< Ahebri 2 >
1 Nʼchifukwa chake, ife tiyenera kusamalira kwambiri zimene tinamva, kuopa kuti pangʼono ndi pangʼono tingazitaye.
Hessa gishshi nuni siyda qaalape balettidi kundontta mala nu siyida qaala lo7ethi naagans besses.
2 Popeza uthenga umene unayankhulidwa kudzera mwa angelo unali okhazikika ndithu, choncho aliyense amene ananyozera ndi kusamvera analandira chilango choyenera.
Azas gikko kase kitanchata bagara yotetida qalay tumu gidida he qaala yedhi adhiday bees bessiza qixate ekees.
3 Nanga ife tidzapulumuka bwanji tikapanda kusamala chipulumutso chachikulu chotere? Ambuye ndiye anayamba kuyankhula za chipulumutsochi, kenaka amenenso anamvawo anatitsimikizira.
Nu qase hessa mala gita maaroteth coo leppi hisitko waani attanee? Hayssi maarotethay koyro Goda baggara nuusu yootetides. Izape siyidaytika nuusu geeshi yootida.
4 Mulungu anachitiranso umboni pochita zizindikiro, zinthu zodabwitsa ndi zamphamvu zamitundumitundu ndi powapatsa mphatso za Mzimu Woyera monga mwachifuniro chake.
Xoossi qasseka malatata, malalithiza miishata, dumma dumma malatata oothonine ba shene mala immida xiillo ayana imotata baggara istta markatethaa minithides.
5 Mulungu sanapereke kwa angelo ulamuliro wa dziko limene likubwerali, limene ife tikulinena.
Xoossi hayssa nu iza gishshi hasa7iza buro yaana alameza kiitanchas harisibeyna.
6 Koma palipo pena pamene wina anachitira umboni kuti, “Kodi munthu ndani kuti muzimukumbukira, kapena mwana wa munthu kuti muzimusamalira?
Gido attin geisha maxaafay harason hizigdes “Ne izas yuusha qopanas asi aazee? Izas ne qopanas asanay izi aazee?
7 Munamuchepetsa pangʼono kusiyana ndi angelo; munamupatsa ulemerero ndi ulemu.
Ne iza kiitanchatape guuth wodes guuthadasa. Boncho zawudene galata iza hu7en wothadas.
8 Munamupatsa ulamuliro pa zinthu zonse.” Poyika zinthu zonse pansi pa ulamuliro wake, Mulungu sanasiye kanthu kamene sikali mu ulamuliro wake. Koma nthawi ino sitikuona zinthu pansi pa ulamuliro wake.
Ne wursaka iza too garisan haarisadasa. Xoossi wursika izape garisara izas harisishin attiday ay miishika deena. Gido attin ha7i qasse wurikka izas haretishin nu beyok.
9 Koma tikuona Yesu, amene kwa kanthawi kochepa anamuchepetsa pangʼono kwa angelo, koma tsopano wavala ulemerero ndi ulemu chifukwa anamva zowawa za imfa, kuti mwachisomo cha Mulungu, Iye afere anthu onse.
Gido attin Xoossa kiyatethan asa wuriso gishshi hayqanas kiitanchatape guutha wode guuxida Yesusay waaye hayqo hayqidi ha7i bonchone galata zawude ba hu7en wothidayssa beyosu.
10 Mulungu amene analenga zinthu zonse ndipo zinthu zonse zilipo chifukwa cha Iye ndi mwa Iye, anachiona choyenera kubweretsa ana ake ambiri mu ulemerero. Kunali koyenera kudzera mʼnjira ya zowawa, kumusandutsa Yesu mtsogoleri wangwiro, woyenera kubweretsa chipulumutso chawo.
Hanzay wurikka izape izas medhetida Xoossi daro nayta bonchoso efanas istta marotethas hu7e gidida Yesusay waayen polanas koshizazi giddies.
11 Popeza iye amene ayeretsa ndi oyeresedwa onse ndi abanja limodzi. Nʼchifukwa chake Yesu sachita manyazi kuwatcha iwo abale ake.
As geeshizayinne izan geeyiza asay heyti issi keeththa aseko. Hessa gishshi Yesusay istta ba ishata gi xeyganas yellatena.
12 Iye akuti, “Ine ndidzawuza abale anga za dzina lanu. Ndidzakuyimbirani nyimbo zamatamando pamaso pa mpingo.”
“Tani ne sunththan ta ishatas yootana shiiqida dere sinthan nena galatiza yethi ta yexana.”
13 Ndiponso, “Ine ndidzakhulupirira Iyeyo.” Ndiponso Iye akuti, “Ine ndili pano pamodzi ndi ana amene Mulungu wandipatsa.”
Hessaththoka “Ta izan ammanetana” qasseka “Tanane taas Xoossi immida nayti nu handes” gees geesha maxaafay.
14 Tsono popeza kuti anawo ndi anthu, okhala ndi mnofu ndi magazi, Yesu nayenso anakhala munthu ngati iwowo kuti kudzera mu imfa yake awononge Satana amene ali ndi mphamvu yodzetsa imfa.
Nytas ashoyne suthi diza mala izika istta mala aseko. Hessika hayqo bolla izas wolqay diza dabulosa izi ba hayqo wolqan zaaranas.
15 Pakuti ndi njira yokhayi imene Iye angamasule amene pa moyo wawo wonse anali ngati akapolo chifukwa choopa imfa.
Hessaththoka ba diza wode wurison hayqos babon hareti qachetidayta hayqope wozanaskko.
16 Pakuti tikudziwanso kuti sathandiza angelo, koma zidzukulu za Abrahamu.
Izi ha yiday kiitanchata maadanas gidonta Abirame zerethista maadanas yides.
17 Chifukwa cha zimenezi, Iye anayenera kukhala wofanana ndi abale ake pa zonse, kuti akhale mkulu wa ansembe wachifundo ndi wokhulupirika potumikira Mulungu, kuti potero achotse machimo a anthu.
Hesa gishshi wuriso baggara izi ba ishata milatanas besizade gidides. Izi hessa oothiday maarizadene ammanetida waana qesse halaqa gididi Xoossas oothanasine dereza nagarape maaranaskko.
18 Popeza Iye mwini anamva zowawa pamene anayesedwa, Iyeyo angathe kuthandiza amene akuyesedwanso.
Izi ba hu7en pacetidi meto ekkida gishshi paccetizayta maadanas danda7es.