< Hoseya 2 >
1 “Nena kwa abale ako kuti, ‘Ndinu anthu anga,’ kwa alongo ako kuti ‘Ndinu okondedwa anga.’”
“Amaiba: le, dia na: iyado Isala: ili dunu ilima amo dio asulima, “Gode Ea fi dunu” amola “Hina Gode da ilima asigisa.”
2 “Dzudzulani amayi anu, adzudzuleni iwo, pakuti si mkazi wanga, ndipo ine sindine mwamuna wake. Iyeyo achotse maonekedwe adama pa nkhope yake, ndi kusakhulupirika pa mawere ake.
“Na mano dilia! Dilia ha: giwane dilia amema edegema. E da wali na uda hame. Amola na da wali ea dunu hame. Amola inia: dunu adole lasu hou amola hina da: iga bidi lasu hou yolema: ne ha: giwane sia: ma.
3 Akapanda kutero ndidzamuvula, ndipo adzakhala wamaliseche monga tsiku limene anabadwa; ndidzamuwumitsa ngati chipululu, adzakhala ngati dziko lopanda madzi, ndi kumupha ndi ludzu.
Be e da dilia sia: i defele hame hamosea, Na da ea abula gagadelale fasili, bu da: i nabado hi musa: emea lalelegei amo defele ba: ma: mu. Amola Na da e soge hano hamedei amola ifa hame heda: i, amo defele hamomu. Amola e da hano hanaga bogomu.
4 Sindidzaonetsa chikondi changa pa ana ake, chifukwa ndi ana a mʼchiwerewere.
5 Amayi awo akhala akuchita zachiwerewere ndipo anawabereka anawo akuchita zinthu zochititsa manyazi. Iwo anati, ‘Ine ndidzatsatira zibwenzi zanga, zimene zimandipatsa chakudya ndi madzi, ubweya ndi thonje, mafuta ndi chakumwa.’
Na da ema amola ea manoma hame asigimu. Bai ea mano da inia: wamomanoba: le, e da hame gogosiasa amola hame beda: sa. Amola uda da hisu amane sia: i, ‘Na da na gilisili golabe dunu ilima masunu. Ilia da nama ha: i manu amola hano, sibi hinabo, abula, olife susuligi amola waini hano iaha.’
6 Choncho njira yake ndidzayitseka ndi minga; ndidzamuzinga ndi khoma kotero kuti sadzapezanso njira yotulukira.
Amaiba: le, Na da asili, aya: gaga: nomei aya: lidili, ea masunu logo hedofama: ne gagomu.
7 Adzathamangira zibwenzi zake koma sadzazipeza; adzazifunafuna koma sadzazipeza. Pamenepo iye adzati, ‘Ndibwerera kwa mwamuna wanga woyamba uja, pakuti ndinali pabwino ndi iyeyo kusiyanitsa ndi pano.’
E da ea sasagesu dunu gagumusa: hehenamu amomane hame gagulaligimu. Ea da amo hogomu be amomane hame ba: mu. Amalalu, e da amane sia: mu, ‘Na ni musa: fi dunu ema sinidigimu. Amola musa: esalusu amo dawa: le, waha esalebe we dawa: loba da musa: esalusu amo da defeadafa dawa: sa.’
8 Iye sanazindikire kuti ndine amene ndinkamupatsa tirigu, vinyo watsopano ndi mafuta. Ndine amene ndinkamukhuthulira siliva ndi golide, zimene ankapangira mafano a Baala.
Ea da gagoma, waini, olife susuligi, silifa amola gouli amoga Ba: ilema nodone sia: ne gadosu. Be amo liligi huluane Na da ema i dagoi, amo e da hamedafa dawa: i.
9 “Choncho Ine ndidzamulanda tirigu wanga pa nthawi yokolola, ndi vinyo wanga watsopano pa nthawi yopsinya mphesa. Ndidzamulanda ubweya ndi thonje langa, zomwe akanaphimba nazo umaliseche wake.
Amaiba: le, na da gamisu eso amoga gagoma amola waini hano Na ema i, amo bu Ni lamu. Amola wulo amola abula Na ema gasisa: lima: ne i, amo bu Ni lamu.
10 Motero tsopano ndidzaonetsa maliseche ake pamaso pa zibwenzi zake; palibe ndi mmodzi yemwe adzamupulumutse mʼmanja mwanga.
Amola Na da ea sasagesu dunu ilia si da: iya ea abula sali gagadelale fasimu. Amola Na gasa bagadeba: le, e da enoga gaga: mu hamedei ba: mu.
11 Ndidzathetsa zikondwerero zake zonse: zikondwerero zake za chaka ndi chaka, za mwezi watsopano, za pa masiku a Sabata ndi maphwando ake onse a pa masiku okhazikitsidwa.
Na da ea lolo nabe gilisisu huluane, ea odega amola oubiga amola Sa: bade amola sia: ne gadosu gilisisu, amo huluane Na da dagolesimu.
12 Ndidzawononga mitengo yake ya mpesa ndi mitengo yake yamkuyu, imene iye ankanena kuti inali malipiro ake ochokera kwa zibwenzi zake. Ndidzayisandutsa chithukuluzi, ndipo zirombo zakuthengo zidzadya zipatsozo.
