< Ahebri 10 >

1 Malamulo ndi chithunzithunzi cha zinthu zabwino zimene zikubwera, osati madalitso enieniwo. Pa chifukwa chimenechi sizingatheke konse kuti nsembe zimodzimodzi, zoperekedwa kawirikawiri, kosalekeza ndi chaka ndi chaka, kuti nʼkusandutsa angwiro amene amabwera kudzapembedza.
Bangkongtetpawiteh, kâlawk teh ka tho hane hno kahawinaw e a tâhlip lah ao teh, a katang e lah awmhoeh. Hatdawkvah, kum tangkuem sathei thuengnae lahoi Ama koevah thuengnae kasaknaw teh kuepnae koe phat thai awh hoeh.
2 Ngati zikanamatero iwowo akanasiya kupereka nsembezo. Pakuti opembedzawo akanamayeretsedwa kamodzi kokha, sibwenzi chikumbumtima chawo chikuwatsutsabe chifukwa cha machimo awo.
Hottelah hoehpawiteh, kabawkkungnaw hah vai touh hoi a yon thoungsak toung vaiteh, yonpennae awm hoeh toung vaiteh sathei thuengnae laipalah awm awh mahoeh namaw.
3 Koma nsembezo zimawakumbutsa anthuwo machimo awo chaka ndi chaka.
Hatei, hottelah thuengnae lahoi a kum tangkuem yonnae boutbout a pouk awh.
4 Chifukwa nʼkosatheka kuti magazi angʼombe yayimuna ndi mbuzi yayimuna achotse machimo.
Bangkongtetpawiteh Maito hoi hmae e a thi ni yonnae hah thoungsak thai hoeh.
5 Nʼchifukwa chake Khristu atabwera pa dziko lapansi anati, “Simunafune nsembe kapena zopereka, koma thupi munandikonzera.
Hatdawkvah Jisuh ni het talaivan a tho navah, oe Cathut, nang ni sathei hoi thuengnae na ngai hoeh dawkvah, kai hanlah tak hah rakueng pouh toe.
6 Simunakondwere nazo nsembe zopsereza ndi nsembe zopereka chifukwa cha tchimo.
Bawipa ni hmaisawi thuengnae hoi yon thuengnae hah a ngai e nahoeh.
7 Tsono, Ine ndinati, ‘Ndili pano Ine, Inu Mulungu, ndabwera kudzachita zimene mukufuna monga zinalembedwa mʼMalemba.’”
Hatnavah, Kai ni cakalawng dawk kai hanelah na thut e patetlah, na ngainae sak hanelah kai teh ka tho toe Cathut telah ka dei pouh.
8 Poyamba Iye anati, “Nsembe kapena zopereka zopsereza ndi nsembe zopereka chifukwa cha tchimo, Inu simunazifune kapena kukondwera nazo.” Ngakhale kuti Malamulo ndiye amanena kuti ziperekedwe.
Ahmaloe vah, kâlawk patetlah thuengnae sak e naw, sathei hoi hno poe e naw, hmaisawi e sathei hoi yonthanae satheinaw hah ka ngai hoeh, hotnaw dawkvah lungkuepnae haiyah ka tawn hoeh, telah a ti.
9 Pamenepo Iye anati, “Ndili pano Ine, ndabwera kudzachita zimene mukufuna.” Khristu anachotsa nsembe zoyamba zija kuti mʼmalo mwake ayikemo nsembe za mtundu wachiwiri.
Hathnukkhu, Bawipa e ngainae tawk hanelah ka tho, telah ati. Hettelah hoi Bawipa ni apâhni thuengnae hah acak sak teh, apasueke thuengnae hah a takhoe.
10 Chifukwa chakuti Yesu Khristu anachita zimene Mulungu anafuna kuti achite, ndife oyeretsedwa ndi nsembe ya thupi lake, limene analipereka kamodzi kokha.
Hote ngainae lahoi, Jisuh Khrih ni a tak hah vai touh hoi kakhoutlah a thueng e lahoi maimouh teh yon thoungsak lah o awh.
11 Wansembe aliyense amayimirira tsiku ndi tsiku nʼkutumikira, ndipo amapereka nsembe imodzimodzi mobwerezabwereza, nsembe zimene sizingathe kuchotsa machimo.
Vaihmanaw pueng ni hnintangkuem a kangdue awh teh thuengnae hoi yon katha thai hoeh e sathei hah atu hoi atu thuengnae a sak awh.
12 Koma pamene wansembe uyu anapereka kamodzi kokha nsembe imodzi yokha chifukwa cha machimo, Iye anakhala pansi ku dzanja lamanja la Mulungu.
