< Agalatiya 2 >

1 Kenaka, patatha zaka khumi ndi zinayi, ndinapitanso ku Yerusalemu, nthawi iyi ndinapita ndi Barnaba. Ndinatenganso Tito kuti apite nafe.
then through/because of fourteen year again to ascend toward Jerusalem with/after Barnabas (to take along with *NK(o)*) and Titus
2 Ine ndinapita chifukwa Mulungu anachita kundionetsera kuti ndipite ndipo ndinakakumana ndi atsogoleri mu msonkhano mwamseri ndi kuwafotokozera Uthenga Wabwino umene ndimalalikira pakati pa anthu a mitundu ina. Ndinachita zimenezi kuti ndikhale ndi chitsimikizo kuopa kuti mwina ndinathamanga kapena ndimathamanga liwiro pachabe.
to ascend then according to revelation and to set before it/s/he the/this/who gospel which to preach in/on/among the/this/who Gentiles according to one's own/private then the/this/who to think not how toward empty to run or to run
3 Komatu ngakhale Tito, amene anali nane sanakakamizidwe kuti achite mdulidwe, ngakhale iyeyo anali Mgriki.
but nor Titus the/this/who with I/we Greek, Gentile to be to compel to circumcise
4 Nkhani iyi inayambika chifukwa abale ena achinyengo amene analowerera pakati pathu kuti adzaone za ufulu umene tili nawo mwa Khristu Yesu ndikuti atisandutse akapolo.
through/because of then the/this/who infiltrated false brother who/which to come in to spy the/this/who freedom me which to have/be in/on/among Christ Jesus in order that/to me (to enslave *N(k)O*)
5 Ife sitinawagonjere ndi pangʼono pomwe, nʼcholinga chakuti choonadi cha Uthenga Wabwino chikhalebe ndi ife.
which nor to/with hour to yield the/this/who submission in order that/to the/this/who truth the/this/who gospel to remain to/with you
6 Koma kunena za aja ankaoneka ngati ofunika kwambiri, chimene iwo anali sichisintha kanthu kwa ine; chifukwa Mulungu alibe tsankho, iwowo sanawonjezepo kanthu pa uthenga wanga.
away from then the/this/who to think to exist one what sort? once/when to be none me to spread/surpass face (the/this/who *no*) God a human no to take I/we for the/this/who to think none to confer
7 Makamaka anaona kuti ine ndinapatsidwa ntchito yolalikira Uthenga Wabwino kwa anthu a mitundu ina monga momwe Petro anapatsidwa ntchito yolalikira Uthenga Wabwino kwa Ayuda.
but instead to perceive: see that/since: that to trust (in) the/this/who gospel the/this/who uncircumcision as/just as Peter the/this/who circumcision
8 Pakuti Mulungu, amene amagwira ntchito mu utumiki wa Petro monga mtumwi kwa Ayuda, amagwiranso ntchito mu utumiki wanga monga mtumiki kwa anthu a mitundu ina.
the/this/who for be active Peter toward apostleship the/this/who circumcision be active and I/we toward the/this/who Gentiles
9 Yakobo, Petro ndi Yohane, amene ankatengedwa ngati mizati, atazindikira chisomo chimene chinapatsidwa kwa ine, anagwirana chanza ndi ine ndi Barnaba kusonyeza chiyanjano chathu. Iwo anavomereza kuti ife tipite kwa anthu a mitundu ina ndipo iwo apite kwa Ayuda.
and to know the/this/who grace the/this/who to give me James and Cephas and John the/this/who to think pillar to exist right to give I/we and Barnabas participation in order that/to me (on the other hand *o*) toward the/this/who Gentiles it/s/he then toward the/this/who circumcision
10 Chimene iwo anapempha ndi chakuti ife tipitirize kukumbukira osauka, chinthu chimene ine ndinali okonzeka kuchichita.
alone the/this/who poor in order that/to to remember which and be eager it/s/he this/he/she/it to do/make: do
11 Petro atafika ku Antiokeya, ine ndinamudzudzula pa gulu chifukwa anapezeka wolakwa.
when then to come/go (Cephas *N(k)O*) toward Antioch according to face it/s/he to oppose that/since: since to condemn to be
12 Pakuti asanafike anthu otumidwa ndi Yakobo, iye ankadya pamodzi ndi anthu a mitundu ina. Koma atafika, iyeyo anachoka pakati pa anthuwo nakakhala pa yekha chifukwa ankaopa anthu a mʼgulu la mdulidwe.
