< Genesis 35 >

1 Tsono Mulungu anati kwa Yakobo, “Nyamuka uchoke kuno kupita ku Beteli. Kumeneko ukamange guwa lansembe la Mulungu amene anadza kwa iwe pamene umathawa Esau, mʼbale wako.”
Gode da Ya: igobema amane sia: i, “Di da Bedele sogega hedolo asili, esaloma. Amoga Nama oloda hamoma. Na da Gode amo di da Isoba: le hobealoba, Na da dima misi.”
2 Choncho Yakobo anawuza a pa banja pake ndi onse amene anali naye kuti, “Chotsani milungu yachilendo imene muli nayo, ndipo mudziyeretse nokha ndi kusintha zovala zanu.
Amaiba: le, Ya: igobe da ea sosogo fi amola dunu huluane ema gilisi, ilima amane sia: i, “Ga loboga hamoi ‘gode’ liligi dilia gagui amo huluane fadegale fasima. Dilia nigima: dodofelalu, abula gaheabolo salima.
3 Tiyeni tinyamuke kuchoka kuno kupita ku Beteli. Kumeneko ndikamumangira guwa lansembe Mulungu amene anandithandiza pa nthawi za masautso anga, komanso amene wakhala nane mʼmayendedwe anga onse.”
Ninia da amo soge yolesili, Bedele moilaiga masunu. Amoga na da Gode amo da na se nabasu ganodini fidi, amola na lalebe soge huluane E da gilisili lala, amoga na da oloda hamomu.
4 Choncho anamupatsa Yakobo milungu yachilendo yonse imene anali nayo pamodzi ndi ndolo. Iye anazikwirira pansi pa mtengo wa thundu ku Sekemu.
Amaiba: le, ilia da loboga hamoi ‘gode’ liligi amola gegagulu ilia ge ganodini sali, amo huluane duga: le, Ya: igobema i. Ya: igobe da amo liligi huluane ‘ouge’ ifa Siegeme soge ganodini amo haguduga uli dogone sali.
5 Pamenepo ananyamuka, ndipo mtima woopa Mulungu unagwera anthu onse a mʼmizinda yozungulira, kotero kuti palibe aliyense amene anatsatira banja la Yakobo.
Amalalu, ilia da logoga asili, moilai dunu huluane gadenene esalu da beda: i bagade ba: i. Ilia da beda: iba: le, Ya: igobe ea fi hame se bobogei.
6 Yakobo ndi anthu onse anali naye aja anafika ku Luzi (ku Beteli) mu dziko la Kanaani.
Ya: igobe amola ea fi huluane da Luse (wali ea dio da Bedele), Ga: ina: ne soge ganodini amoga doaga: i.
7 Kumeneko anamanga guwa lansembe nalitcha Eli Beteli, chifukwa kunali kumeneko kumene Mulungu anadziwulula yekha kwa Yakobo pamene ankathawa mʼbale wake.
Amoga e da oloda hamone amola amo soge dio eno asuli amo Ele Bedele. Bai amoga e da ea olaba: le hobeale ahoanoba, Gode da ema misi.
8 Debora mlezi wa Rakele anamwalira komweko nayikidwa mʼmanda pansi pa mtengo wa thundu cha kumunsi kwa Beteli. Choncho panatchedwa Aloni-Bakuti (mtengo wamaliro).
Lebega ea hawa: hamosu uda amo Debola da amoga bogoi. Ea da: i hodo ilia da ‘ouge’ ifa Bedele sogebi amoga ga (south) dialu, amo hagudu uli dogone sali. Amaiba: le, amo ifaga ilia da ‘Disu Ouge Ifa’ dio asuli.
9 Yakobo atabwera kuchokera ku Padanaramu, Mulungu anabweranso kwa iye namudalitsa.
Ya: igobe da Mesoubouda: imia yolesili, bu Ga: ina: ne sogega bu misini, Gode da ema bu misini, ema hahawane dogolegele fidima: ne sia: i.
10 Mulungu anati kwa iye, “Dzina lako ndiwe Yakobo, koma sudzatchedwanso Yakobo; koma udzatchedwa Israeli.” Choncho anamutcha iye Israeli.
Gode da ema amane sia: i, “Dia dio da Ya: igobe, be amo fa: no dia dio da Isala: ili.” Amaiba: le, Gode da ema Isala: ili dio asuli.
11 Ndipo Mulungu anati kwa iye, “Ine ndine Mulungu Wamphamvuzonse; berekanani ndi kuchulukana. Mtundu wa anthu, inde, mitundu yambiri ya anthu idzatuluka mwa iwe, ndipo ena mwa zidzukulu zako adzakhala mafumu.
Amola Gode da ema amane sia: i, “Na da Gode Bagadedafa! Di mano bagohame lalelegema! Digaga fi da fifi asi gala bagohame ba: mu, amola di da hina bagade dunu ilima aowa ba: mu.
12 Dziko limene ndinapereka kwa Abrahamu ndi Isake ndiliperekanso kwa iwe. Lidzakhala lako ndi la zidzukulu zako.”
Soge Na da A: ibalaha: me amola Aisage elama i dagoi, amo na da dima imunu. Amola fa: no digaga fibi ilima imunu.”
