< Genesis 24 >
1 Tsopano Abrahamu anali atakalamba kwambiri, ndipo Yehova anamudalitsa mu zonse anachita.
and Abraham be old to come (in): advanced in/on/with day: year and LORD to bless [obj] Abraham in/on/with all
2 Tsiku lina Abrahamu anawuza wantchito wake wamkulu amene ankayangʼanira zonse anali nazo, kuti “Ika dzanja lako pansi pa ntchafu yanga.
and to say Abraham to(wards) servant/slave his old house: household his [the] to rule in/on/with all which to/for him to set: put please hand: swear your underneath: swear thigh my
3 Ndikufuna kuti ulumbire pamaso pa Yehova, Mulungu wakumwamba ndi dziko lapansi, kuti sudzamupezera mwana wanga mkazi pakati pa atsikana Achikanaani a kuno kumene ndikukhala,
and to swear you in/on/with LORD God [the] heaven and God [the] land: country/planet which not to take: take woman: wife to/for son: child my from daughter [the] Canaanite which I to dwell in/on/with entrails: among his
4 koma kuti udzapita ku dziko la kwathu ndi kukamupezera mkazi mwana wanga Isake pakati pa abale anga.”
for to(wards) land: country/planet my and to(wards) relatives my to go: went and to take: take woman: wife to/for son: child my to/for Isaac
5 Wantchito uja anafunsa kuti, “Nanga atakhala kuti mkaziyo sakufuna kubwera nane kuno? Kodi ine ndingadzatenge mwana wanu ndi kubwerera naye ku dziko kumene munachokera?”
and to say to(wards) him [the] servant/slave perhaps not be willing [the] woman to/for to go: follow after me to(wards) [the] land: country/planet [the] this to return: return to return: return [obj] son: child your to(wards) [the] land: country/planet which to come out: come from there
6 Abrahamu anati, “Uwonetsetse kuti usadzabwerere naye mwana wanga kumeneko.
and to say to(wards) him Abraham to keep: careful to/for you lest to return: return [obj] son: child my there [to]
7 Yehova Mulungu wakumwamba amene ananditenga kwa makolo anga nanditulutsa mʼdziko lobadwira, ameneyo anayankhula nane molumbira kuti, ‘Kwa zidzukulu zako ndidzapereka dziko ili.’ Iyeyu adzatumiza mngelo wake kuti akutsogolere kumeneko kukapezera mwana wanga mkazi.
LORD God [the] heaven which to take: take me from house: household father my and from land: country/planet relatives my and which to speak: speak to/for me and which to swear to/for me to/for to say to/for seed: children your to give: give [obj] [the] land: country/planet [the] this he/she/it to send: depart messenger: angel his to/for face: before your and to take: take woman: wife to/for son: child my from there
8 Ngati mkaziyo adzakana kubwerera nawe ndiye kuti udzakhala womasuka ku lumbiro langa. Koma usadzamutenge mwana wanga ndi kubwerera naye kumeneko.”
and if not be willing [the] woman to/for to go: follow after you and to clear from oath my this except [obj] son: child my not to return: return there [to]
9 Choncho wantchitoyo anayika dzanja lake pansi pa ntchafu ya mbuye wake Abrahamu nalumbira kwa iye kuti adzachitadi monga mwa mawu a Abrahamu.
and to set: put [the] servant/slave [obj] hand: swear his underneath: swear thigh Abraham lord his and to swear to/for him upon [the] word: thing [the] this
10 Tsono wantchito uja anatengapo ngamira khumi mwa ngamira za mbuye wake pamodzi ndi zinthu zabwino za mitundumitundu. Ndipo ananyamuka kupita ku mzinda wa Nahori, mʼdziko la Mesopotamiya.
and to take: take [the] servant/slave ten camel from camel lord his and to go: went and all goodness lord his in/on/with hand: to his and to arise: rise and to go: went to(wards) Mesopotamia Mesopotamia to(wards) city Nahor
11 Atafika, anagwaditsa pansi ngamira zija pafupi ndi chitsime chimene chinali kunja kwa mzinda uja. Awa anali madzulo ndithu, nthawi imene amayi amapita kukatunga madzi.
