< Ahebri 12 >
1 Tsono popeza ifenso tazunguliridwa ndi gulu lalikulu la mboni, tiyeni titaye chilichonse chimene chimatitchinga, makamaka tchimo limene limatikola mosavuta, ndipo tithamange ndi khama mpikisano umene tayambawu.
Daawnok'o noon gúúrts gaw jamanotsi no detstsotse no'ats kur wotts keew jamwotsi no'ats deshts morro k'a'úbayr no shinatse beyiru nohewo k'amde kup'ar woc'one.
2 Tiyeni tiyangʼanitsitse Yesu, amene ndi woyamba ndi wotsiriza wa chikhulupiriro chathu. Chifukwa cha chimwemwe chimene chimamudikira anapirira zowawa zapamtanda. Iye ananyoza manyazi a imfa yotere ndipo tsopano akukhala ku dzanja lamanja la mpando waufumu wa Mulungu.
Nowos'etwere no imnetiyo ned'itsonat s'eentstso Iyesus ats no ááwo gerdeniye, bíwere b́ shinatse need'wtsts geneúwatse tuutson jitatse k'irr gac'ewo eegok'oor b́ taawrawo jitatse gondbek'on k'iro k'amb́dek'i, Ik' be jooroke k'ano maants be b́wtsi.
3 Muzilingalira za Iye amene anapirira udani waukulu chotere wochokera kwa anthu ochimwa, kuti musafowoke ndi kutaya mtima.
Eshe taahr, maac'o it k'ut'rawok'o morretswots bín bo k'eefere k'amdek'tso Iyesusi s'ilde'ere.
4 Polimbana ndi uchimo, simunafike mpaka pokhetsa magazi.
It morronton mak'orewoke s'ats kud'efetsosh b́borfetso k'eferafa'tee.
5 Kodi mwayiwala mawu olimbitsa mtima aja, amene Mulungu anayankhula kwa inu ngati ana ake? Mawuwo ndi awa: “Mwana wanga, usapeputse kulanga kwa Ambuye ndipo usataye mtima pamene akukudzudzula.
Ik'o b́ nana'ikok'o woshdek't itango kup'shosh hank'o bí ettso batk'rerte, «T naayo! doonzo sezo ketik'aye, b́ hadoshowere maac'o k'ut'k'aye,
6 Chifukwa Ambuye amadzudzula amene amawakonda ndipo amalanga aliyense amene amamulandira.”
Doonzo b́ shuntsoniye b́ sezfoni, B́ nayik'owosh dekt b́s'iliruwono b́fayefoni.»
7 Pamene mukupirira masautso monga chilango, Mulungu achitira inu monga ana ake. Kodi ndi mwana wotani amene abambo ake samulanga?
Ik'o b́ nanaúwotsk'o itn b́tawtsotse b́ sezo k'amoore, b́ niho bín b́ sezraw na'o kone?
8 Ngati inu simulangidwa, komatu aliyense amalangidwa, ndiye kuti sindinu ana enieni koma amʼchigololo.
Nana'a wotts jamwots bo daatsiru sezo it were daatso it k'azal dik'al itna boko nana'a itnaliye.
9 Komanso, tonsefe tinali ndi abambo athu otibala amene amatilanga ndipo timawapatsa ulemu. Nanga kodi sitidzagonjera Atate a mizimu yathu kuti tikhale ndi moyo?
Haniyere okoon, noúnetsi sezf meetsi nihwots detsfone b́teshi, bonowere mangiye nomangifoni, bere kashon beyosh kashi weeron nih wottsosh iki bogshde azazewo aawk'oneya noosh geyiwo b́k'azeti!
10 Abambo athu ankatilanga kwa kanthawi kochepa monga amaonera kufunika kwake, koma Mulungu amatilanga kuti tipindule, kuti tikhale oyera mtima.
Bosh sheengo araat b́ be'etsok'on muk' gizewush noon sezrne, bímo b́ S'ayino kayitwotsi nowotish sheengosh noon sezfe.
11 Palibe chilango chimene chimaoneka kuti ndi chabwino pa nthawiyo, komatu chowawa. Koma pambuyo pake, chimabweretsa chipatso chachilungamo ndi mtendere kwa iwo amene aleredwa mwa njira imeneyi.
Sez jamo manorish shiyanitka bako geneúshitk areratse, ilomo man dandek'ts ashuwotssh jeenon s'eentso kááw fini shwo boosh daatsituwe.
12 Nʼchifukwa chake limbitsani manja anu otopa ndi mawondo anu ogowoka.
Mansh it kish neftswotsnat itgubr maawtswotsi kup'ide'ere.
13 Muziyenda mʼnjira zowongoka, kuti iwo amene akukutsatirani ngakhale ndi olumala ndi ofowoka asapunthwe ndi kugwa koma adzilimbikitsidwa.
Doklirwo b́ kashitwok'owa bako b́ beyoke keer b́ tisherawok'o, it tufooshowere weerindi kááwo woshde'ere.
14 Yesetsani kukhala pa mtendere ndi anthu onse ndi kukhala oyera mtima, pakuti popanda chiyero palibe ndi mmodzi yemwe adzaona Ambuye.
S'ayn woteraniye konworu doonzo bek'osh b́ falawotse, ash jamonton jeenon bewore, S'ayinon beyoshowere kup'owere,
15 Yangʼanitsitsani kuti wina aliyense asachiphonye chisomo cha Mulungu ndiponso kuti pasaphuke muzu wamkwiyo umene udzabweretsa mavuto ndi kudetsa ambiri.
