< Genesis 38 >

1 Pa nthawi imeneyi, Yuda anasiyana ndi abale ake napita kukakhala ndi munthu wina wa ku Adulamu wotchedwa Hira.
Hnin at vaengah tah Judah te a manuca rhoek taeng lamkah suntla tih Adullami hlang, a ming te Hirah taengah pah.
2 Kumeneko, Yuda anaona mwana wamkazi wa munthu wina wa Chikanaani wotchedwa Suwa. Anamukwatira nagona naye malo amodzi.
Te vaengah Judah loh Kanaan hoel nu, a ming ah Shua a hmuh hatah pahoi a loh tih a ih puei.
3 Iye anatenga pathupi, nabala mwana wamwamuna amene anamutcha Eri.
Te dongah pumrhih tih capa a cun vaengah a ming te Er a sak.
4 Anatenganso pathupi nabala mwana wa mwamuna ndipo anamutcha Onani.
Te phoeiah koep pumrhih tih ca a cun hatah a ming te Onan a sak.
5 Anaberekanso mwana wina wamwamuna ndipo anamutcha Sela. Ameneyu anabadwa Yuda ali ku Kezibi.
Te phoeiah a rhaep bal tih capa a cun hatah a ming te Shelah a sak. Tedae Shelah a cun vaengah Kezib ah om.
6 Yuda anamupezera mkazi mwana wake woyamba uja Eri, ndipo dzina la mkaziyo linali Tamara.
Te phoeiah Judah loh a caming Er ham yuu a loh pah tih anih ming tahTamar ni.
7 Koma ntchito zoyipa za Eri, mwana wachisamba wa Yuda zinayipira Yehova. Choncho Mulungu anamulanga ndi imfa.
Tedae Judah kah a caming Er tah BOEIPA kah mikhmuh ah boethae la a om dongah anih te BOEIPA loh a duek sak.
8 Pamenepo Yuda anati kwa Onani, “Kwatira mkazi wamasiye wa mʼbale wako. Ulowe chokolo kuti mʼbale wako akhale ndi mwana.”
Te dongah Judah loh Onan la, “Na maya yuu taengah kun lamtah anih te yucanah. Te phoeiah na maya ham a tii a ngan thoh pah,” a ti nah.
9 Koma Onani anadziwa kuti mwanayo sadzakhala wake. Choncho nthawi zonse pamene amagona naye mkaziyo, ankatayira umuna pansi kuti asamuberekere mwana mʼbale wake.
Tedae a tii a ngan te amah ham om hae mahpawh tila Onan loh a ming dongah, a maya yurho taengah a ih vaengah khaw diklai ah vik a san tih a maya ham tiingan khueh pah pawh.
10 Zimene ankachitazi zinayipira Yehova. Choncho anamulanganso ndi imfa.
Anih kah a saii te BOEIPA mikhmuh ah a lolh bal dongah anih khaw BOEIPA loh a duek sak.
11 Kenaka Yuda anati kwa mpongozi wake Tamara, “Bwererani ku nyumba ya abambo anu ndi kukhala kumeneko ngati wamasiye mpaka mwana wanga Sela atakula.” Ananena izi chifukwa ankaopa kuti Sela angafenso ngati abale ake aja. Choncho Tamara anapita kukakhala ku nyumba ya abambo ake.
Te vaengah Shelah khaw a maya rhoi bangla duek ve a ti. Te dongah Judah loh a langa Tamar la, “Ka capa Shelah a pantai hil tah na pa im ah nuhmai la khosa mai,” a ti nah. Te dongah Tamar khaw cet tih a napa im ah kho a sak.
12 Patapita nthawi yayitali, Batishua, mkazi wa Yuda anamwalira. Yuda atatha kulira maliro a mkazi wake, anapita, iyeyu pamodzi ndi bwenzi lake Hira, Mwadulamu uja, ku Timna kumene ankameta nkhosa zawo.
