< Hoseya 14 >

1 Iwe Israeli bwerera kwa Yehova Mulungu wako. Machimo anu ndi amene akugwetsani!
Kilekitin O Israel, na Pakai na Pathen hengah. Ajeh chu nathemmona jeh'a lhu nahitai.
2 Bweretsani zopempha zanu ndipo bwererani kwa Yehova. Munene kwa Iye kuti, “Tikhululukireni machimo athu onse ndi kutilandira mokoma mtima, kuti tithe kukuyamikani ndi mawu a pakamwa pathu.
Nasuhkhel ho chu ponlang Pakai henga kilekittan. Akoma seiyin “Kachonsetna jouse neingaidamin, hepitah in nei lalut in. Chutengleh keihon, nangma kachoisang dingu ahi.
3 Asiriya sangatipulumutse; ife sitidzakwera pa akavalo ankhondo, sitidzanenanso kuti, ‘Milungu yathu’ kwa zimene manja athu omwe anazipanga, pakuti ndinu amene mumachitira chifundo ana amasiye.”
Assyria in eihuh jou pouve. Keiho jong sakolte chunga toupovinge, Tukalla lhah keihon jong kakhutsoh-u milim doi jah ah ‘ka Pathen’ katikit louhel dingu ahi. Nachunga hin nulou palouten hepina akimujin ahiye” tiuvin.
4 Ine ndidzachiza kusakhulupirika kwawo ndipo ndidzawakonda mwaufulu pakuti ndaleka kuwakwiyira.
Pakaiyin aseiye, “Tahsan um nahijeha kadamsah ding nahiye, Kangailutnan gamgi aneipoi, Kalunghan najouse aimatihchana dingin mangtahen.
5 Ndidzakhala ngati mame kwa Israeli Ndipo iye adzachita maluwa ngati kakombo. Adzazika mizu yake pansi ngati mkungudza wa ku Lebanoni;
Keima Israel a ding hitange, Vanna kon-a hunglha daitwi chimset tobang hinge. Israel chu Lily pah tobang hiding ahi, ajung jong leipha laiya thuh taha keh hihen, Lebonan lhanga Cedar tobang hin.
6 mphukira zake zidzakula. Kukongola kwake kudzakhala ngati mtengo wa olivi, kununkhira kwake ngati mkungudza wa ku Lebanoni.
Abah lha jong olive thing bangin, namtwi sellin Lebonan-a Cedar phung tobang hihen.
7 Anthu adzakhalanso mu mthunzi wake. Iye adzakula bwino ngati tirigu. Adzachita maluwa ngati mphesa ndipo kutchuka kwake kudzakhala ngati vinyo wochokera ku Lebanoni.
Kamite kalim noiya umkit ding ahi.
8 Efereimu adzati, “Ndidzachita nawonso chiyani mafano? Ine ndidzamuyankha ndi kumusamalira. Ine ndili ngati mtengo wa payini wobiriwira; zipatso zako zimachokera kwa Ine.”
O Israel, milim doi a konin gamlauvin! Keima nataonau donbutpa chu kahi chule navengtup pao chu kahi. Keima thingphung dumjing jeng chu kahi. Nathingga jouse chu keija kon ahiye.”
9 Ndani ali ndi nzeru? Adzazindikire zinthu izi. Ndani amene amamvetsa zinthu? Adzamvetse izi. Njira za Yehova ndi zolungama; anthu olungama amayenda mʼmenemo, koma anthu owukira amapunthwamo.
Jite jousen hitihohi hethemuhen, Thil hetkhenna nei jousen phatechan ngaijuvin. Pakai lampi chu adihin chule ajange, Chule midih ho jouse amatoh umkhom ding ahiuve. Ahilah Michonse ho kiseplhuva kijam dan ding ahiuve.

< Hoseya 14 >