and to bless [the] camel from outside to/for city to(wards) well [the] water to/for time evening to/for time to come out: come [the] to draw
12 Ndipo wantchito uja anapemphera nati, “Haa, Yehova, Mulungu wa mbuye wanga Abrahamu, mulole kuti zinthu zindiyendere ine lero, ndipo muonetseni mbuye wanga Abrahamu kukoma mtima kwanu kosasinthika.
and to say LORD God lord my Abraham to meet please to/for face of my [the] day and to make: do kindness with lord my Abraham
13 Taonani ndayima pambali pa chitsimechi, ndipo atsikana a mu mzindawu akubwera kudzatunga madzi.
behold I to stand upon spring [the] water and daughter human [the] city to come out: come to/for to draw water
14 Ine ndipempha mtsikana wina kuti, ‘Chonde tula mtsuko wako kuti ndimweko madzi.’ Tsono iye akayankha kuti ‘Imwani,’ ndipo ndidzapatsanso ngamira zanu madziwo, ameneyo akhale mkazi amene mwasankhira mtumiki wanu Isake.” Zimenezi zikachitika, ndidzadziwa kuti mwaonetsadi kukoma mtima kwanu kosasinthika kwa mbuye wanga.
and to be [the] maiden which to say to(wards) her to stretch please jar your and to drink and to say to drink and also camel your to water: watering [obj] her to rebuke to/for servant/slave your to/for Isaac and in/on/with her to know for to make: do kindness with lord my
15 Asanatsirize kupemphera, anangoona Rebeka watulukira atasenza mtsuko wake pa phewa. Iyeyu anali mwana wa Betueli mwana wa Milika, mkazi wa Nahori mʼbale wake wa Abrahamu.
and to be he/she/it before to end: finish to/for to speak: speak and behold Rebekah to come out: come which to beget to/for Bethuel son: child Milcah woman: wife Nahor brother: male-sibling Abraham and jar her upon shoulder her
16 Mtsikanayo anali wokongola kwambiri, namwali amene sanadziwe mwamuna. Iye anatsikira ku chitsime nadzaza mtsuko nakweranso ku mtunda.
and [the] maiden pleasant appearance much virgin and man not to know her and to go down [the] spring [to] and to fill jar her and to ascend: rise
17 Wantchito uja anathamanga kukakumana naye nati, “Chonde patseko madzi pangʼono a mu mtsuko wakowo kuti ndimwe.”
and to run: run [the] servant/slave to/for to encounter: meet her and to say to swallow me please little water from jar your
18 Mtsikanayo anati, “Imwani mbuye wanga.” Ndipo mofulumira anatsitsa mtsuko uja nawuyika mʼmanja ndi kumupatsa kuti amwe.
and to say to drink lord my and to hasten and to go down jar her upon hand her and to water: drink him
19 Atatha kupereka madzi akumwa kwa mlendo uja, mtsikanayo anati, “Ndikatungiranso ngamira madzi kuti zimwe mpaka zitakwana.”
and to end: finish to/for to water: drink him and to say also to/for camel your to draw till if: until to end: finish to/for to drink
20 Choncho anafulumira kukhuthula madzi a mu mtsuko aja momwera ziweto, nathamanga kubwerera ku chitsime kukatunga madzi ena, ndipo anatunga okwanira ngamira zake zonse.
and to hasten and to uncover jar her to(wards) [the] trough and to run: run still to(wards) [the] well to/for to draw and to draw to/for all camel his
21 Modekha, munthu uja anayangʼanitsitsa kwambiri mtsikana uja kuti adziwedi ngati Yehova anamutsogolera pa ulendo wake uja kapena ayi.