Tedae kum a yet phoeiah tah Judah yuu Shua nu te duek. Te dongah Judah khaw hal tih a tu mul aka vo neh a hui Adullami Hirah taengah Timnah la cet.
13 Tamara atamva kuti apongozi ake akupita ku Timna kukameta nkhosa,
Te dongah, “Tu mul vok ham Timnah la na marhang cet hang ke,” a ti na tih Tamar taengla a puen pah.
14 iye anavula zovala zake za umasiye, nadziphimba nkhope ndi nsalu kuti asadziwike, ndipo anakhala pansi pa chipata cha ku Enaimu popita ku Timna. Tamara anachita izi chifukwa anaona kuti ngakhale Selayo anali atakula tsopano, iye sanaperekedwe kuti amulowe chokolo.
Te vaengah Shelah khaw ham coeng dae anih yuu la n'khueh moenih tila Tamar loh a hmuh dongah amah dongkah nuhmai himbai te a dul. Te phoeiah hnii a yil, muei a thuh tih Timnah long kah Enaim thohka ah ngol.
15 Yuda atamuona anangomuyesa mkazi wadama chabe, chifukwa anadziphimba nkhope.
Tedae anih te Judah loh a hmuh vaengah a hmai a dah dongah pumyoi ni tila a poek.
16 Tsono anapita kwa mkaziyo pamphepete pa msewu paja nati, “Tabwera ndigone nawe.” Apa Yuda sankadziwa kuti mkazi uja anali mpongozi wake. Ndiye mkazi uja anamufunsa Yuda nati, “Mudzandipatsa chiyani kuti ndigone nanu?”
Anih te amah langa la a ming pawt dongah long taengla anih taengah pah tih, “Halo, nang taengah ka ip ni ne,” a ti nah hatah, “Kai taengah na kun te kai ham balae na khueh eh?,” a ti nah.
17 Iye anati, “Ndidzakutumizira kamwana kambuzi ka mʼkhola mwanga.” Mkaziyo anayankha kuti, “Chabwino, ndavomera, koma mungandipatse chikole mpaka mutanditumizira mbuziyo?”
Te vaengah Judah loh, “Kamah loh boiva khuikah maae ca kan pat bit ni,” a ti nah. Tedae Tamar loh, “Nan pat hlanah hnohol han khueh dae,” a ti nah.
18 Iye anati, “Ndikupatse chikole chanji?” Mkaziyo anayankha, “Mundipatse mphete yanuyo, chingwe chanucho pamodzi ndi ndodo imene ili mʼdzanja lanulo.” Choncho anazipereka kwa iye nagona naye ndipo anatenga pathupi.
Te dongah, “Hnohol te balae nang taengah kan paek eh?,” a ti nah. Te vaengah, “Na kutbuen mai khaw, hamnak khaw, na kut kah conghol mai te khaw,” a ti nah. Te dongah anih te a paek tih a kun thil dongah Judah loh Tamar a vawn sak.
19 Kenaka Tamara anachoka, navula nsalu anadziphimba nayo ija, navalanso zovala zake za umasiye zija.
Te phoeiah thoo tih, cet tih a pum dongkah hnii te a dul phoeiah nuhmai himbai tloep a bai.
20 Tsono Yuda anatuma bwenzi lake Mwadulamu uja ndi kamwana kambuzi kaja kuti akapereke kwa mkazi wadama uja, ndi kuti akatero amubwezere chikole chake chija. Koma atafika sanamupezepo.
Te dongah huta kut kah hnohol te tlan ham Judah loh a hui Adullami hoel kut ah maae ca te a pat van hatah rhawp hmu pawh.
21 Anawafunsa anthu a komweko, “Kodi mkazi wadama uja amene ankakhala pambali pa msewu wa ku Enaimu, ali kuti?” Iwo anayankha, “Sipanakhalepo mkazi wa dama aliyense pano.”
Te dongah te hmuen kah hlang rhoek te a dawt “Enaim long taengkah hlanghalh te melae?,” a ti nah vaengah he rhoek ah hlanghalh om pawh,” a ti na uh.
