< Genesis 47 >

1 Yosefe anapita kukamuwuza Farao kuti, “Abambo anga, abale anga pamodzi ndi nkhosa, ngʼombe zawo, ndi antchito awo abwera kuchokera ku dziko la Kanaani ndipo tsopano ali ku Goseni.”
Amaiba: le, Yousefe da yolalali biyale gala amo Felouma oule asi. E da Felouma amane sia: i, “Na ada amola nolalali da Ga: ina: ne soge fisili guiguda: misi. Ilia lai gebo amola gagui liligi huluane oule misi. Ilia da wali Gousiene sogega esala.”
2 Iye anapita kwa Farao kuja ndi abale ake asanu, kukawaonetsa.
Amalalu, e da yolalali ili Felouma gousa: ma: ne oule misi.
3 Farao anafunsa abale akewo kuti, “Mumagwira ntchito yanji?” Iwo anamuyankha kuti, “Ife, bwana ndife oweta ziweto, monga ankachitira makolo athu.
Felou da ilima amane adole ba: i, “Dilia da adi hawa: hamosala: ?” Ilia da bu adole i, “Ninia da ninia aowalali defele, lai gebo fi ouligisu dunu esala.
4 Ife tabwera kudzakhala kuno kwa kanthawi chifukwa njala yafika poopsa ku Kanaani motero kuti kulibe msipu wodyetsera ziweto. Ndiye bwana tiloleni kuti tikhale ku Goseni.”
Ninia soge Ga: ina: ne amoga ha: i bagade ganebeba: le, ninia lai gebo da gisi hamedafa. Amaiba: le, ninia da amo soge guiguda: fimusa: misi. Ninia da Gousiene soge amo ganodini fimusa: , nini da dima ha: giwane edegesa.”
5 Farao anati kwa Yosefe, “Abambo ako ndi abale ako abwera kwa iwe.
Felou da Yousefema amane sia: i, “Dia eda amola diolalali ili da doaga: beba: le,
6 Dziko lonse la Igupto lili mʼdzanja lako. Uwakhazike abambo ako ndi abale ako mʼmalo achonde kwambiri. Akhale ku Goseni. Ndipo ngati ukudziwapo ena mwa iwo amene ali akatswiri pa kuweta ziweto, uwapatse udindo woyangʼanira ziweto zanga.”
Idibidi soge huluane da ilia soge. Gousiene soge da Idibidi soge bisili noga: i gala. Ilia da amogai fimu da defea. Amola ilia fi amo ganodini lai gebo ouligisu dunu ida: iwane esalea, defea, amo dunu da na lai gebo ouligima: ne sia: ma.”
7 Kenaka Yosefe anapita ndi abambo ake kwa Farao kukawaonetsa, ndipo Yakobo anadalitsa Faraoyo.
Amalalu, Yousefe da ea ada Ya: igobe amo Felouma gousa: musa: oule misi. Ya: igobe da Felouma amane sia: i, “Gode da di hahawane dogolegele fidimu da defea.”
8 Atatero, Farao anafunsa Yakobo kuti, “Muli ndi zaka zingati?”
Felou da Ya: igobema amane sia: i, “Dia lalelegele, ode habodayane esalabela: ?”
9 Yakobo anayankha kuti, “Zaka za maulendo anga zakwana 130. Zaka za moyo wanga ndi zowerengeka, komanso zakhala zaka za masautso. Zaka za moyo wanga sizingafanane ndi zaka za moyo wa makolo anga.”
Ya: igobe da bu adole i, “Na da wali ode 130 amoga udigili lalu. Na aowalali da ode bagohame hahawane lalu. Be na esalebe ode da bagahame, amola se nabasu galu.”
10 Atatha kumudalitsa Farao uja, Yakobo anatsanzika nʼkunyamuka.
Ya: igobe da Felouma Gode e hahawane dogolegele fidima: ne amola “asigibio”, sia: nanu, yolesili asi.
11 Choncho Yosefe anakhazika abambo ake aja ndi abale ake mʼdziko la Igupto. Iye anawapatsa dera la Ramesesi limene linali dziko lachonde kwambiri monga analamulira Farao.
Amalalu, Yousefe da fidibiba: le, ea ada amo yolalali ilia da Idibidi ganodini hahawane fi. Ilia da Felou ea sia: defele, moilai La: mesisi amo gadenene fi galu.
12 Yosefe anaperekanso chakudya kwa abambo ake, kwa abale ake ndi kwa onse a mʼnyumba ya abambo ake monga mwa chiwerengero cha ana awo.