and [the] man to gaze to/for her be quiet to/for to know to prosper LORD way: journey his if not
22 Ngamira zija zitatha kumwa, mlendo uja anatulutsa chipini chagolide cholemera theka la sekeli ndi zibangiri zagolide ziwiri zolemera masekeli 100.
and to be like/as as which to end: finish [the] camel to/for to drink and to take: take [the] man ring gold bekah weight his and two bracelet upon hand: swear her ten gold weight their
23 Kenaka anafunsa namwaliyo kuti, “Chonde tandiwuza, kodi ndiwe mwana wa yani? Ndipo kodi malo alipo kwanu woti ife nʼkugona?”
and to say daughter who? you(f. s.) to tell please to/for me there house: home father your place to/for us to/for to lodge
24 Anamuyankha kuti, “Ine ndine mwana wa Betueli, mwana amene Milika anaberekera Nahori.”
and to say to(wards) him daughter Bethuel I son: child Milcah which to beget to/for Nahor
25 Ndipo anapitiriza kunena kuti, “Chakudya chodyetsa nyamazi chilipo kwathu ndipo malo woti mugone aliponso.”
and to say to(wards) him also straw also fodder many with us also place to/for to lodge
26 Kenaka munthuyo anawerama pansi napembedza Yehova,
and to bow [the] man and to bow to/for LORD
27 nati, “Alemekezeke Yehova, Mulungu wa mbuye wanga Abrahamu, amene waonetsa kukoma mtima kwake kosasintha ndi kukhulupirika kwake kwa mbuye wanga. Yehova wanditsogolera pa ulendo wanga mpaka ndafika ku nyumba kwa abale ake a mbuye wanga.”
and to say to bless LORD God lord my Abraham which not to leave: forsake kindness his and truth: faithful his from from with lord my I in/on/with way: journey to lead me LORD house: home brother: male-relative lord my
28 Mtsikana uja anathamanga nakafotokozera zimenezi anthu a kwa amayi ake.
and to run: run [the] maiden and to tell to/for house: household mother her like/as word: thing [the] these
29 Tsono Rebeka anali ndi mlongo wake dzina lake Labani.
and to/for Rebekah brother: male-sibling and name his Laban and to run: run Laban to(wards) [the] man [the] outside [to] to(wards) [the] spring
30 Iyeyu atangoona chipini pa mphuno ndi zibangiri pa mikono ya mlongo wake komanso kumva zimene mlendo uja ananena kwa Rebekayo, anathamangira kwa mlendo uja, ndipo anamupeza atangoyima ndi ngamira zake pafupi ndi chitsime.
and to be like/as to see: see [obj] [the] ring and [obj] [the] bracelet upon hand sister his and like/as to hear: hear he [obj] word Rebekah sister his to/for to say thus to speak: speak to(wards) me [the] man and to come (in): come to(wards) [the] man and behold to stand: stand upon [the] camel upon [the] spring
31 Iye anati, “Tiyeni kwathu, ndinu munthu amene Yehova wamudalitsa. Bwanji mwangoyimirira panja pano? Ine ndakukonzerani malo ogona inu ndi ngamira zanu.”
and to say to come (in): come to bless LORD to/for what? to stand: stand in/on/with outside and I to turn [the] house: home and place to/for camel
32 Choncho munthu uja analowa mʼnyumba. Labani anatsitsa katundu anali pa ngamira uja. Kenaka anazipatsa ngamira zija chakudya, ndiponso anapereka madzi wosamba mapazi kwa mlendo uja ndi anthu ena onse.
and to come (in): come [the] man [the] house: home [to] and to open [the] camel and to give: give straw and fodder to/for camel and water to/for to wash: wash foot his and foot [the] human which with him
33 Chakudya chitabwera mlendo uja anati, “Sindidya mpaka nditakuwuzani zimene ndadzera kuno.” Labani anati, “Yankhulani.”