Ititsere konshoru Ik' s'aato b́ shaprawok'o it atso korde'ere, mank'owere s'aam shuu iko shuwit s'ap'o ititse boc'r iti b́ kic'irawok'o, aywotsno b́ kimshrawok'o korde'ere.
16 Yangʼanitsitsani kuti pasakhale wina wachigololo. Kapena wosapembedza ngati Esau, amene chifukwa cha chakudya cha kamodzi kokha anagulitsa ukulu wake.
Gusiyetso wee iknoti móósha ett b́ took k'aabo kemtso Esawkok'o shayri ash woterawo ititsere b́ daatserawok'o it atso korde'ere.
17 Monga inu mukudziwa, pambuyo pake pamene anafuna kuti adalitsidwe anakanidwa. Sanapezenso mpata woti asinthe maganizo, ngakhale anafuna madalitsowo ndi misozi.
Esaw il s'aato aaniy dek'osh b́ geyor s'aatman bísh baziyetsok'o danfte, b́k'altso woniyosh kup'dek't eepfetst b́geyiyalor weero daatso falratse.
18 Inu simunafike ku phiri limene mungathe kulikhudza, loyaka moto wa mdima bii, la mphepo yamkuntho;
Kishon shuu'etwok wee mis'etuo Sin gurok borafa'ate, bamplomants, shatits t'alwots, eegurahi jongokowere,
19 limene pali kulira kwa lipenga, ndiponso kumveka kwa mawu. Anthu amene amamva mawuwo anapempha kuti asawayankhulenso mawu ena.
Ezbedi k'arokowere wee keeweyiru aap'o b́ shishetwoko borafa'ate, aap'ets keewman shishts ashuwots «Eshe bodre haniyak k'osho noosh aap'ek'aye» et bok'onfetso bodrnee.
20 Iwo anachita mantha ndi lamulo lija lakuti, “Ngakhale nyama ikangokhudza phirilo, iphedwe ndi miyala.”
«Gizo dab gurman b́ t'awiyal Shútson togeyar k'irwee» Etiru tzaziyo boats b́mangtsosh bín kuro falratsne.
21 Maonekedwenso a Mose anali woopsa kwambiri, ngakhale Mose yemwe anati, “Ine ndinachita mantha ndi kunjenjemera.”
Manoke bek'ets keewman eenonat shatiik b́teshtsotse dab́ Muse woor «Taa shataat, k'ewere» bí et.
22 Koma inu mwafika ku Phiri la Ziyoni, ku mzinda wa Mulungu wamoyo, Yerusalemu wakumwamba. Mwafika mu msonkhano wa angelo osangalala osawerengeka.
Itiyelee S'iyon guromants t'inwtsertee, bihe kashetso Ik'o kito wotts daritstsu Iyerusalemiye, genee'úwon kakwedek'tswotsok, ay kumon taawet mlakiwotsok t'inrte,
23 Mwafika mu mpingo wa ana oyamba kubadwa, amene mayina awo analembedwa kumwamba. Inu mwafika kwa Mulungu, woweruza anthu onse, ndiponso kwa mizimu ya anthu olungama ndi osandutsidwa kukhala angwiro.
Bo shúútso darots guut'etswotsok, k'aab nana'a wotts amantsuwots ko'eetsok, kááw angshitu Izar izewerokonat s'ayin wotat daatsts shayirwotsok t'inrte.
24 Kwa Yesu mʼkhalapakati wa pangano latsopano, ndiponso mwafika ku magazi owazidwa amene amayankhula mawu abwino kuposa magazi a Abele.
Handr taareyosh dag taalotse manik wottso Iyesusnat Abeel s'atsoniyere k'antso keewiru fakets s'atsookowere t'inrte.
25 Chenjerani kuti musakane kumvera amene akuyankhula nanu. Anthu amene anakana kumvera iye amene anawachenjeza uja pa dziko lapansi pano, sanapulumuke ku chilango ayi, nanga tsono ife tidzapulumuka bwanji ngati tikufulatira wotichenjeza wochokera kumwamba?
Keewirman de'atsone it erawok'o itatso korde'ere, Ekeewots Ik'o ashon datsatse boosh b́ keewre k'ewatsone ettswots b́shirotse kesho bomaawiyakon, bére noo darotse noosh keewirwo dek'onok'azal awuk'o kalrniya b́ kishotse kesho nofaliti!
26 Pa nthawiyo mawu ake anagwedeza dziko lapansi, koma tsopano Iye walonjeza kuti, “Kamodzi kenanso ndidzagwedeza osati dziko lapansi lokha komanso thambo.”
Manoor bí aap'o datso shek'ere, «andmó datsu mec'ro b́woterawo aani dabr darono dabde'er shek'ituwe» eton keewure.
27 Mawu akuti, “Kamodzi kenanso,” akuonetsa kuchotsedwa kwa zimene zitha kugwedezeka, zonse zolengedwa, kotero kuti zimene sizingatheke kugwedezeka zitsale.
Han «Iknoto dabr, » etiru keewoniye b́ kitsiriyee shek'eraw keewwots kup'arr bobetuwok'o shek'eyirwots wee azeets keewwots bobeyoke botuwitok'oniye.
28 Popeza tikulandira ufumu umene sungagwedezeke, tiyeni tikhale oyamika ndi kupembedza Mulungu movomerezeka ndi mwaulemu ndi mantha.
Eshe noo shek'eraw mengstu nonaatetwotse Ik'o udoonee, b́ gene'úwitwok'oon mangiyonat shatoon bísh finone.
29 Pakuti Mulungu wathu ndi moto wonyeketsa.
No Ik'o Izar Izewer mitsit tawok'oyiye.