< Agalatiya 1 >
1 Paulo mtumwi, osati wosankhidwa ndi anthu kapena kutumidwa ndi munthu ayi, koma Yesu Khristu, ndi Mulungu Atate amene anamuukitsa Yesuyo kwa akufa,
I Paoly, Firàheñe, (tsy nirahe’ ondatio, ndra t’indaty, fa Iesoà Norizañey naho i Andrianañahare Rae nampitroatse aze an-kavilasy)
2 pamodzi ndi abale onse amene ali nane, Kulembera mipingo ya ku Galatiya:
naho o longo amako atoa iabio, Ho amo Fivory e Galate añeo:
3 Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale nanu.
Hasoa naho Fañanintsiñe boak’ aman’ Añahare Rae naho i Talèntika Iesoà Norizañey,
4 Yesuyo anadzipereka yekha chifukwa cha machimo athu kuti atipulumutse ku njira za moyo woyipa uno, molingana ndi chifuniro cha Mulungu ndi Atate athu. (aiōn )
ie nanolo-piaiñe ty amo hakeon-tikañeo, handrombake antika ami’ty sa raty henaneo, ty amy satrin’ Añahare Raen-tikañe; (aiōn )
5 Ulemerero ukhale kwa Mulunguyo mpaka muyaya. Ameni. (aiōn )
ama’e abey ty engeñe nainai’e donia. Amena (aiōn )
6 Ine ndikudabwa kuti mukusiya mwamsangamsanga chotere Mulungu amene anakuyitanani mwachisomo cha Khristu ndipo mwatembenuka ndi kutsatira uthenga wina wosiyana,
Mahalatsa ahy te nifarie’ areo aniany i nikanjy anahareo mb’amy hasoa’ i Norizañeiy, hitolik’ amy ze o talili-soa ila’e zao,
7 umene si Uthenga Wabwino konse. Pali anthu ena amene akukusokonezani komanso akufuna kupotoza Uthenga Wabwino wa Khristu.
tsy t’ie aman’ ila’e, fe ao ty mitsibore anahareo hañamengoke ty talili-soa’ i Norizañey
8 Ngakhale ife kapena mngelo wochokera kumwamba, akalalikira Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene tinakulalikirani uja, iyeyo akhale wotembereredwa!
Aa ndra te zahay, ndra te anjely hirik’ andindìñe añe ty mitaroñe ama’ areo ty talily ila’ te amy nitaroñe’aiy, le sira naho molale.
9 Monga tanena kale, tsopano ndikubwereza kunenanso kuti, “Ngati wina aliyense akulalikirani Uthenga Wabwino wosiyana ndi umene munawulandira, iyeyo akhale wotembereredwa.”
Hambañe amy fivola’ay teoy, le indraeko henaneo, ndra ia t’indaty minday talili-soa ama’ areo mandietse i rinambe’ areoy, le fatra an-tane.
10 Kodi tsopano ndikufuna kukopa anthu kuti andivomereze, kapena Mulungu? Kapena ndikufuna kukondweretsa anthu? Ngati ine ndikanakhala kuti ndikufunabe kukondweretsa anthu, sindikanakhala mtumiki wa Khristu.
Mipay fañisohañe am’ondatio hao iraho henaneo he aman’ Añahare? Ke mipay hahafale ondaty? F’ie te ho nanitra ondaty, le tsy ho ni-fetrek’oro’ i Norizañey.
11 Abale, ine ndikufuna kuti mudziwe, kuti Uthenga Wabwino umene ndinalalikira si ochokera kwa munthu ayi.
Hampahafohineko anahareo ry longo, te tsy nifototse am’ondaty i talili-soa itaroñakoy.
12 Ine sindinawulandire kuchokera kwa munthu aliyense, kapena kuphunzitsidwa; koma ndinawulandira mwa vumbulutso lochokera kwa Khristu.
Tsy rinambeko ama’ ondaty, naho tsy nanarañ’ ahiko, fa amy namentabentara’ Iesoà Norizañey ahiy.
13 Pakuti inu munamva za moyo wanga wakale mʼChiyuda, mmene ndinkazunzira mpingo wa Mulungu koopsa ndi kuyesetsa kuwuwononga.
Toe jinanji’areo i fanoeko taolo amo Tehodaoy, te loho nampisoañeko i Fivorin’ Añaharey, naho nimaneako rotsake,
14 Ine ndinkapambana Ayuda ambiri a msinkhu wanga pochita za Chiyuda, ndipo ndinali wachangu koposa pa miyambo ya makolo athu.
vaho nionjoñe amy fitalahoa’ o Jiosioy mandikoatse o longoko maro mpirai-nono amakoo, ie nilozoheko o lilin-droaekoo.
15 Koma Mulungu, amene anandipatula ine ndisanabadwe, ndi kundiyitana mwachisomo chake, atakondweretsedwa
Aa kanao ninòn’ Añahare nañambak’ ahy boak’ an-tron-dreneko ao, le nikanjie’e ty amy hasoa’ey,
16 kuvumbulutsa Mwana wake mwa ine, kuti ndikalalikire Khristuyo pakati pa anthu a mitundu ina, ine sindinapemphe nzeru kwa munthu aliyense.
hampalangese’e amako i ana’ey, hitaroñako aze amo kilakila’ ondatio; ie henane zay tsy niharoako safiry ty nofotse aman-dio
17 Ine sindinapite ku Yerusalemu kukaonana ndi amene anali atumwi ine ndisanakhale mtumwi. Mʼmalo mwake nthawi yomweyo ndinapita ku Arabiya ndi kubwereranso ku Damasiko.
naho tsy nionjomb’e Ierosaleme mb’ amo Firàheñe taolokoo mb’eo f’ie nifokofoko mb’ Arabia añe; vaho nimpoly mb’e Damaskose ao.
18 Pambuyo pake, patatha zaka zitatu, ndinapita ku Yerusalemu kukaonana ndi Petro ndikukhala naye masiku khumi ndi asanu.
Ie niritse ty telo taoñe le nionjomb’e Ierosaleme mb’eo hifandrèndreke amy Kefasy, vaho nitoboke ama’e ao folo andro lim’ amby.
19 Ine sindinaonane ndi atumwi enawo koma Yakobo yekha, mʼbale wa Ambuye.
Le tsy nahatrea Firàheñe ila’e iraho naho tsy Iakobe, zai’ i Talè avao.
20 Ine ndikutsimikizira inu pamaso pa Mulungu kuti zimene ndikukulemberani si zonama ayi.
(Aa ty amo sokireko ama’ areoo, le ifantàko añatrefan’ Añahare te tsy mandañitse.)
21 Pambuyo pake ndinapita ku Siriya ndi ku Kilikiya.
Ie añe, le nimb’am-paripari’ i Sirià naho i Kilkia mb’eo;
22 Koma sindimadziwika ndi nkhope ku mipingo ya ku Yudeya imene ili mwa Khristu.
ie mb’e namoea’ o Fivory amy Norizañey e Iehodào ty tareheko.
23 Iwo anangomva mbiri yokha yakuti, “Munthu amene poyamba anatizunza ife, tsopano akulalikira chikhulupiriro chimene iyeyo nthawi ina anafuna kuchiwononga.”
Toe jinanji’ iereo avao te, i nampisoañe antika taoloy ro mone mitsey i fatokisañe nimanea’e rotsake heikey.
24 Ndipo iwo anayamika Mulungu chifukwa cha ine.
Le nandrenge an’ Andrianañahare ty amako.