< Genesis 23 >

1 Sara anakhala ndi moyo zaka 127.
Sarah el moul sun yac siofok longoul itkosr matwal.
2 Anamwalirira ku Kiriyati-Araba, kumeneku ndi ku Hebroni, mʼdziko la Kanaani, ndipo Abrahamu anapita kukakhuza maliro a Sara, namulirira.
El misa Hebron in acn Canaan, ac Abraham el asor yokna kacl.
3 Kenaka Abrahamu ananyamuka pamene panali mtembo wa mkazi wakepo kupita kukayankhula ndi anthu a ku Hiti. Ndipo anati,
El tuyak liki acn se ma monin mutan kial oan we, ac som nu yurin mwet Hit, ac fahk,
4 “Ine ndine mlendo wongoyendayenda kwanu kuno. Bwanji mundigulitse malo woti akhale manda kuti ndiyikepo thupi la mkazi wanga.”
“Nga mwetsac se muta inmasrlowos inge. Kukakunma sie ipin acn an nu sik, ngan pikinya mutan kiuk uh we.”
5 Anthu a ku Hiti aja anamuyankha Abrahamu kuti,
Elos topuk,
6 “Tatimverani mbuye wathu, inu ndinu mwana wa mfumu wamkulu pakati pathu. Chonde ikani thupi la mkazi wanu mʼmanda aliwonse amene mungafune. Palibe mmodzi wa ife amene adzakukanizani manda ake kuti musayike mkazi wanu.”
“Mwet kacto, porongekut. Kut oek mu kom mwet kol fulat ac pwengpeng se. Kom ku in pikinya mutan kiom an ke kulyuk se ma wo emeet lasr uh. Kut nukewa arulana engan in asot sie kulyuk an nu sum, tuh kom fah pikinya mutan kiom an kac.”
7 Tsono Abrahamu anayimirira naweramira anthu a dziko la Hiti aja
Na Abraham el pasrla ye mutalos
8 nati, “Ngati mwaloladi kuti ndiyike mkazi wanga kuno, ndiye ndimvereni. Mundipemphere kwa Efroni mwana wa Zohari
ac fahk, “Kowos fin insese in lela nga in pikinya mutan kiuk uh inge, nunak munas siyuk sel Ephron, wen natul Zohar,
9 kuti andigulitse phanga la Makipela, limene lili kumapeto kwa munda wake. Mumupemphe kuti andigulitse pamtengo wake ndithu inu mukuona kuti akhale manda.”
elan kukakunma luf se Machpelah, su oanna ke sisken acn lal. Siyuk elan kukakunma nu sik ke molo na pwaye an ye motowos, ac nga fah molela luk mwe kulyuk.”
10 Pamenepo nʼkuti Efroni Mhiti ali pomwepo pakati pa anthuwo amene anabwera ku chipata cha mzindawo. Ndipo onse akumva anamuyankha Abrahamu
In pacl sac, Ephron el wi mwet Hit wial muta ke acn in meeting se ke mutunpot nu in siti uh. Ac el topuk ye mutun mwet nukewa su muta in acn sac,
11 nati, “Ayi mbuye wanga tandimverani, ine ndikukupatsani mundawo ndiponso phanga limene lili mʼmenemo. Ndikukupatsani malowa pamaso pa anthu a mtundu wanga. Chonde ikani mtembo wamkazi wanu.”
“Mwet kacto, porongeyu. Nga fah sot nu sum ipin acn sac nufon wi pac luf se ma oan we ah. Nga ac sot lom ye mutun mwet luk inge, tuh kom fah ku in pikinya mutan kiom an we.”
12 Apo Abrahamu anaweramanso mwaulemu pamaso pa anthu a mʼdzikolo
Tusruktu Abraham el pasrla ye mutun mwet Hit uh
13 ndipo anthu onse akumva Abrahamu anati kwa Efroni, “Ngati kungatheke, chonde ndimvereni. Ine ndichita kugula mundawu. Landirani ndalama za mundawu kuti ine ndiyike mkazi wanga mʼmenemo.”
ac fahk nu sel Ephron tuh mwet nukewa in ku in lohng, “Nga siyuk kom in nunak munas lohngwin ma nga ac fahk uh. Nga ac moli ipin acn nufon sac. Sruokya molo uh, tuh nga fah ku in pikinya mutan kiuk uh we.”
14 Koma Efroni anamuyankha Abrahamu nati,
Ephron el topuk,
15 “Mundimvere mbuye wanga; mundawo mtengo wake ndi masekeli asiliva okwana 400. Koma zimenezo nʼchiyani pakati pa ine ndi inu? Ikani mtembo wa mkazi wanu.”
“Mwet kacto, lupan molin acn uh ipin silver angfoko na — lupa se ingan ma na pilasr siktal. Pikinya na mutan kiom an we.”
16 Abrahamu anavomera mtengo umene ananena Efroni Ahiti onse akumva ndipo anamuwerengera masekeli asiliva okwana 400 monga mwa mtengo wa ndalama umene amalonda a nthawi imeneyo ankagwiritsa ntchito.
Abraham el insese nu kac, ac srikeya lupa se ma Ephron el fahk ye mutun mwet ah — ipin silver angfoko, fal nu ke srikasrak ma orekmakinyuk sin mwet kuka.
17 Choncho munda wa Efroni wa ku Makipela umene unali kufupi ndi Mamre, kuphatikiza munda, phanga linali mʼmenemo pamodzi ndi mitengo yonse ya mʼmundamo, zinaperekedwa
Pa oru acn sel Ephron in Machpelah, su oan kutulap in Mamre, tuh lal Abraham lac ah. Ma Ephron el kitaung uh pa acn ah, luf sac, ac sak nukewa fin acn sac, utyak na nwe ke masrol lal ah.
18 kwa Abrahamu ngati chuma chake pamaso pa anthu onse a ku Hiti amene anabwera ku chipata cha mzindawo.
Eteyuk sin mwet Hit nukewa su wi muta in pacl sac lah ma lac lal Abraham pa acn sac.
19 Zitatha izi, Abrahamu anayika mkazi wake Sara mʼphanga la mʼmunda wa ku Makipela, kufupi ndi ku Mamre (kumene ndi ku Hebroni) mʼdziko la Kanaani.
Tukun ma inge, Abraham el piknilya Sarah, mutan kial, in luf se Machpelah in acn Canaan.
20 Choncho Ahiti anapereka munda pamodzi ndi phanga la mʼmenemo kwa Abrahamu kuti akhale manda.
Ouinge ipin acn se su tuh ma lun mwet Hit ah meet, ac luf se ma oan we, ma lac lal Abraham mwe kulyuk.

< Genesis 23 >