< Genesis 5 >

1 Ndondomeko ya mibado ya Adamu ndi iyi: Pamene Mulungu analenga munthu, anamulenga mʼchifaniziro cha Mulungu.
Dies ist das Buch von des Menschen Geschlecht. Da Gott den Menschen schuf, machte er ihn nach dem Gleichnis Gottes
2 Iye analenga mwamuna ndi mkazi. Anawadalitsa ndipo anawatcha “Munthu.”
und schuf sie ein Männlein und Fräulein; und segnete sie und hieß ihren Namen Mensch zur Zeit, da sie geschaffen wurden.
3 Pamene Adamu anali ndi zaka 130, anabereka mwana wamwamuna wofanana naye ndipo anamutcha Seti.
Und Adam war hundertunddreißig Jahre alt und zeugete einen Sohn. der seinem Bilde ähnlich war, und hieß ihn Seth;
4 Atabadwa Seti, Adamu anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
und lebte danach achthundert Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
5 Zaka zonse za Adamu zinali 930 ndipo anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward neunhundertunddreißig Jahre, und starb.
6 Pamene Seti anali ndi zaka 105, anabereka Enosi.
Seth war hundertundfünf Jahre alt und zeugte Enos;
7 Atabadwa Enosi, Seti anakhala ndi moyo zaka zina 807 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
und lebte danach achthundertundsieben Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
8 Zaka zonse za Seti zinali 912 ndipo anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward neunhundertundzwölf Jahre, und starb.
9 Pamene Enosi anali ndi zaka 90, anabereka Kenani.
Enos war neunzig Jahre alt und zeugete Kenan;
10 Atabadwa Kenani, Enosi anakhala ndi moyo zaka zina 815 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
und lebte danach achthundertundfünfzehn Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
11 Zaka zonse za Enosi pamodzi zinali 905 ndipo anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward neunhundertundfünf Jahre, und starb.
12 Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli.
Kenan war siebenzig Jahre alt und zeugete Mahalaleel;
13 Atabadwa Mahalaleli, Kenani anakhala ndi moyo zaka zina 840 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
und lebte danach achthundertundvierzig Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
14 Zaka zonse za Kenani zinali 910, ndipo anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward neunhundertundzehn Jahre, und starb.
15 Pamene Mahalaleli anali ndi zaka 65, anabereka Yaredi.
Mahalaleel war fünfundsechzig Jahre alt und zeugete Jared;
16 Atabadwa Yaredi, Mahalaleli anakhala ndi moyo zaka zina 830 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
und lebte danach achthundertunddreißig Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
17 Zaka zonse za Mahalaleli zinali 895 ndipo anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward achthundertfünfundneunzig Jahre, und starb.
18 Pamene Yaredi anali ndi zaka 162, anabereka Enoki.
Jared war hundertundzweiundsechzig Jahre alt und zeugete Henoch;
19 Atabadwa Enoki, Yaredi anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
und lebte danach achthundert Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
20 Zaka zonse za Yaredi zinali 962 ndipo anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward neunhundertzweiundsechzig Jahre, und starb.
21 Pamene Enoki anali ndi zaka 65, anabereka Metusela.
Henoch war fünfundsechzig Jahre alt und zeugete Methusalah.
22 Atabadwa Metusela, Enoki anayenda ndi Mulungu zaka 300 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
Und nachdem er Methusalah gezeuget hatte, blieb er in einem göttlichen Leben dreihundert Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
23 Zaka zonse za Enoki zinali 365.
daß sein ganzes Alter ward dreihundertfünfundsechzig Jahre.
24 Enoki anayenda ndi Mulungu; ndipo iye sanaonekenso chifukwa Mulungu anamutenga.
Und dieweil er ein göttlich Leben führete, nahm ihn Gott hinweg, und ward nicht mehr gesehen.
25 Pamene Metusela anali ndi zaka 187, anabereka Lameki.
Methusalah war hundertsiebenundachtzig Jahre alt und zeugete Lamech;
26 Ndipo atabadwa Lameki, Metusela anakhala ndi moyo zaka zina 782 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
und lebte danach siebenhundertzweiundachtzig Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
27 Zaka zonse za Metusela zinali 969, ndipo anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward neunhundertneunundsechzig Jahre, und starb.
28 Pamene Lameki anali ndi zaka 182, anabereka mwana wamwamuna.
Lamech war hundertzweiundachtzig Jahre alt und zeugete einen Sohn
29 Ndipo anamutcha Nowa ndipo anati, “Iyeyu adzatipumulitsa ku ntchito zathu zolemetsazi, zolima nthaka imene Yehova anayitemberera.”
und hieß ihn Noah und sprach: Der wird uns trösten in unserer Mühe und Arbeit auf Erden, die der HERR verflucht hat.
30 Atabadwa Nowa, Lameki anakhala zaka zina 595 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
Danach lebte er fünfhundertfünfundneunzig Jahre und zeugete Söhne und Töchter;
31 Zaka zonse za Lameki zinali 777, ndipo kenaka anamwalira.
daß sein ganzes Alter ward siebenhundertsiebenundsiebenzig Jahre, und starb.
32 Pamene Nowa anali ndi zaka 500, anabereka Semu, Hamu ndi Yafeti.
Noah war fünfhundert Jahre alt und zeugete Sem, Ham und Japheth.

< Genesis 5 >