda efodi kapena fano.
Denn viele Tage werden die Söhne Israels wohnen ohne König, und ohne Obersten, und ohne Opfer, und ohne Denksäule, und ohne Ephod und Theraphim.
5 Pambuyo pake Aisraeli adzabwerera ndi kufunafuna Yehova Mulungu wawo ndi Davide mfumu yawo. Adzabwera kwa Yehova akunjenjemera ndipo adzalandira madalitso mʼmasiku awo otsiriza.
Danach werden die Söhne Israels zurückkehren und suchen Jehovah, ihren Gott, und David, ihren König, und mit Schauern kommen zu Jehovah und zu Seinem Guten, in den letzten der Tage.

< Hoseya 3 >