< Ahebri 1 >

1 Kale lija Mulungu ankayankhula ndi makolo athu pa nthawi zosiyanasiyana ndiponso mwa njira zosiyanasiyana kudzera mwa aneneri.
Beni wodepe oykidi Xoossi dumma dumma ogera nabeta baggara kase nu Aawatas daro wode yootides.
2 Koma masiku otsiriza ano, Mulungu wayankhula nafe kudzera mwa Mwana wake. Mwanayu anamusankha kuti akhale mwini wa zinthu zonse, ndiponso Mulungu analenga dziko lonse kudzera mwa Iye. (aiōn g165)
Qasse hayssa wurisetha wode bolla wursi latisidane ha alameza midhida ba naaza baggara nuusu yootides. (aiōn g165)
3 Mwanayo ndiye kuwala kwa ulemerero wa Mulungu, chithunzithunzi chenicheni cha khalidwe lake. Iyeyu amachirikiza zinthu zonse ndi mphamvu ya mawu ake. Iye atayeretsa anthu kuchoka ku machimo awo, anakhala pansi kumwamba kudzanja lamanja la Mulungu waulemerero.
Izika Xoossa boncho po7osine Xoossa xoossatethas lo7o lemuso gididi ba wolliqama qaalan wursika shiishi oykides. Izi asa nagarape geeshidape guye salon boncho Xoossa oshachan uttides.
4 Mwanayu ndi wamkulu koposa angelo, monga momwe dzina limene analandira limaposa dzina la angelo.
Hessa gishshi laattida sunthay kiitanchata sunthafe adhdhizayssa mala izika kiitanchatape keehi adhdhees.
5 Kodi ndi kwa mngelo uti, kumene Mulungu anati, “Iwe ndiwe mwana wanga; Ine lero ndakhala Atate ako.” Kapena kunenanso kuti, “Ine ndidzakhala abambo ake; iye adzakhala mwana wanga.”
Xoossi kiitanchape “Neni ta nako, Ta nena hachchi yeladis.” Woyko qasseka Ta izas Aawa gidana; Izika ta ta gidana” Oonas gidee?
6 Pamene Mulungu amatuma Mwana wake woyamba kubadwa ku dziko lapansi anati, “Angelo onse a Mulungu amupembedze Iye.”
Qasseka Xooss ba bayra naaza duge ha biitta yeddishe “Xoossa kiitanchati wurikka izas goyneto” gides.
7 Iye ponena za angelo akuti, “Mulungu amasandutsa angelo ake mphepo, amasandutsa atumiki ake malawi amoto.”
Kiitanchata gishshi hasa7ishe qasse “Kiitanchata ayanata; Be oothanchataka tama laco kesses” gees.
8 Koma za Mwana wake akuti, “Inu Mulungu, mpando wanu waufumu udzakhala mpaka muyaya, ndipo mudzaweruza molungama mu ufumu wanu. (aiōn g165)
Nza gishshi qasse “Godo ne zupaney medhinape medhina gakanas minni deyana. Neni ne kawotetha like kaalethasa. (aiōn g165)
9 Mwakonda chilungamo ndi kudana ndi zoyipa; Nʼchifukwa chake, Mulungu wanu wakukwezani kuposa anzanu pokudzozani mafuta osonyeza chimwemwe.”
Neni xiillotehta dosadasa. Makal7aka ixxasa. Hessa gishshi Xoossi ne Goday nena ne lagistape bolla kessides. Nena ufayssa zayte tiyides.
10 Mulungu akutinso, “Ambuye, pachiyambi Inu munayika maziko a dziko lapansi; ndipo zakumwambako ndi ntchito za manja anu.
Qasse hizgees “Godo neni koyro biitta medhadasa. Salo tika ne kushen oothetida.
11 Zimenezi zidzatha, koma Inu ndinu wachikhalire. Izo zidzatha ngati zovala.
Istti dhayana, neni gidiko minna deyana. Istti wurikka mayo mala gal7ana.
12 Mudzazipindapinda ngati chofunda; ndipo zidzasinthidwa ngati chovala. Koma Inu simudzasintha, ndipo zaka zanu sizidzatha.”
Neni istta mayo mala qalam77ana. Isttika mayo mala laamistana. Ne gidiko aydeka neni nena. Ne duusas wurisethi deena” gees.
13 Kodi ndi kwa Mngelo uti kumene Mulungu ananenapo kuti, “Khala kudzanja langa lamanja mpaka nditapanga adani ako kukhale chopondapo mapazi ako.”
Xoossi kiitanchatape “Tani ne morketa ne too garisan nena yedhisana gakanas ne ta oshachan utta” Oona gidee?
14 Kodi angelo onse si mizimu yotumikira odzalandira chipulumutso?
Kiitanchati wurikka atotetha laatana asatas oothanas Xoossafe kiitetiza oothancha ayana gidetenee?

< Ahebri 1 >