(and to set: put *Q(K)*) to/for face: before his to/for to eat and to say not to eat till if: surely no to speak: speak word: speaking my and to say to speak: speak
34 Motero iye anati, “Ine ndine wantchito wa Abrahamu.
and to say servant/slave Abraham I
35 Yehova wadalitsa mbuye wanga kwambiri, ndiponso walemera. Wamupatsa nkhosa ndi ngʼombe, siliva ndi golide, antchito aamuna ndi antchito aakazi, komanso ngamira ndi abulu.
and LORD to bless [obj] lord my much and to magnify and to give: give to/for him flock and cattle and silver: money and gold and servant/slave and maidservant and camel and donkey
36 Sara, mkazi wa mbuye wanga anamubalira iye mwana wamwamuna ngakhale kuti Sarayo anali wokalamba. Tsono mbuye wanga wamupatsa mwanayo chuma chonse.
and to beget Sarah woman: wife lord my son: child to/for lord my after old age her and to give: give to/for him [obj] all which to/for him
37 Tsono mbuye wanga anandilumbiritsa kuti ndisunge mawu ake akuti, ‘Usadzamupezere mwana wanga mkazi kuchokera mwa atsikana a dziko lino la Kanaani,
and to swear me lord my to/for to say not (to take: take *LA(bh)*) woman: wife to/for son: child my from daughter [the] Canaanite which I to dwell in/on/with land: country/planet his
38 koma upite ku banja la abambo anga ndi kwa abale anga kuti ukamupezere mkazi mwana wanga.’”
if: surely yes not to(wards) house: household father my to go: went and to(wards) family my and to take: take woman: wife to/for son: child my
39 “Ndipo ine ndinati kwa mbuye wanga, ‘Nanga mkaziyo akakapanda kubwera nane pamodzi?’
and to say to(wards) lord my perhaps not to go: follow [the] woman after me
40 “Iye anayankha, ‘Yehova amene ndakhala ndikumumvera nthawi zonse, adzatumiza mngelo wake kuti akuperekeze ndipo adzakuthandiza mpaka ukamupezere mwana wanga mkazi kuchokera ku mtundu wanga, wa fuko langa.
and to say to(wards) me LORD which to go: walk to/for face: before his to send: depart messenger: angel his with you and to prosper way: journey your and to take: take woman: wife to/for son: child my from family my and from house: household father my
41 Ukadzachita zimenezi udzakhala mfulu wosamangidwa ndi lumbiro langali. Koma tsono ukadzafika kwa fuko langa, ndipo ngati sadzalola kukupatsa mbeta ya mwana wanga, aponso udzamasuka ku lumbiro langali.’”
then to clear from oath my for to come (in): come to(wards) family my and if not to give: give to/for you and to be innocent from oath my
42 “Tsono lero lino pamene ndafika pa chitsime, ndinapempha kuti, ‘Yehova, Mulungu wa mbuye wanga, Abrahamu, ngati Inu mwandidalitsadi pa ulendowu,
and to come (in): come [the] day to(wards) [the] spring and to say LORD God lord my Abraham if there you please to prosper way: journey my which I to go: went upon her
43 taonani ndayima pambali pa chitsime ichi; ndipo ndidzati kwa namwali amene atabwere kudzatunga kuti, chonde nditamwako madzi a mu mtsuko wakowu,’
behold I to stand upon spring [the] water and to be [the] maiden [the] to come out: come to/for to draw and to say to(wards) her to water: drink me please little water from jar your
44 ndipo ngati adzandiyankha kuti, ‘Imwani ndipo ndizimwetsanso madzi ngamira zanuzi,’ ameneyo akhale yemwe Yehova wamusankhira mwana wa mbuye wanga.”
and to say to(wards) me also you(m. s.) to drink and also to/for camel your to draw he/she/it [the] woman which to rebuke LORD to/for son: child lord my
45 “Ndisanatsirize kupemphera, ndinangoona Rebeka akutulukira mtsuko wake uli pa phewa. Anatsetserekera ku chitsime kukatunga madzi ndipo ndinati kwa iye, ‘Chonde patseko madzi akumwa.’