13 Kenaka Mulungu anamusiya Yakobo.
Amalalu, Gode da yolesili asi.
14 Yakobo anayika mwala wachikumbutso pa malo pamene Mulungu anayankhula naye paja. Iye anathirapo nsembe yachakumwa ndi yamafuta.
Amogawi, Gode da amo sogebiga ema sia: musa: misiba: le, Ya: igobe da wanonesisu gele bugili, amo Godema modale ligiagama: ne, amo da: iya waini amola olife susuligi sogadigi.
15 Yakobo anawatcha malo amene Mulungu anayankhula naye aja kuti Beteli.
E da amo sogebiga dio asuli, amo Bedele.
16 Kenaka anachoka ku Beteli. Koma ali pafupi kufika ku Efurata nthawi yakuti Rakele aone mwana inakwana. Iye anavutika pobereka.
Ya: igobe amola ea sosogo fi da Bedele yolesili, logoga ahoanoba, Efala: de amoga mae doaga: le, La: isele da mano lamusa: se nabi. E da mano lalelegemu logebeba: le, gasa bagade ba: i.
17 Akanali chivutikire choncho, mzamba anamulimbikitsa nati, “Usaope pakuti ubala mwana wina wamwamuna.”
Mano lamusa: se bagade nabaloba, mano lasu fidisu uda da ema amane sia: i, “La: isele! Mae beda: ma! Dunu mano da lalelegei dagoi.
18 Tsono pamene Rakele ankapuma wefuwefu (popeza ankamwalira) iye anatcha mwana uja kuti Beni-Oni. Koma abambo ake anamutcha kuti Benjamini.
Be La: isele da bogolalu, amola mifo laha da gadenene dagoloba, ea manoma dio asuli amo Benoni. Be Ya: igobe da ema Bediamini dio asuli.
19 Choncho Rakele anamwalira ndipo anayikidwa pa njira yopita ku Efurata (Kumeneko ndiye ku Betelehemu).
La: isele da bogoi. Ilia da ea da: i hodo Efala: de moilai logo ahoasu dafulili uli dogoi. Amo moilai ea dio wali da Bedeleheme.
20 Pa manda ake, Yakobo anayimika mwala wachikumbutso wa pa manda ndipo ulipobe mpaka lero.
Ya: igobe da dawa: ma: ne gele wanonesisu amoga bugi, amola wali amo da La: isele ea uli dogoi amoga dawa: ma: ne diala.
21 Israeli (Yakobo) anasunthanso nakamanga tenti yake kupitirira nsanja ya Ederi.
Ya: igobe da asili, diasu gagagula heda: i, ea dio Ede amo baligili, ea abula diasu gagui.
22 Israeli akanali mʼderali, Rubeni anapita nakagonana ndi Biliha, mdzakazi wa abambo ake. Yakobo uja anazimva zimenezi. Yakobo anali ndi ana aamuna khumi ndi awiri:
Ya: igobe da amo soge ganodini esaloba, ea mano Liubene da misini, Ya: igobe ea gidesedagi uda amo Biliha ema gilisili golai. Ya: igobe da amo hou nababeba: le, mi hanai galu. Ya: igobe ea dunu mano da fagoyale galu.
23 Ana a Leya ndi awa: Rubeni anali mwana woyamba wa Yakobo, Simeoni, Levi, Yuda, Isakara, ndi Zebuloni.
Lia ea dunu manolali da Liubene (Ya: igobe ea magobo mano) Simione, Lifai, Yuda, Isiga amola Sebiulane.
24 Ana a Rakele ndi awa: Yosefe ndi Benjamini.
La: isele ea dunu manola da Yousefe amola Bediamini.
25 Ana a Biliha, wantchito wa Rakele ndi awa: Dani ndi Nafutali.
La: isele ea hawa: hamosu uda Biliha amo ea dunu manola da Da: ne amola Na: badalai.
26 Ana a Zilipa wantchito wa Leya ndi awa: Gadi ndi Aseri. Awa ndiwo ana a Yakobo amene anabadwira ku Padanaramu.
Lia ea hawa: hamosu uda Siliba amo ea dunu manola da Ga: de amola A: sie. Amo dunu mano ilia da Mesoubouda: imia sogega lalelegei.
27 Yakobo anafika ku mudzi kwa abambo ake Isake ku Mamre, (kumene kunkatchedwa ku Kiriyati-Ariba kapenanso Hebroni) kumene Abrahamu ndi Isake anakhalako kale.
Aisage da Ma: melei amo Hibalone moilaiga gadenene esalu. Amoga Ya: igobe da asi.
28 Isake anakhala ndi moyo zaka 180.
Aisage da lalelegele, ode 180 esalu.
29 Anamwalira ali wokalamba kwambiri ndipo anakakhala ndi anthu a mtundu wake. Ndipo ana ake Esau ndi Yakobo anamuyika mʼmanda.
E da amo ode bagohame lai dagoloba, bogoi. Ea mano Iso amola Ya: igobe da ea da: i hodo uli dogone sali.

< Genesis 35 >