Hatei, Khrih ni yonnae hanelah vai touh dueng thuengnae lahoi a yungyoe han kakhoutlah a sak hnukkhu, Cathut e aranglah a yungyoe a tahung.
13 Kumeneko akudikira tsono kuti Mulungu asandutse adani ake kukhala chopondapo mapazi ake.
Ama e a tarannaw khok toungnae lah ao hoehroukrak ngaihawi laihoi a ring.
14 Chifukwa cha nsembe imodzi Iye anasandutsa angwiro kwamuyaya iwo amene akuwayeretsa.
Bangkongtetpawiteh Bawipa ni vai touh dueng thuengnae lahoi thoungsak lah kaawm e naw hah yungyoe akuep sak.
15 Mzimu Woyera nayenso akuchitira umboni za zimenezi kwa ife. Poyamba Iye anati,
Kathoung Muitha nihaiyah maimouh koe na kampangkhai.
16 “Ili ndi pangano limene ndidzachita nawo atapita masiku amenewo,” akutero Yehova. “Ndidzayika malamulo anga mʼmitima mwawo, ndipo ndidzawalemba mʼmaganizo mwawo.”
Cathut ni atotovah ahnimouh koe ka poe hane lawkkam teh, Kai Cathut ni kâlawknaw hah ahnimae a lungthin dawk ka pakhum pouh han. A lungthin muitha dawk ka thut pouh han, telah a ti.
17 Ndipo akutinso: “Sindidzakumbukiranso konse machimo awo ndi zolakwa zawo.”
Hahoi, Kai ni ahnimae a yonnae hoi kâlawk a tapoenae hah ka pâkuem pouh mahoeh toe telah a ti.
18 Ndipo pamene machimo akhululukidwa, sipafunikanso nsembe yoperekedwa chifukwa cha machimowo.
Hottelah yonthanae a onae hmuen koe teh yon hanlah thuengnae bout panki hoeh toe.
19 Ndipo tsono abale, molimba mtima timalowa mʼMalo Opatulika kwambiri chifukwa cha magazi a Yesu.
Hatdawkvah, hmaunawnghanaw, maimouh teh Jisuh e thipaling pawlawk dawk hoi hmuen kathoung poung koe kâen hanlah taranhawinae tawn awh.
20 Iye anatitsekulira njira yatsopano ndi yamoyo kudutsa chinsalu chotchinga, chimene ndi thupi lake.
Hote a thi lahoi, Bawipa ni amae tak lah kaawm e lukkarei yap e koehoi hringnae lamthung katha hah na rasoun pouh awh.
21 Ndiponso tili ndi wansembe wamkulu woyangʼanira nyumba ya Mulungu.
Hot dueng tho laipalah, maimouh koevah Cathut imthungkhu ka uk e kalenpounge Vaihma tawn awh dawkvah,
22 Tsono tiyeni tiyandikire kwa Mulungu ndi mtima woona ndi wodzaza ndi chikhulupiriro. Popeza mitima yathu yayeretsedwa, ndi yopanda chikumbumtima chotitsutsa, ndiponso matupi athu asambitsidwa ndi madzi woyera.
maimae lungthin dawk e thoehawi panuenae kahawihoehe teh thoungsak lah o toe, maimae tak hai tui kathoung hoi pâsu lah ao toung dawkvah yuemnae kakuep tawn hoi lungthin katang hoi Cathut hnai awh sei.
23 Tiyeni tigwiritsitse mosagwedezeka zimene timaziyembekezera ndi kuzivomereza, pakuti amene anatilonjezayo ndi wokhulupirika.
Lawkkamnae kapoekung teh lawkkam acak dawkvah pâpho awh e ngaihawinae hah kâhuen sak laipalah caksak awh sei.
24 Tiziganizira mmene tingalimbikitsirane wina ndi mnzake pokondana ndi kuchita ntchito zabwino.
Hahoi, lungpatawnae tawn thai nahan hoi hnokahawi sak thai nahanlah buet touh hoi buet touh tha kâpoe awh nateh kâkhen awh.
25 Tiyeni tisaleke kusonkhana kwathu pamodzi monga mmene ena amachitira, koma tizilimbikitsana makamaka poona kuti tsiku la Ambuye layandikira.
Tami tangawn ni a sak e patetlah kamkhuengnae pahnawt laipalah, buet touh hoi buet touh kâhruetcuet awh sei. A tue hoehoe a hnai toung dawkvah, hottelah hoe sak awh sei.
26 Ngati ife tipitirira kuchimwa mwadala pamene tikudziwa choona, palibenso nsembe ina imene ingaperekedwe chifukwa cha machimo athuwo.
Bangkongtetpawiteh, lawkkatang panue awh hnukkhu, ma ngai lahoi yonnae bout sak awh pawiteh, yonnae tha nahanelah thuengnae bout awmhoeh toe.