I before to end: finish to/for to speak: speak to(wards) heart my and behold Rebekah to come out: come and jar her upon shoulder her and to go down [the] spring [to] and to draw and to say to(wards) her to water: drink me please
46 “Mofulumira, anatsitsa mtsuko wake pa phewa pake nati, ‘Imwani ndiponso ndizimwetsa madzi ngamira zanuzi.’ Kotero ine ndinamwa ndipo anamwetsanso ngamirazo.
and to hasten and to go down jar her from upon her and to say to drink and also camel your to water: watering and to drink and also [the] camel to water: watering
47 “Ndinamufunsa kuti, ‘Ndiwe mwana wa yani?’ “Iye anati, ‘Ndine mwana wa Betueli mwana wa Nahori, amene Milika anamuberekera.’ “Tsono ndinayika chipini pa mphuno yake ndi kumveka zibangiri mʼmikono yake,
and to ask [obj] her and to say daughter who? you(f. s.) and to say daughter Bethuel son: child Nahor which to beget to/for him Milcah and to set: put [the] ring upon face: nose her and [the] bracelet upon hand her
48 kenaka ndinawerama pansi ndi kupembedza Yehova. Ndipo ndinatamanda Yehova, Mulungu wa mbuye wanga Abrahamu, amene anandilondolera mokhulupirika njira yanga. Iye wandifikitsa kwa mʼbale wake kumene ndapezera mbeta mwana wa mbuye wanga.
and to bow and to bow to/for LORD and to bless [obj] LORD God lord my Abraham which to lead me in/on/with way: journey truth: true to/for to take: take [obj] daughter brother: male-relative lord my to/for son: child his
49 Tsono ngati mukufuna kuonetsa kukoma mtima kwanu kwa mbuye wanga, ndikuonetsa kukhulupirika kwanu, ndiwuzeni; ndipo ngati si choncho ndiwuzeninso kuti ndidziwe chochita.”
and now if there you to make: do kindness and truth: faithful with lord my to tell to/for me and if not to tell to/for me and to turn upon right or upon left
50 Labani ndi Betueli anayankha nati, “Izi ndi zochokera kwa Yehova, ndipo ife sitinganenepo kanthu.
and to answer Laban and Bethuel and to say from LORD to come out: come [the] word: thing not be able to speak: speak to(wards) you bad: harmful or pleasant
51 Nayu Rebeka, mutengeni muzipita naye kuti akakhale mkazi wa mwana wa mbuye wanu, monga Yehova wanenera.”
behold Rebekah to/for face: before your to take: take and to go: went and to be woman: wife to/for son: child lord your like/as as which to speak: speak LORD
52 Wantchito wa Abrahamu uja atamva zimene anawerama pansi pamaso pa Yehova.
and to be like/as as which to hear: hear servant/slave Abraham [obj] word their and to bow land: soil [to] to/for LORD
53 Kenaka wantchitoyo anatulutsa ziwiya zagolide ndi zasiliva ndi zovala nazipereka kwa Rebeka. Anaperekanso mphatso zina za mtengowapatali kwa mlongo wake ndi amayi ake a Rebeka.
and to come out: send [the] servant/slave article/utensil silver: money and article/utensil gold and garment and to give: give to/for Rebekah and precious thing to give: give to/for brother: male-sibling her and to/for mother her
54 Tsono wantchito uja ndi anthu amene anali naye anadya, kumwa nagona komweko. Kutacha mmawa wake, wantchito uja anati, “Mundilole ndibwerere kwa mbuye wanga.”
and to eat and to drink he/she/it and [the] human which with him and to lodge and to arise: rise in/on/with morning and to say to send: depart me to/for lord my
55 Koma mlongo wake ndi amayi ake a Rebeka anayankha kuti, “Muloleni mtsikanayu abakhala nafe masiku khumi kapena kupyolerapo, kenaka mukhoza kupita.”
and to say brother: male-sibling her and mother her to dwell [the] maiden with us day or ten (after *L(S)*) to go: went
56 Koma iye anawawuza kuti, “Chonde musandichedwetse. Yehova wandithandiza kale pa ulendo wanga. Mundilole ndibwerere kwa mbuye wanga.”
