< Agalatiya 1 >
1 Paulo mtumwi, osati wosankhidwa ndi anthu kapena kutumidwa ndi munthu ayi, koma Yesu Khristu, ndi Mulungu Atate amene anamuukitsa Yesuyo kwa akufa,
មនុឞ្យេភ្យោ នហិ មនុឞ្យៃរបិ នហិ កិន្តុ យីឝុខ្រីឞ្ដេន ម្ឫតគណមធ្យាត៑ តស្យោត្ថាបយិត្រា បិត្រេឝ្វរេណ ច ប្រេរិតោ យោៜហំ បៅលះ សោៜហំ
2 pamodzi ndi abale onse amene ali nane, Kulembera mipingo ya ku Galatiya:
មត្សហវត៌្តិនោ ភ្រាតរឝ្ច វយំ គាលាតីយទេឝស្ថាះ សមិតីះ ប្រតិ បត្រំ លិខាមះ។
3 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale nanu.
បិត្រេឝ្វរេណាស្មាំក ប្រភុនា យីឝុនា ខ្រីឞ្ដេន ច យុឞ្មភ្យម៑ អនុគ្រហះ ឝាន្តិឝ្ច ទីយតាំ។
4 Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
អស្មាកំ តាតេឝ្វរេស្យេច្ឆានុសារេណ វត៌្តមានាត៑ កុត្សិតសំសារាទ៑ អស្មាន៑ និស្តារយិតុំ យោ (aiōn )
5 Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
យីឝុរស្មាកំ បាបហេតោរាត្មោត្សគ៌ំ ក្ឫតវាន៑ ស សវ៌្វទា ធន្យោ ភូយាត៑។ តថាស្តុ។ (aiōn )
6 Ine ndikudabwa kuti mukusiya mwamsangamsanga chotere Mulungu amene anakuyitanani mwachisomo cha Khristu ndipo mwatembenuka ndi kutsatira uthenga wina wosiyana,
ខ្រីឞ្ដស្យានុគ្រហេណ យោ យុឞ្មាន៑ អាហូតវាន៑ តស្មាន្និវ្ឫត្យ យូយម៑ អតិតូណ៌ម៑ អន្យំ សុសំវាទម៑ អន្វវត៌្តត តត្រាហំ វិស្មយំ មន្យេ។
7 umene si Uthenga Wabwino konse. Pali anthu ena amene akukusokonezani komanso akufuna kupotoza Uthenga Wabwino wa Khristu.
សោៜន្យសុសំវាទះ សុសំវាទោ នហិ កិន្តុ កេចិត៑ មានវា យុឞ្មាន៑ ចញ្ចលីកុវ៌្វន្តិ ខ្រីឞ្ដីយសុសំវាទស្យ វិបយ៌្យយំ កត៌្តុំ ចេឞ្ដន្តេ ច។
8 Ngakhale ife kapena mngelo wochokera kumwamba, akalalikira Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene tinakulalikirani uja, iyeyo akhale wotembereredwa!
យុឞ្មាកំ សន្និធៅ យះ សុសំវាទោៜស្មាភិ រ្ឃោឞិតស្តស្មាទ៑ អន្យះ សុសំវាទោៜស្មាកំ ស្វគ៌ីយទូតានាំ វា មធ្យេ កេនចិទ៑ យទិ ឃោឞ្យតេ តហ៌ិ ស ឝប្តោ ភវតុ។
9 Monga tanena kale, tsopano ndikubwereza kunenanso kuti, “Ngati wina aliyense akulalikirani Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene munawulandira, iyeyo akhale wotembereredwa.”
បូវ៌្វំ យទ្វទ៑ អកថយាម, ឥទានីមហំ បុនស្តទ្វត៑ កថយាមិ យូយំ យំ សុសំវាទំ គ្ឫហីតវន្តស្តស្មាទ៑ អន្យោ យេន កេនចិទ៑ យុឞ្មត្សន្និធៅ ឃោឞ្យតេ ស ឝប្តោ ភវតុ។
10 Kodi tsopano ndikufuna kukopa anthu kuti andivomereze, kapena Mulungu? Kapena ndikufuna kukondweretsa anthu? Ngati ine ndikanakhala kuti ndikufunabe kukondweretsa anthu, sindikanakhala mtumiki wa Khristu.
សាម្ប្រតំ កមហម៑ អនុនយាមិ? ឦឝ្វរំ កិំវា មានវាន៑? អហំ កិំ មានុឞេភ្យោ រោចិតុំ យតេ? យទ្យហម៑ ឥទានីមបិ មានុឞេភ្យោ រុរុចិឞេយ តហ៌ិ ខ្រីឞ្ដស្យ បរិចារកោ ន ភវាមិ។
11 Abale, ine ndikufuna kuti mudziwe, kuti Uthenga Wabwino umene ndinalalikira si ochokera kwa munthu ayi.
ហេ ភ្រាតរះ, មយា យះ សុសំវាទោ ឃោឞិតះ ស មានុឞាន្ន លព្ធស្តទហំ យុឞ្មាន៑ ជ្ញាបយាមិ។
12 Ine sindinawulandire kuchokera kwa munthu aliyense, kapena kuphunzitsidwa; koma ndinawulandira mwa vumbulutso lochokera kwa Khristu.