22 Choncho anabwerera kwa Yuda nati, “Sindinamupeze mkazi uja. Kuwonjeza apo, anthu a kumeneko amati, ‘Sipanakhalepo mkazi wadama pano.’”
Te dongah Judah taengla koep bal tih, “Anih te ka hmuh moenih. Te phoeiah he hmuen kah hlang rhoek long khaw, 'He rhoek ah hlanghalh a om moenih,’ a ti uh,” a ti nah.
23 Pamenepo Yuda anati, “Mulekeni atenge zinthuzo zikhale zake, kuopa kuti anthu angatiseke. Ine sindinalakwe, ndinamutumizira kamwana kambuzika, koma simunamupeze.”
Te dongah Judah loh, “Amah neh amah te khoem uh saeh, nueihbu la n'om uh ve. Maae ca n'thak he khaw anih te na hmuh voel pawt tih he,” a ti nah.
24 Patapita miyezi itatu, Yuda anawuzidwa kuti, “Mpongozi wanu Tamara anachita zadama, ndipo zotsatira zake nʼzakuti ali ndi pathupi.” Yuda anati, “Kamutulutseni ndipo mukamutenthe kuti afe!”
Tedae hla thum tluk a lo vaengah Judah taengah,” Nang langa Tamar te cukhalh tih pumyoihnah neh vawn lah ko te,” a ti nah tih a puen pa uh hatah Judah loh, “Anih te khuen uh lamtah hoeh,” a ti nah.
25 Akumutulutsa, iye anatuma mawu kwa apongozi ake. Anati, “Ndili ndi pathupi pa munthu amene ndi mwini wake wa zinthu izi. Taziyangʼanitsitsani, kodi mwini wa khoza, chingwe ndi ndodo yoyenderayi ndi yani?”
Anih te a mawt uh van hatah, “He rhoek he u hlang kah nim. Kai khaw tekah hlang hut la ka vawn dongah hekah kutnoek, hamnak neh conghol, ukah nim tila hmat lah saeh,” a ti nah tih a marhang taengla Tamar loh a pat.
26 Yuda anazizindikira zinthuzo ndipo anati, “Uyu ndi wolungama kuposa ine, chifukwa sindinamupereke kwa mwana wanga Sela.” Ndipo Yuda sanagone nayenso.
Tedae Judah loh a hmat vaengah, “Ka capa Shelah te anih ka paek pawt dongah te kai lakah anih tang coeng,” a ti. Te dongah anih ming ham koep khoep voel pawh.
27 Pamene Tamara nthawi inamukwanira yoti abeleke, mʼmimbamo munali mapasa.
Tedae ca-om tue vaengah tah a bung khuiah caphae rhoi la tarha om.
28 Pamene ankabereka, mmodzi wa iwo anatulutsa dzanja lake. Choncho mzamba anatenga kawulusi kofiira nakamangirira pa mkono pa mwanayo nati, “Uyu ndiye anayamba kubadwa.”
Te dongah camoe a om vaengah kut pakhat te han thawt dongah ca-om loh a tuuk tih, a kut dongah a lingdik a cin pah tih, “Lamhma la om coeng he,” a ti.
29 Koma pamene anabweza mkonowo, mʼbale wake anabadwa ndipo mzamba anati, “Wachita kudziphotcholera wekha njira chonchi!” Ndipo anamutcha Perezi.
Tedae a kut vik a yueh tih a mana lat ha thoeng dongah, “Namah loh a puut Metlamlae nam va,” a ti nah dongah a ming te Perez a sak.
30 Pambuyo pake mʼbale wake amene anali ndi ulusi wofiira pa mkono wake uja anabadwa ndipo anapatsidwa dzina lakuti Zera.
Te phoeiah a kut dongah a lingdik aka om a maya te ha pawk tih a ming te Zerah a sak.

< Genesis 38 >