< Hoseya 11 >

1 “Israeli ali mwana, ndinamukonda, ndipo ndinayitana mwana wanga kuti atuluke mu Igupto.
Kad Israēls bija bērns, tad Es viņu mīlēju, un Savu dēlu atsaucu no Ēģiptes.
2 Koma ndimati ndikamapitiriza kuyitana iwo amandithawa kupita kutali. Ankapereka nsembe kwa Abaala ndipo ankafukiza lubani kwa mafano.
Bet jo (tie pravieši) tos sauca, jo vairāk tie no viņiem nogāja; tie upurēja Baāliem un kvēpināja elku tēliem.
3 Ndi Ine amene ndinaphunzitsa Efereimu kuyenda, ndipo ndinawagwira pa mkono; koma iwo sanazindikire kuti ndine amene ndinawachiritsa.
Es tomēr Efraīmu mācīju staigāt, Es tos ņēmu uz Savām rokām, bet tie neatzina, ka Es tos dziedināju.
4 Ndinawatsogolera ndi zingwe zachifundo cha anthu ndi zomangira za chikondi; ndinachotsa goli mʼkhosi mwawo ndipo ndinawerama nʼkuwadyetsa.
Es tos vilku ar cilvēka valgiem, ar mīlestības saitēm, un tiem biju kā kas apaušus no viņu žokļiem atvieglina, un Es tiem pasniedzu barību.
5 “Sadzabwerera ku Igupto, koma Asiriya ndiye adzakhala mfumu yawo pakuti akana kutembenuka.
Viņš neatgriezīsies atpakaļ uz Ēģiptes zemi, bet Asurs, tas būs viņa ķēniņš, tāpēc ka tie liedzās atgriezties.
6 Malupanga adzangʼanima mʼmizinda yawo, ndipo adzawononga mipiringidzo ya zipata zawo nadzathetseratu malingaliro awo.
Un zobens zibēs viņu pilsētās un nobeigs un aprīs viņu aizšaujamos viņu padomu dēļ.
7 Anthu anga atsimikiza zondifulatira Ine. Ngakhale atayitana Wammwambamwamba, sizidzatheka kuti Iye awakwezenso.
Jo Maniem ļaudīm prāts nesās, no Manis nogriezties; tie gan top aicināti uz augšu, bet neviena nav, kas ceļas.
8 “Kodi ndingakusiye bwanji iwe Efereimu? Kodi ndingakupereke bwanji iwe Israeli? Kodi ndingakuchitire bwanji zimene ndinachitira Adima? Kodi ndingathe bwanji kukuchitira zimene ndinachitira Zeboimu? Mtima wanga wakana kutero; chifundo changa chonse chikusefukira.
Kā Es tev darīšu, Efraīm? Vai Man tevi būs nodot, Israēl? Vai Es tev darīšu kā Admai? Vai tevi postīšu kā Ceboīmu? Mana sirds ir griezusies, un Mana apžēlošanās visai iedegusies.
9 Sindidzalola kuti ndikulange ndi mkwiyo wanga woopsa, kapena kutembenuka ndi kuwononga Efereimu. Pakuti Ine ndine Mulungu osati munthu, Woyerayo pakati panu. Sindidzabwera mwaukali.
Es nedarīšu pēc Savas bardzības karstuma, nedz Efraīmu atkal postīšu, jo Es esmu Dievs un ne cilvēks, tas Svētais tavā vidū. Un dusmās Es nenākšu.
10 Iwo adzatsatira Yehova; Iye adzabangula ngati mkango. Akadzabangula, ana ake adzabwera akunjenjemera kuchokera kumadzulo.
Tad tie dzīsies Tam Kungam pakaļ, Viņš kauks kā lauva, un kad Viņš kauks, tad tie bērni no vakara puses drebēs.
11 Adzabwera akunjenjemera ngati mbalame kuchokera ku Igupto, ngati nkhunda kuchokera ku Asiriya. Ine ndidzawakhazikanso mʼnyumba zawo,” akutero Yehova.
Tie drebēdami nāks no Ēģiptes, kā putns un kā balodis no Asura zemes, un Es tiem likšu dzīvot viņu namos, tā saka Tas Kungs.
12 Efereimu wandizungulira ndi mabodza, nyumba ya Israeli yandizungulira ndi chinyengo. Ndipo Yuda wawukira Mulungu, wawukira ngakhale Woyerayo amene ndi wokhulupirika.
Efraīms Mani apstāj ar meliem un Israēla nams ar viltu, un Jūda vēl šaubās ap Dievu, to uzticīgo un svēto.

< Hoseya 11 >