អហំ កស្មាច្ចិត៑ មនុឞ្យាត៑ តំ ន គ្ឫហីតវាន៑ ន វា ឝិក្ឞិតវាន៑ កេវលំ យីឝោះ ខ្រីឞ្ដស្យ ប្រកាឝនាទេវ។
13 Pakuti inu munamva za moyo wanga wakale mʼChiyuda, mmene ndinkazunzira mpingo wa Mulungu koopsa ndi kuyesetsa kuwuwononga.
បុរា យិហូទិមតាចារី យទាហម៑ អាសំ តទា យាទ្ឫឝម៑ អាចរណម៑ អករវម៑ ឦឝ្វរស្យ សមិតិំ ប្រត្យតីវោបទ្រវំ កុវ៌្វន៑ យាទ្ឫក៑ តាំ វ្យនាឝយំ តទវឝ្យំ ឝ្រុតំ យុឞ្មាភិះ។
14 Ine ndinkapambana Ayuda ambiri a msinkhu wanga pochita za Chiyuda, ndipo ndinali wachangu koposa pa miyambo ya makolo athu.
អបរញ្ច បូវ៌្វបុរុឞបរម្បរាគតេឞុ វាក្យេឞ្វន្យាបេក្ឞាតីវាសក្តះ សន៑ អហំ យិហូទិធម៌្មតេ មម សមវយស្កាន៑ ពហូន៑ ស្វជាតីយាន៑ អត្យឝយិ។
15 Koma Mulungu, amene anandipatula ine ndisanabadwe, ndi kundiyitana mwachisomo chake, atakondweretsedwa
កិញ្ច យ ឦឝ្វរោ មាត្ឫគព៌្ហស្ថំ មាំ ប្ឫថក៑ ក្ឫត្វា ស្វីយានុគ្រហេណាហូតវាន្
16 kuvumbulutsa Mwana wake mwa ine, kuti ndikalalikire Khristuyo pakati pa anthu a mitundu ina, ine sindinapemphe nzeru kwa munthu aliyense.
ស យទា មយិ ស្វបុត្រំ ប្រកាឝិតុំ ភិន្នទេឝីយានាំ សមីបេ ភយា តំ ឃោឞយិតុញ្ចាភ្យលឞត៑ តទាហំ ក្រវ្យឝោណិតាភ្យាំ សហ ន មន្ត្រយិត្វា
17 Ine sindinapite ku Yerusalemu kukaonana ndi amene anali atumwi ine ndisanakhale mtumwi. Mʼmalo mwake nthawi yomweyo ndinapita ku Arabiya ndi kubwereranso ku Damasiko.
បូវ៌្វនិយុក្តានាំ ប្រេរិតានាំ សមីបំ យិរូឝាលមំ ន គត្វារវទេឝំ គតវាន៑ បឝ្ចាត៑ តត្ស្ថានាទ៑ ទម្មេឞកនគរំ បរាវ្ឫត្យាគតវាន៑។
18 Pambuyo pake, patatha zaka zitatu, ndinapita ku Yerusalemu kukaonana ndi Petro ndikukhala naye masiku khumi ndi asanu.
តតះ បរំ វឞ៌ត្រយេ វ្យតីតេៜហំ បិតរំ សម្ភាឞិតុំ យិរូឝាលមំ គត្វា បញ្ចទឝទិនានិ តេន សាទ៌្ធម៑ អតិឞ្ឋំ។
19 Ine sindinaonane ndi atumwi enawo koma Yakobo yekha, mʼbale wa Ambuye.
កិន្តុ តំ ប្រភោ រ្ភ្រាតរំ យាកូពញ្ច វិនា ប្រេរិតានាំ នាន្យំ កមប្យបឝ្យំ។
20 Ine ndikutsimikizira inu pamaso pa Mulungu kuti zimene ndikukulemberani si zonama ayi.
យាន្យេតានិ វាក្យានិ មយា លិខ្យន្តេ តាន្យន្ឫតានិ ន សន្តិ តទ៑ ឦឝ្វរោ ជានាតិ។
21 Pambuyo pake ndinapita ku Siriya ndi ku Kilikiya.
តតះ បរម៑ អហំ សុរិយាំ កិលិកិយាញ្ច ទេឝៅ គតវាន៑។
22 Koma sindimadziwika ndi nkhope ku mipingo ya ku Yudeya imene ili mwa Khristu.
តទានីំ យិហូទាទេឝស្ថានាំ ខ្រីឞ្ដស្យ សមិតីនាំ លោកាះ សាក្ឞាត៑ មម បរិចយមប្រាប្យ កេវលំ ជនឝ្រុតិមិមាំ លព្ធវន្តះ,
23 Iwo anangomva mbiri yokha yakuti, “Munthu amene poyamba anatizunza ife, tsopano akulalikira chikhulupiriro chimene iyeyo nthawi ina anafuna kuchiwononga.”
យោ ជនះ បូវ៌្វម៑ អស្មាន៑ ប្រត្យុបទ្រវមករោត៑ ស តទា យំ ធម៌្មមនាឝយត៑ តមេវេទានីំ ប្រចារយតីតិ។
24 Ndipo iwo anayamika Mulungu chifukwa cha ine.
តស្មាត៑ តេ មាមធីឝ្វរំ ធន្យមវទន៑។