before the/this/who for to come/go one away from James with/after the/this/who Gentiles to eat with when then (to come/go *NK(O)*) to withdraw and to separate themself to fear the/this/who out from circumcision
13 Ayuda enanso anamutsata pochita zachinyengozi, kotero kuti ngakhale Barnaba anasocheretsedwa chifukwa cha chinyengo chawocho.
and to join hypocrisy it/s/he and the/this/who remaining Jew so and Barnabas to lead away with it/s/he the/this/who hypocrisy
14 Koma nditaona kuti iwo sankachita molingana ndi choonadi cha Uthenga Wabwino, ndinawuza Petro pamaso pa anthu onse kuti, “Iwe ndiwe Myuda koma ukukhala ngati munthu wa mtundu wina, osati Myuda. Nanga nʼchifukwa chiyani ukukakamiza anthu a mitundu ina kuti akhale ngati Ayuda?
but when to perceive: see that/since: that no be upright to/with the/this/who truth the/this/who gospel to say the/this/who (Cephas *N(k)O*) before all if you Jew be already Gentile-way and (not! *N(k)O*) Jew to live (how! *N(k)O*) the/this/who Gentiles to compel Jew
15 “Ife amene ndife Ayuda mwachibadwa, osati anthu a mitundu ina ochimwa,
me nature Jew and no out from Gentiles sinful
16 tikudziwa kuti munthu salungamitsidwa pochita ntchito za lamulo koma ndi chikhulupiriro mwa Yesu Khristu. Chomwecho, ifenso tinakhulupirira Khristu Yesu kuti tilungamitsidwe mwachikhulupiriro mwa Khristu ndipo osati pochita ntchito za lamulo, chifukwa palibe amene adzalungamitsidwa pochita ntchito za lamulo.
to know (then *no*) that/since: that no to justify a human out from work law if not through/because of faith Jesus Christ and me toward Christ Jesus to trust (in) in order that/to to justify out from faith Christ and no out from work law (that/since: since *N(k)O*) out from work law no to justify all flesh
17 “Tsono ngati ife, pamene tikufuna kulungamitsidwa mwa Khristu, zikuonekeratu poyera kuti ndifenso ochimwa, kodi zikutanthauza kuti Khristu amalimbikitsa uchimo? Ayi. Nʼkosatheka!
if then to seek to justify in/on/among Christ to find/meet and it/s/he sinful no? Christ sin servant not to be
18 Ngati ine ndimanganso chimene ndinachigumula, ndikuonetsa kuti ndine wophwanya lamulo.
if for which to destroy/lodge this/he/she/it again to build transgresor I/we to commend
19 “Pakuti pamene ndinayesera kutsatira lamulo, lamulolo linandionetsa kuti ndine wochimwa. Choncho ndinasiya kutsatira lamulo kuti ndikhale ndi moyo kwa Mulungu.
I/we for through/because of law law to die in order that/to God to live
20 Ndinapachikidwa pa mtanda pamodzi ndi Khristu, kotero kuti sindinenso amene ndili ndi moyo, koma ndi Khristu amene ali ndi moyo mwa ine. Moyo umene ndili nawo tsopano mʼthupi lino, ndi moyo mwachikhulupiriro mwa Mwana wa Mulungu, amene anandikonda nadzipereka yekha chifukwa cha ine.
Christ to crucify with to live then no still I/we to live then in/on/among I/we Christ which then now to live in/on/among flesh in/on/among faith to live the/this/who the/this/who son the/this/who God (and Christ *O*) the/this/who to love me and to deliver themself above/for I/we
21 Ine sindikukankhira kumbali chisomo cha Mulungu, chifukwa ngati chilungamo chikanapezeka pochita ntchito za lamulo, ndiye kuti Khristu anafa pachabe.”
no to reject the/this/who grace the/this/who God if for through/because of law righteousness therefore Christ freely to die

< Agalatiya 2 >