< Agalatiya 1 >

1 Paulo mtumwi, osati wosankhidwa ndi anthu kapena kutumidwa ndi munthu ayi, koma Yesu Khristu, ndi Mulungu Atate amene anamuukitsa Yesuyo kwa akufa,
Nghngicim üngka naw lawkia am kya lü, nghngicima phäha pi am kya lü, Jesuh Khritaw mtho beki Pa Pamhnam la Jesuh Khritaw üngka kei Pawluh la,
2 pamodzi ndi abale onse amene ali nane, Kulembera mipingo ya ku Galatiya:
ka hlawnga awmkia jumeiki he naküt naw Kalatiha awmkia sangcim he ning jah hnukset ve ung:
3 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale nanu.
Mi Pa Pamhnam la Bawipa Jesuh Khritaw naw bäkhäknak la dim’yenak ning jah pe se.
4 Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn g165)
Mi Pamhnam la mi Pa ngjakhlüa, tuhkbäih ahina kcün kse üngka naw a jah mhlätnak vaia, Khritaw naw mi katnak hea phäha amät ngpe kyuki; (aiōn g165)
5 Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn g165)
Pamhnama veia hlüngtainak angläta ve se! Amen. (aiōn g165)
6 Ine ndikudabwa kuti mukusiya mwamsangamsanga chotere Mulungu amene anakuyitanani mwachisomo cha Khristu ndipo mwatembenuka ndi kutsatira uthenga wina wosiyana,
Khritawa bäkhäknak üng ning jah khüki yawk u lü, thangkdaw akce nami dokhamei naw na m’yühei ve.
7 umene si Uthenga Wabwino konse. Pali anthu ena amene akukusokonezani komanso akufuna kupotoza Uthenga Wabwino wa Khristu.
“Thangkdaw akce” am ve. Khyang avang naw ning jah mlung mthüiei u lü Khritawa thangkdaw thuhlai hlüsaki he pi ami awma phäha ahikba ka pyen ni.
8 Ngakhale ife kapena mngelo wochokera kumwamba, akalalikira Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene tinakulalikirani uja, iyeyo akhale wotembereredwa!
Cunsepi, keimia pi kyase, khankhaw üngka khankhawngsäa pi kyase nami veia kami pyena thangkdawa kthaka hngalangeikia thangkdaw a pyen üngta, mulaimei däa mkateia kya kawm.
9 Monga tanena kale, tsopano ndikubwereza kunenanso kuti, “Ngati wina aliyense akulalikirani Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene munawulandira, iyeyo akhale wotembereredwa.”
Kami ning jah mtheh päng, tuhkbäih ning jah mtheh law be vang: “Nami yah pänga thangkdawa kthaka thangkdaw akce ning jah mtheh lawki a awm üngta mulaimei däa mkateia kya kawm.”
10 Kodi tsopano ndikufuna kukopa anthu kuti andivomereze, kapena Mulungu? Kapena ndikufuna kukondweretsa anthu? Ngati ine ndikanakhala kuti ndikufunabe kukondweretsa anthu, sindikanakhala mtumiki wa Khristu.
Khyanga ngak ka yahnak vaia ka pyenkia mäi lawki aw? Acukba am ni! Mhnama ngaknak ni ka ngjak hlü. Khyang hea ksunga ka ngminga ngthang vai ka ktha naki aw? Acukba ka ni üngta Khritawa m'ya am ka kya khai.
11 Abale, ine ndikufuna kuti mudziwe, kuti Uthenga Wabwino umene ndinalalikira si ochokera kwa munthu ayi.
Ka püi he aw, thangkdaw ka sang hin nghngicim khyang üngka ngthuha am kya naw ti ning jah mtheh veng.
12 Ine sindinawulandire kuchokera kwa munthu aliyense, kapena kuphunzitsidwa; koma ndinawulandira mwa vumbulutso lochokera kwa Khristu.
Nghngicim khyang üngka ka yahkia am kya, u naw pi am na mthei naw. Jesuh Khritaw amät naw a na mdana ni akya ve.
13 Pakuti inu munamva za moyo wanga wakale mʼChiyuda, mmene ndinkazunzira mpingo wa Mulungu koopsa ndi kuyesetsa kuwuwononga.
Judah hea jumeinak ka läk k’um üng Pamhnama sangcim he ä jah m’yenei lü jah mkhuimkha lü jah kpyeh vaia ka kthanak khawi cen nami ngjaki.
14 Ine ndinkapambana Ayuda ambiri a msinkhu wanga pochita za Chiyuda, ndipo ndinali wachangu koposa pa miyambo ya makolo athu.
Judah hea jumeinak lama kei cun ka ngtehpüi hea kthaka pi ktha na bawk lü, mi pupa hea thumcame üng pi ka ng’apei bawki.
15 Koma Mulungu, amene anandipatula ine ndisanabadwe, ndi kundiyitana mwachisomo chake, atakondweretsedwa
Acunsepi am ka hmi law ham üng Pamhnam naw a bäkhäknak am na xü lü amät ka khüih khaia a na khü päng.
16 kuvumbulutsa Mwana wake mwa ine, kuti ndikalalikire Khristuyo pakati pa anthu a mitundu ina, ine sindinapemphe nzeru kwa munthu aliyense.
Ka veia a capa a mdan law üng Khyangmjükce hea veia amäta mawng thangkdaw ka sangnak vaia ua mcäinak am kthäh nawng,
17 Ine sindinapite ku Yerusalemu kukaonana ndi amene anali atumwi ine ndisanakhale mtumwi. Mʼmalo mwake nthawi yomweyo ndinapita ku Arabiya ndi kubwereranso ku Damasiko.
keia kthaka ngsäa kya maki he ka jah hmu khaia Jerusalema pi am cit nawng. Arab khawa cit ktäih lü acunüng Damatet khawa ni ka nghlat be ve.
18 Pambuyo pake, patatha zaka zitatu, ndinapita ku Yerusalemu kukaonana ndi Petro ndikukhala naye masiku khumi ndi asanu.
Acunüng, kum kthum ngsawk se Pitaa veia ksingkhyapnak ka yah khaia Jerusalem khawa hang cit lü acuia ania hlawnga mhmüp xaleimhma ka awmki.
19 Ine sindinaonane ndi atumwi enawo koma Yakobo yekha, mʼbale wa Ambuye.
Bawipaa na Jakuk dänga thea ngsä akce u am jah hmu nawng.
20 Ine ndikutsimikizira inu pamaso pa Mulungu kuti zimene ndikukulemberani si zonama ayi.
Nami veia ka yuk law hmanki. Am ka hleihlak Pamhnam naw ksingki.
21 Pambuyo pake ndinapita ku Siriya ndi ku Kilikiya.
Acun käna Siria khaw la Kilikih khawa ka citki.
22 Koma sindimadziwika ndi nkhope ku mipingo ya ku Yudeya imene ili mwa Khristu.
Acuna kcün üng Judah khawa sangcim he naw akhyang puma am na ksing ham u.
23 Iwo anangomva mbiri yokha yakuti, “Munthu amene poyamba anatizunza ife, tsopano akulalikira chikhulupiriro chimene iyeyo nthawi ina anafuna kuchiwononga.”
“Ajana jah mkhuimkha khawi lü, ajana a kpyeh hlü khawia jumnak cen sang hü ve” ti khyang hea pyen ngja u lü,
24 Ndipo iwo anayamika Mulungu chifukwa cha ine.
acunüng, keia phäha Pamhnam mküimtoki he.

< Agalatiya 1 >