Yousefe da ea ada amola yolalali ilima amola ea ada fi huluane amola mano fa: nodafa lalelegei, ilima ha: i manu i. Ha: Bagade
13 Njala inakula kwambiri motero kuti chakudya chinasowa mʼdziko lonse. Anthu a ku Igupto ndi ku Kanaani analefuka nayo njalayo.
Soge huluane amo ganodini da ha: bagade ba: i. Ha: i manu hamedafa ba: i. Idibidi dunu amola Ga: ina: ne dunu huluane da ha: iba: le, gasa hame ba: i.
14 Yosefe anasonkhanitsa ndalama zonse zimene anthu a mu Igupto ndi Kanaani ankapereka pogula tirigu, ndipo anabwera nazo ku nyumba kwa Farao.
Ilia da gagoma amola bali amo muniga lai. Amo muni Yousefe da Felou ea diasuga gaguli asi.
15 Anthu a ku Igupto ndi Kanaani ndalama zitawathera, Aigupto onse anabwera kwa Yosefe nati, “Tipatseni chakudya. Nanga tiferenji pamaso panu? Ndalama zathu zatha.”
Muni huluane Idibidi amola Ga: ina: ne amo ganodini ebelei ba: loba, Idibidi dunu da Yousefema misini, amane sia: i, “Ninima ha: i manu ima! Nini bogogia: sa: besa: le fidima! Ninia muni da ebelei dagoi!”
16 Ndipo Yosefe anawayankha kuti, “Bwerani ndi ziweto zanu ndipo tidzasinthana ndi chakudya poti mukuti ndalama zanu zatha.”
Yousefe da ilima bu adole i, “Dilia lai gebo oule misa. Dilia muni ebeleiba: le, na da dilia lai gebo bidi lale, ha: i manu amoga dabemu.”
17 Choncho anthu anabwera ndi ziweto zawo monga akavalo, nkhosa, mbuzi, ngʼombe ndi abulu ndipo Yosefe anawapatsa zakudya.
Amaiba: le, ilia da ilia lai gebo amo Yousefema oule misi amola e da ilia hosi, sibi, goudi, bulamagau, dougi, amo lale, ilima ha: i manu dabe i.
18 Chitatha chaka chimenecho, anthu anapitanso kwa Yosefe chaka chinacho nati, “Ife sitingakubisireni mbuye wathu kuti ndalama zathu zatithera ndipo ziweto zathu zili ndi inu, palibenso choti nʼkukupatsani mbuye wathu kupatula matupi athu ndi dziko lathu.
Amo ode da gidigili, eno ba: loba, ilia da Yousefema misini amane sia: i “Ninia muni da ebelei dagoi amola ninia lai gebo huluane di da lai dagoi. Amo ninia da dima hame wamolegemu. Wali dima imunu liligi da hame. Ninia da: i hodo amola ninia soge fawane diala.
19 Tiferenji ife ndi dziko lathu inu mukuona? Mutipatse chakudya ndipo tidzigulitsa ife ndi minda yathu yomwe. Ife tidzakhala akapolo a Farao. Tipatseni mbewuzo kuti tikhale ndi moyo tisafe ndipo dziko lisachite bwinja.”
Nini bogogia: sa: besa: le, nini fidima. Ninia soge da ha: i manu mae bugili, udigili dialumu da defea hame. Ninia da: i hodo amola ninia soge, bidi lama. Ninia da Felou ea udigili hawa: hamosu dunu esalumu amola e da ninia soge gagumu. Nini mae bogoma: ne ha: i manu ninima ima. Amola ninia sogega bu sagama: ne, hawa: bugima: ne ninima ima.”
20 Choncho Yosefe anamugulira Farao dziko lonse la Igupto. Aliyense mu Igupto anagulitsa munda wake chifukwa njala inakula kwambiri. Dziko lonse linasanduka la Farao,
Yousefe da soge huluane Idibidi ganodini amo bidi lale, Felouma i. Ha: da gasa bagadeba: le Idibidi dunu huluanedafa da ilia soge gagumu hamedeiwane ba: i. Soge huluane da Felou ea soge fawane ba: i.
21 ndipo Yosefe anawasandutsa anthu onse kukhala akapolo a Farao, kuchokera ku malire a mbali ina ya Igupto kukafika ku malire a mbali ina ya dzikolo.
Amola Yousefe da Idibidi dunu huluanedafa, amo udigili hawa: hamosu dunu hamoi.