Na da ea waini efe sagai amola figi ifa (amo da ea gilisili golabe dunu ilia da ema dabe agoane i e da sia: su) amo huluane wadela: lesimu. Na da amo wadela: lesisia, soge da hafoga: i wadela: i soge agoane ba: mu. Amola sigua ohe da amo wadela: lesimu.
13 Ndidzamulanga chifukwa cha masiku amene anafukiza lubani kwa Abaala; anadzikongoletsa povala mphete ndi mikanda yamtengowapatali ndipo anathamangira zibwenzi zake, koma Ine anandiyiwala,” akutero Yehova.
Na da ema se bagade imunu. Bai eso bagohame, e da Na gogolele, ogogosu ‘gode’ Ba: ile ema gabusiga: manoma gobele salasu amola nina: hamosu liligi gaga: ne ea sasagesu dunu ilia ahoabe fa: no bobogesu,” Hina Gode da sia: i dagoi.”
14 “Koma tsopano ndidzamukopa mkaziyo; ndidzapita naye ku chipululu ndipo ndidzamuyankhula mwachikondi.
“Amaiba: le, Na da e bu hafoga: i sogega oule masunu. Amogawi, Na da e Nama bu sinidigima: ne, asigi sia: sia: mu.
15 Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa, ndipo ndidzasandutsa Chigwa cha Akori kukhala khomo la chiyembekezo. Kumeneko iye adzayimba nyimbo monga mʼmasiku a ubwana wake, monga tsiku limene anatuluka ku Igupto.
Na da ea musa: waini efe sagai duga: i amo ema bu imunu. Na da Bidi Hamosu Fago afadenene, bu hahawane misunu logo holei agoane hamomu. E da ea a: fini esoga Idibidi yolesili, Nama asigi galu. Amo defele, e da Nama bu asigimu.
16 “Tsiku limeneli,” Yehova akuti, “udzandiyitana kuti, ‘Amuna anga;’ sudzandiyitananso kuti, ‘Mbuye wanga.’
Amasea, e da bu Nama ‘Nagoa’ sia: mu. E da Nama ‘Na Ba: ile’ amo bu hame sia: mu.
17 Ndidzachotsa mayina a Abaala pakamwa pake; sadzatchulanso mayina awo popemphera.
Amola e da Ba: ile ea dio bu hamedafa sia: ma: ne, Na da hamomu.
18 Tsiku limenelo ndidzachita pangano ndi zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga ndiponso zolengedwa zokwawa pansi kuti ziyanjane ndi anthu anga. Ndidzachotsa mʼdzikomo uta, lupanga ndi zida zonse zankhondo, kuti onse apumule mwamtendere.
Amo esoha, Na da sigua ohe amola sio fi huluane ilima gousa: su hamomu. Ilia da Na fi dunu hamedafa wadela: lesima: ne, Na da gousa: su hamomu. Amola Na da Isala: ili sogega gegesu liligi (gobihei sedade amola dadi) amo huluane samogele fasimu. Amasea, Na hamobeba: le, Na fi dunu da olofole amola gaga: iwane esalumu.
19 Ndidzakutomera kuti ukhale mkazi wanga mpaka muyaya; ndidzakutomera mwachilungamo, mwaungwiro, mwachikondi ndi mwachifundo.
Isala: ili fi! Na da di Na uda hamomu! Na da di hamedafa yolesimu. Na da dima asigidafa hou amola gogolema: ne olofosu hou olelemu. Amola di da Na udadafa agoane esalalalumu.
20 Ndidzakutomera mokhulupirika ndipo udzadziwa Yehova.
Na da Na dafawane ilegei sia: i noga: le ouligili, di Na udadafa hamomu. Amola di da Nama dia Hina Godedafa sia: mu.
21 “Tsiku limenelo Ine ndidzayankha,” akutero Yehova. “Ndidzayankha mlengalenga pempho lake lofuna mitambo ndipo mvula idzagwa pa dziko lapansi;
22 ndipo nthaka idzamvera kupempha kwa tirigu, vinyo ndi mafuta, ndipo zidzamvera Yezireeli.
Amo esoga Na da Na fi Isala: ili dunu ilia sia: ne gadosa adole ba: i liligi ilima imunu. Na da gibu defele imunu. Amasea, osoboga gagoma amola waini fage amola olife fage bagade heda: lebe ba: mu.
23 Ndidzadzala Israeli mʼdziko kuti akhale wanga: ndidzaonetsa chikondi changa kwa anthu amene ndinkawatchula dzina loti, ‘Sakondedwa.’ Ndidzawawuza amene ndinkawatchula dzina loti, ‘Si anthu anga,’ kuti, ‘Ndinu anthu wanga;’ ndipo adzanena kuti, ‘ndinu Mulungu wathu,’”
Na da hamobeba: le, Na fi dunu da ilia sogega hahawane amola bagade gaguiwane esalebe ba: mu. Na da musa: Na fi dunuma, ‘Ilima hame Asigisa’ dio asuli. Be Na da ilima asigidafa hou bu olelemu. Amola Na musa: Na fi dunuma ‘Na fi dunu hame’ dio asuli. Be Na da fa: no ‘Dilia da Na fidafa dunu’ ilima sia: mu. Amola ilia da Nama amane sia: mu, ‘Di da ninia Gode.’”