< Genesis 12 >

1 Tsiku lina Yehova anamuwuza Abramu kuti, “Tuluka mʼdziko lako. Siya abale ako ndi banja la abambo ako ndipo pita ku dziko limene ndidzakusonyeza.
Rəbbee İbramık'le eyhen: – Yiğna ölka, dekkın xav, vas k'anebınbı g'alepçe, Zı vak'le eyhesde ölkeeqa hoora.
2 “Ndidzakusandutsa kholo la mtundu waukulu wa anthu ndipo ndidzakudalitsa; ndi kukusandutsa wotchuka kotero kuti udzakhala dalitso kwa anthu ambiri.
Vas xayir-düə hevles, vake xədın millet g'ales, do axtı qa'as, yiğne doyuka xayir-düə hevles.
3 Ndidzadalitsa amene adzadalitsa iwe, ndi kutemberera amene adzatemberera iwe; ndipo mafuko onse a pa dziko lapansi adzadalitsika kudzera mwa iwe.”
Zı vas xayir-düə huvuynbışis, xayir-düə, bed-düə hav'uynbışis, bed-düə g'axuvles. Ç'iyeyne aq'valyne gırgıne milletbışe valek'ena xayir-düə alyapt'as.
4 Choncho Abramu ananyamuka monga momwe Yehova anamuwuzira, napita pamodzi ndi Loti. Pamene Abramu amachoka ku Harani nʼkuti ali ndi zaka 75.
İbram, Rəbbee eyhəxür, yəqqı'l gexha. Lutur mang'uka sacigee ayk'an. Xaraneençe qığeç'uyng'a İbramıqa yights'ale xholle senniy vod.
5 Abramu anatenga mkazi wake Sarai, Loti, mwana wamngʼono wake, pamodzi ndi chuma chawo chimene anapeza ndi antchito amene anali nawo ku Harani. Iwo ananyamuka ulendo mpaka kukafika ku dziko la Kanaani.
İbramee Xaranee hı'iyn gırgın kar, xhunaşşe Saray, çoçuna dix Lut, cun nukarar alyapt'ı Kana'anne ölkeeqa yəqqı'l gexha. Manbı Kana'anne ölkeeqa hiviyxharanbı.
6 Abramu anadutsa mʼdzikomo mpaka kukafika ku Sekemu pa mtengo wa thundu wa ku More. Nthawi imeneyo Akanaani analipobe mʼdzikomo.
İbram maa'ar More eyhene mı'qəsqa, Şekem eyhene cigeene hiyxhar. Manke maa'ad Kana'anaaşin milletniy eyxhen.
7 Yehova anadza kwa Abramu nati, “Kwa zidzukulu zako ndidzapereka dziko limeneli.” Choncho Abramu anamangira Yehova amene anadza kwa iye, guwa lansembe.
Rəbb İbramısqa dyagu uvhuyn: – Zı ina ölka yiğne nasılıs hevles. İbramee cus dyaguyne Rəbbis, maa'ad q'urbanbı alyaa'an ciga alya'a.
8 Atachoka pamenepo analowera cha ku mapiri a kummawa kwa Beteli namangako tenti yake pakati pa Beteli chakumadzulo ndi Ai chakummawa. Kumeneko anamangira Yehova guwa lansembe napemphera mʼdzina la Yehovayo.
Mançer Bet-Eline şargılyne suvabınane cigeeqa ayk'an. Ma'ab mang'vee çadır giviyxə. Çadırne garbıl Bet-El, şargılib Ğay eyhena şahar vooxhe. İbramee maa'ad Rəbbis q'urbanbı gyaat'an ciga ali'ı ı'bəədat ha'a.
9 Kenaka Abramu ananyamuka kumalowera cha ku Negevi.
İbram kırra-kırra mançer ayk'anna canubulqa, Negevne sahrayne suralqa.
10 Kunagwa njala yayikulu mʼdzikomo, ndipo Abramu anapita ku Igupto kukakhala ngati mlendo kwa kanthawi kochepa popeza njalayo inakula kwambiri.
İne ölkee it'umun mısvalybı xət qetxhava İbram sık'ınna gahıs Misirılqa ayk'ann.
11 Atatsala pangʼono kulowa mu Igupto, Abramu anamuwuza mkazi wake Sarai kuti, “Ndimadziwa kuti ndiwe mkazi wokongola kwambiri.
Misireeqa hiviyxharang'a mang'vee cune xhunaşşe Sarayk'le eyhen: – Ğu geer uftanra yixhay zak'le ats'an.
12 Tsono Aigupto akakuona adzanena kuti ‘Ameneyu ndi mkazi wake.’ Tsono adzandipha ine nakusiya iwe ndi moyo.
Misirbışe ğu g'aycu eyhesın: «İng'una xhunaşşevur». Manke manbışe zı gik'u ğu üç'ürra g'alerçes.
13 Tsono udzikawawuza kuti iwe ndiwe mlongo wanga. Ukatero zidzandiyendera bwino ndipo ndidzapulumuka chifukwa cha iwe.”
Hucoone ixhes ğu manbışik'le eyhe, ğu yizda yiçu vor, yiğnemee zak sidyoot'a, üç'ürra g'alyaraççe.
14 Pamene Abramu anafika ku Igupto, Aigupto aja anaona kuti Sarai anali mkazi wokongoladi.
İbram Misirqa hirxhılymee, misiribışik'le mang'una xhunaşşe geer uftanra yixhay g'ecen.
15 Pamene akuluakulu a ku nyumba ya Farao anamuona, anakamuyamikira pamaso pa Farao ndipo ananka naye ku nyumba ya Farao.
Zəiyfa g'aycuyne Misirne paççahne, fironne insanaaşe məng'ı'ne micagiyvalina gaf fironus haa'a. Manar qiykekkana fironne sareeqa.
16 Abramu naye zinthu zinkamuyendera bwino chifukwa cha Sarai. Farao anamupatsa nkhosa, ngʼombe, abulu aamuna ndi abulu aakazi, antchito aakazi pamodzi ndi ngamira.
Firon məng'ı'nimee İbramıkar yugra ıxha. Mang'uqa çavra-vəq'ə, əməler, devabı, nukar adamer, nukar yedar vooxhe.
17 Koma Yehova anabweretsa matenda owopsa pa Farao pamodzi ndi banja lake lonse chifukwa cha Sarai mkazi wa Abramu.
İbramne xhunaşşe Saraynimee Rəbbee fironneyiy fironne xaabınbışilqa xətta ık'arbı alyaa'a.
18 Choncho Farao anayitanitsa Abramu namufunsa kuti, “Nʼchiyani wandichitirachi? Nʼchifukwa chiyani sunandiwuze kuti ameneyu ndi mkazi wako?
Fironee İbram qort'ul eyhen: – İn hucoon ğu zak hı'iyn?! Nya'a Saray yiğna xhunaşşe yixhay ittevhu?
19 Nʼchifukwa chiyani unati ndi mlongo wako, mpaka ine ndinamutenga kukhala mkazi wanga? Eko mkazi wako. Mutenge uzipita!”
Nişil-allane «yizda yiçuva» uvhu, məng'ı'ka davatbı ha'as hassır? Alert'e yiğna xhunaşşer, hoora!
20 Farao analamula asilikali ake ndipo iwo anamutulutsa Abramu pamodzi ndi mkazi wake ndi zonse anali nazo.
Fironee İbramiy cuna xhunaşşe, cone vardatıka sacigee ölkençe yəqqı'l hee'eva əmr haa'a.

< Genesis 12 >