< Habakuku 1 >

1 Uthenga umene mneneri Habakuku analandira mʼmasomphenya.
Breme, ki ga je videl prerok Habakúk.
2 Kodi inu Yehova, ndidzakhala ndikukupemphani thandizo kwa nthawi yayitali motani, koma wosayankha? Kapena kufuwulira kwa inu kuti, “Chiwawa kuno!” koma wosatipulumutsa?
Oh Gospod, doklej bom klical in ne boš slišal! Celó klical k tebi o nasilju in ne boš rešil!
3 Chifukwa chiyani mukundionetsa zinthu zoyipa? Chifukwa chiyani mukundionetsa mavutowa? Ndikuona chiwonongeko ndi chiwawa; pali ndewu ndi kukangana kwambiri.
Zakaj mi kažeš krivičnost in mi povzročaš, da gledam gorje? Kajti plenjenje in nasilje sta pred menoj in tam so takšni, ki vzdigujejo spor in prepir.
4 Kotero malamulo anu atha mphamvu, ndipo chilungamo sichikugwira ntchito. Anthu oyipa aposa olungama, kotero apotoza chilungamo.
Zatorej je postava ohlapna in sodba nikoli ne gre naprej, kajti zlobni obdaja pravičnega, zato izhaja napačna sodba.
5 “Yangʼanani pakati pa mitundu ya anthu, ndipo penyetsetsani, ndipo muthedwe nazo nzeru. Pakuti ndidzachitadi zinthu pa nthawi yanu zimene inu simudzazikhulupirira, ngakhale wina atakufotokozerani.
Poglejte med pogane in preudarite in se silno čudite, kajti jaz bom naredil delo, delo v vaših dneh, ki ga ne boste verjeli, čeprav bi vam bilo povedano.
6 Pakuti taonani, Ine ndikuwutsa Ababuloni, anthu ankhanza ndiponso amphamvu, amene amapita pa dziko lonse lapansi kukalanda malo amene si awo.
Kajti glejte, vzdignil bom Kaldejce, ki so zagrenjen in nagel narod, ki bo korakal skozi širino dežele, da vzame v last prebivališča, ki niso njihova.
7 Iwowa ndi anthu ochititsa mantha, ndipo ndi owopsa; amadzipangira okha malamulo ndi kudzipezera okha ulemu.
Strašni so in grozni. Njihova sodba in njihovo dostojanstvo bo izšlo iz njih samih.
8 Akavalo awo ndi aliwiro kwambiri kupambana akambuku ndi owopsa kupambana mimbulu yolusa nthawi ya madzulo. Okwerapo awo akuthamanga molunjika; a pa akavalo awo ndi ochokera kutali, akuwuluka ngati chiwombankhanga chofuna kugwira nyama;
Tudi njihovi konji so hitrejši kakor leopardi in bolj kruti kakor večerni volkovi. Njihovi konjeniki se bodo razprostrli in njihovi konjeniki bodo prišli od daleč. Leteli bodo kakor orel, ki hiti, da žre.
9 onse akubwera atakonzekera zachiwawa. Gulu la ankhondo likubwera ngati mphepo ya mʼchipululu ndi kugwira akapolo ochuluka ngati mchenga.
Vsi bodo prišli zaradi nasilja. Njihovi obrazi bodo izpiti kakor vzhodnik in ujetništva bodo zbrali kakor peska.
10 Akunyoza mafumu ndiponso kuchitira chipongwe olamulira. Akupeputsa mizinda yonse yotetezedwa; akumanga mitumbira ndi kulanda mizindayo.
Norčevali se bodo iz kraljev in princi jim bodo prezir. Zasmehovali bodo vsako oporišče, kajti nagrmadili bodo prah in ga zavzeli.
11 Kenaka amasesa mofulumira ngati mphepo nʼkumangopitirirabe, anthu ochimwa, amene mphamvu zawo ndiye mulungu wawo.”
Potem se bo njegov um spremenil, šel bo mimo in se pohujšal, prištevajoč to svojo moč svojemu bogu.
12 Inu Yehova, kodi sindinu wachikhalire? Mulungu wanga, Woyera wanga, ife sitidzafa. Inu Yehova, munawasankha anthuwo kuti abweretse chiweruzo; Inu Thanthwe, munawayika iwowo kuti atilange.
Mar nisi ti od večnosti, oh Gospod, moj Bog, moj Sveti? Ne bomo umrli. Oh Gospod, za sodbo si jih odredil. Oh mogočni Bog, utrdil si jih za grajanje.
13 Maso anu ndi oyera kwambiri safuna kuona choyipa; Inu simulekerera cholakwa. Chifukwa chiyani nanga mukulekerera anthu ochita zachinyengowa? Chifukwa chiyani muli chete pamene anthu oyipa akuwononga anthu olungama kupambana iwowo?
Tvoje oči so preveč čiste, da bi gledal zlo in ne moreš gledati na krivičnost. Zakaj torej gledaš na tiste, ki postopajo zahrbtno in zadržuješ svoj jezik, ko zlobni požira človeka, ki je pravičnejši kakor on?
14 Mwasandutsa anthu kukhala ngati nsomba zamʼnyanja, ngati zolengedwa zamʼnyanja zimene zilibe wolamulira.
In ljudi delaš kakor ribe morja, kakor plazeče stvari, ki nimajo nobenega vladarja nad seboj?
15 Mdani wawo woyipa amakoka anthu onse ndi mbedza, amawakola mu ukonde wake, amawasonkhanitsa mu khoka lake; kotero iyeyo amakondwa ndi kusangalala.
Vse izmed njih privlečejo s trnkom, lovijo jih v svojo mrežo in jih zbirajo v svojo vlako; zato se veselijo in so veseli.
16 Choncho iye amaperekera nsembe ukonde wake ndiponso kufukizira lubani khoka lake, popeza ukonde wakewo ndiye umamubweretsera moyo wapamwamba ndipo amadya chakudya chabwino kwambiri.
Zato darujejo svoji mreži in svoji vrši zažigajo kadilo, ker po njima je njihov delež obilen in njihova hrana obilna.
17 Kodi iye azipitirabe kugwiritsa ntchito makoka akewo, kuwononga mitundu ya anthu mopanda chifundo?
Ali bodo zato praznili svojo mrežo in ne bodo nenehno prizanašali pobijanju narodov?

< Habakuku 1 >