< Hoseya 14 >

1 Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako. Machimo anu ndi amene akugwetsani!
Dwoguru ir Jehova Nyasaye ma Nyasachu, yaye Israel. Richou ema osemiyo upodho.
2 Bweretsani zopempha zanu ndipo bwererani kwa Yehova. Munene kwa Iye kuti, “Tikhululukireni machimo athu onse ndi kutilandira mokoma mtima, kuti tithe kukuyamikani ndi mawu a pakamwa pathu.
Kaw wechegi kendo uduog ir Jehova Nyasaye! Wachne kama: “Wenwa richowa duto, kendo yie irwakwa gi ngʼwono, mi wanapaki gi dhowa.
3 Asiriya sangatipulumutse; ife sitidzakwera pa akavalo ankhondo, sitidzanenanso kuti, ‘Milungu yathu’ kwa zimene manja athu omwe anazipanga, pakuti ndinu amene mumachitira chifundo ana amasiye.”
Asuria ok nyal resowa, bende ok wana idhi faresegi mag lweny. Ok wanachak wawach kendo ni, ‘Nyisechewa’ ne gik mwaloso gi lwetwa wawegi, nimar kuomi, ema, nyithi kiye yude kech.”
4 Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo ndipo ndidzawakonda mwaufulu pakuti ndaleka kuwakwiyira.
“Anachang-gi kuom baro margi mane gibarogo, kendo anahergi maonge achuna, nimar mirimba osewuok kuomgi.
5 Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli Ndipo iye adzachita maluwa ngati kakombo. Adzazika mizu yake pansi ngati mkungudza wa ku Lebanoni;
Anachal mana ka thoo mar okinyi ne Israel; kendo nolodhi mana ka ondanyo, kendo tiende nokar mana ka yiend Lebanon;
6 mphukira zake zidzakula. Kukongola kwake kudzakhala ngati mtengo wa olivi, kununkhira kwake ngati mkungudza wa ku Lebanoni.
bade nolodhi makee. Enobed maber ka yiend zeituni, kendo nodungʼ mangʼwe ngʼar ka yiend Lebanon.
7 Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake. Iye adzakula bwino ngati tirigu. Adzachita maluwa ngati mphesa ndipo kutchuka kwake kudzakhala ngati vinyo wochokera ku Lebanoni.
Ji nochak odag e tipone. Nonyaa maber mana ka cham, kendo nonyag maber ka mzabibu mi nobed gi huma ka divai moa Lebanon.
8 Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano? Ine ndidzamuyankha ndi kumusamalira. Ine ndili ngati mtengo wa payini wobiriwira; zipatso zako zimachokera kwa Ine.”
Yaye Efraim en angʼo ma datim gi nyiseche manonogi kendo? Anadwoke kendo rite, achalo gi obudo mangʼich, nyak mari aa kuoma.”
9 Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi. Ndani amene amamvetsa zinthu? Adzamvetse izi. Njira za Yehova ndi zolungama; anthu olungama amayenda mʼmenemo, koma anthu owukira amapunthwamo.
En ngʼat mane mariek? Obiro fwenyo tiend gigi. En ngʼat mane manyalo fwenyo tiend wechegi? Obiro ngʼeyogi. Yore mag Jehova Nyasaye nikare, joma nikare ema wuothoe, to joma jendeke to chwanyore.

< Hoseya 14 >