and to say to(wards) them not to delay [obj] me and LORD to prosper way: journey my to send: depart me and to go: went to/for lord my
57 Koma iwo anati, “Bwanji timuyitane mtsikanayo ndipo timufunse ngati afuna kupita nanu panopa.”
and to say to call: call to to/for maiden and to ask [obj] lip her
58 Choncho iwo anamuyitana Rebeka uja namufunsa kuti, “Kodi ukufuna kupita ndi munthuyu panopa?” Iye anayankha kuti, “Ndipita.”
and to call: call to to/for Rebekah and to say to(wards) her to go: went with [the] man [the] this and to say to go: went
59 Kotero anamulola Rebeka pamodzi ndi mlezi wake kuti apite ndi wantchito wa Abrahamu pamodzi ndi anthu amene anali naye.
and to send: depart [obj] Rebekah sister their and [obj] to suckle her and [obj] servant/slave Abraham and [obj] human his
60 Ndipo iwo anadalitsa Rebeka ndi kumuwuza kuti, “Iwe ndiwe mlongo wathu, Mulungu akudalitse iwe, ukhale mayi wa anthu miyandamiyanda; ndi kuti zidzukulu zako zidzalanda mizinda ya adani awo.”
and to bless [obj] Rebekah and to say to/for her sister our you(f. s.) to be to/for thousand myriad and to possess: take seed: children your [obj] gate to hate him
61 Kenaka Rebeka ndi antchito ake ananyamuka kukakwera ngamira zawo ndipo anapita naye pamodzi munthu uja. Choncho wantchito uja anatenga Rebeka nʼkumapita.
and to arise: rise Rebekah and maiden her and to ride upon [the] camel and to go: follow after [the] man and to take: take [the] servant/slave [obj] Rebekah and to go: journey
62 Pa nthawiyi nʼkuti Isake atafika kuchokera ku chitsime cha Wamoyo Wondipenya (Beeri-lahai-roi), popeza tsopano ankakhala ku Negevi.
and Isaac to come (in): come from to come (in): come Beer-lahai-roi Beer-lahai-roi Beer-lahai-roi and he/she/it to dwell in/on/with land: country/planet [the] Negeb
63 Tsiku lina chakumadzulo, Isake anatuluka kukayendayenda ku munda, ndipo atakweza maso anaona ngamira zikubwera.
and to come out: come Isaac to/for to meditate in/on/with land: country to/for to turn evening and to lift: look eye his and to see: see and behold camel to come (in): come
64 Rebeka nayenso anatukula maso naona Isake. Ndipo anatsika pa ngamira yake
and to lift: look Rebekah [obj] eye her and to see: see [obj] Isaac and to fall: fall from upon [the] camel
65 nafunsa wantchito uja kuti, “Kodi munthu uyo ndi ndani akuyenda mʼmundamo kubwera kudzakumana nafe?” Wantchitoyo anayankha, “Ndiye mbuye wanga.” Choncho Rebeka anatenga nsalu ndi kufunda kumaso.
and to say to(wards) [the] servant/slave who? [the] man this [the] to go: walk in/on/with land: country to/for to encounter: meet us and to say [the] servant/slave he/she/it lord my and to take: take [the] shawl and to cover
66 Tsono wantchito uja anawuza Isake zonse zimene anazichita.
and to recount [the] servant/slave to/for Isaac [obj] all [the] word: thing which to make: do
67 Isake analowa naye Rebeka mu tenti ya amayi ake Sara, ndipo anakhala mkazi wake. Isake anamukonda kwambiri Rebeka mkazi wake motero kuti zimenezi zinamutonthoza imfa ya amayi ake.
and to come (in): bring her Isaac [the] tent [to] Sarah mother his and to take: marry [obj] Rebekah and to be to/for him to/for woman: wife and to love: lover her and to be sorry: comfort Isaac after mother his