22 Komabe, sanagule minda ya ansembe chifukwa Farao ankawapatsa thandizo lokwanira. Nʼchifukwa chake sanagulitse minda yawo.
Soge afae afae, e da hame bidi lai. Amo da gobele salasu dunu ilia soge. Felou da ili esaloma: ne, muni ilima i. Amaiba: le, ilia da ili soge hame bidi lai.
23 Yosefe anati kwa anthuwo, “Tsono poti ndakugulani inu ndi minda yanu, kugulira Farao. Nayi mbewu kuti mudzale mʼminda yanu.
Yousefe da dunu huluane ilima amane sia: i, “Ba: ma! Na da Felouma ima: ne, dilia da: i hodo amola dilia soge bidi lai dagoi. Amo hawa: dilia sogega bu sagamusa: , amo lama.
24 Koma podzakolola, mudzapereka gawo limodzi la magawo asanu aliwonse kwa Farao. Magawo anayi enawo adzakhala anu. Zina mudzasunge mbewu ndi zina mudzadye inuyo, mabanja anu ndi ana anu.”
Be ha: i manu faisu eso amoga dilia gagoma amola bali biyale fifili, afadafa Felouma ima. Eno hame i diala amo dili hawa: bugimusa: amola dilia amola dilia sosogo fi, amo moma: ne lama.”
25 Iwo anati, “Mwatipulumutsa potichitira zabwinozi, mbuye wathu, tsono tidzakhala akapolo a Farao.”
Ilia bu adole i, “Di da nini esalusu gaga: i dagoi. Di da nini noga: le fidi. Ninia Felou ea udigili hawa: hamosu dunu esalumu da defea.”
26 Choncho Yosefe anakhazikitsa lamulo limene lilipobe mpaka lero mʼdziko lonse la Igupto kuti limodzi la magawo asanu a zokolola ndi la Farao. Ndi minda ya ansembe yokha imene sinatengedwe kukhala ya Farao.
Amaiba: le, Yousefe da sema hamoi, amane, ‘Idibidi soge ganodini, ha: i manu fai huluane ilia da biyale fifili, amo afadafa Felouma ima: ne sia: i. Amo sema da wali diala. Be Felou da gobele salasu dunu ilia soge fawane hame lalegagui.
27 Tsono Aisraeli anakhazikika mʼdziko la Igupto ku chigawo cha Goseni. Kumeneko anapeza chuma ndipo anaberekana nachuluka kwambiri.
Isala: ili dunu da Idibidi ganodini Gousiene sogega esalu, mano bagohame lai, amola bagade gagui dunu ba: i.
28 Yakobo anakhala ku Igupto zaka 17 ndipo zaka za moyo wake zinali 147.
Ya: igobe da Idibidi soge ganodini ode 17 esalu. E da ode 147 amoga doaga: i.
29 Nthawi itayandikira yoti Israeli amwalire, anayitanitsa mwana wake Yosefe nati kwa iye, “Ngati ukundikondadi monga abambo ako, ika dzanja lako pansi pa ntchafu yanga ndipo ulonjeze kuti udzaonetsa kukoma mtima ndi kukhulupirika kwako kwa ine kuti sudzayika mtembo wanga kuno ku Igupto.
Ea bogomu eso gadenei ba: loba, e da eagofe Yousefe amo misa: ne sia: ne, ema amane sia: i, “Dia lobo amo na masele hagudu ligisima. Nama dafawanedafa ilegele sia: ma, amo di da na da: i hodo Idibidi soge ganodini hame uli dogomu.
30 Ine ndikagona pamodzi ndi makolo anga. Choncho ndikadzamwalira udzanditulutse mu Igupto muno ndipo ukayike mtembo wanga kumene anayikidwa makolo anga.” Yosefe anati, “Ndidzachita monga mwanenera.”
Na da na aowalali amo ilia uli dogosu amo gadenene dialumu hanai galebe. Na da: i hodo di gaguli asili, ilia uli dogoi sogebi amoga na uli dogoma.” Yousefe da bu adole i, “Na da dia sia: i defele hamomu.”
31 Yakobo anati, “Lumbira kwa ine.” Yosefe analumbira kwa iye, ndipo Israeli anapembedza Mulungu atatsamira ndodo yake.
Ya: igobe da amane sia: i, “Gode ba: ma: ne, di da dia sia: i defele hamoma: ne dafawane ilegele sia: ma!” Yousefe da amo dafawane ilegele sia: i, amola Ya: igobe da ea dia heda: su da: iya nodoi.

< Genesis 47 >