27 Koma kumangodikira kokha ndi mantha chiweruzo ndiponso moto woopsa umene udzawononga adani a Mulungu
Lawkcengnae thoseh, ama ka taran e taminaw raphoe nahane a lungkhueknae hmai thoseh, kak hane taki laihoi ring hane dueng doeh kaawm toe
28 Aliyense amene amakana malamulo a Mose amaphedwa popanda nʼchifundo chomwe, malingana pali mboni ziwiri kapena zitatu.
Mosi e kâlawk ka tapoe e tami teh kapanuekkhaikung kahni touh na ou, kathum touh na ou awm pawiteh, pahren laipalah a due sak awh.
29 Koposa kotani nanga ululu wachilango chimene adzalandire munthu amene amapeputsa Mwana wa Mulungu, amene amayesa magazi a pangano, amene anamuyeretsa, kukhala chinthu chodetsedwa, ndi kunyoza Mzimu wachisomo?
Hothloilah, Cathut Capa khok hoi ka coungroe niteh, ama thoungnae lawkkam thipaling hah hno kathoung hoeh lah ka pouk e naw hoi lungmanae hoi ka kâkuen e Muitha ka dudam e naw teh banghloi kalen e reknae maw a khang hanlah a kamcu telah na pouk awh.
30 Pakuti timadziwa amene anati, “Kubwezera chilango nʼkwanga; ndidzawalanga ndine.” Iye anatinso, “Ambuye adzaweruza anthu ake.”
Bangkongtetpawiteh, kut pathungnae teh kaie doeh, kama roeroe ni ka pathung han, ti hai thoseh, Cathut ni a taminaw lawk a ceng han ti hai thoseh, ka tet e hah maimouh ni panue awh.
31 Nʼchinthu choopsa kugwa mʼmanja a Mulungu wamoyo.
Kahring Cathut e kut dawk pha e teh taki a tho poung e hno doeh.
32 Kumbukirani masiku akale aja mutangowunikiridwa chatsopano, pa nthawi imeneyi munapirira zowawa zambiri.
Nangmouh ni angnae dawk na pha hnukkhu, rucatnae puenghoi na khang awh e yampa e ahnin thapanaw hah pouk awh.
33 Nthawi zina ankakunyozani pagulu ndi kukuzunzani. Nthawi zina munkamva zowawa pamodzi ndi amene ankasautsidwa chotere.
Avaivai nangmouh ni taminaw hmalah yonpennae hoi rucatnae na khang awh teh, avaivai, hottelah kasaknaw kakhangkhaikung lah na o awh.
34 Munkawamvera chisoni amene anali mʼndende ndiponso munkalola mokondwera kuti akulandeni katundu wanu chifukwa munkadziwa kuti muli nacho chuma choposa ndi chosatha.
Nangmouh ni thongkabawtnaw na pahren awh dueng tho laipalah, hoehoe ka talue niteh kangning e hno kalvan vah na tawn e hah na panue awh dawkvah, na hnopainaw ayâ ni na lawp awh nakunghai, lunghawicalah hoi na panguep awh.
35 Tsono musataye kulimbika mtima kwanuko pakuti mudzalandira nako mphotho yayikulu.
Hatdawkvah, tawkphu kalenpoung lah ka awm e na yuemnae kacakpounge hah tâkhawng awh hanh.
36 Nʼkofunika kuti mupirire kuti pamene muchita chifuniro cha Mulungu mudzalandire zimene Iye analonjeza.
Cathut ngainae sak hnukkhu, lawkkam e coe nahanlah nangmouh dawk a panki e hno teh panguepnae doeh.
37 Pakuti nʼkanthawi kochepa chabe, Iye amene akubwera adzabwera ndipo sadzachedwa ayi.
Bangkongtetpawiteh, ka tho hane Ahni teh nâsittouh awm mahoeh toe, palang a tho han toe.
38 Koma wolungama wangayo adzakhala ndi moyo mwachikhulupiriro. Ndipo ngati iye abwerera mʼmbuyo chifukwa cha mantha, Ine sindidzakondwera naye.
Tami kalan teh yuemnae lahoi a hring han. Hatei, hnuk kâhnawn pawiteh ka lungthin Muitha ni ahni koe ka lunghawi mahoeh, telah Cathut ni a ti.
39 Koma ife sindife amodzi a iwo obwerera mʼmbuyo mwa mantha ndi owonongedwa, koma ndife amodzi a amene akukhulupirira ndi wopulumutsidwa.
Hatei, maimanaw teh kamkonae dawk pha hanlah hnuk kâhnawn e tami lah awm awh hoeh, rungngang lah o awh nahanlah ka yuem e tami lah o awh.

< Ahebri 10 >