< Ezara 8 >

1 Nawa mayina a atsogoleri a mabanja amene anabwera nane kuchokera ku Babuloni nthawi ya ulamuliro wa mfumu Aritasasita:
Laba bazinhloko zezimuli lalabo ababhalisa kubo abeza lami sisuka eBhabhiloni ngesikhathi sokubusa kweNkosi u-Athazekisisi:
2 Geresomu wa fuko la Finehasi; Danieli wa fuko la Itamara; Hatusi
abesizukulwane sikaFinehasi, uGeshomu; abesizukulwane sika-Ithamari, uDanyeli; abesizukulwane sikaDavida, uHathushi
3 mwana wa Sekaniya wa fuko la Davide; Zekariya wa fuko la Parosi. Pamodzi ndi iyeyu panalembedwa anthu ena 150;
owesizukulwane sikaShekhaniya; abesizukulwane sikaPharoshi, uZakhariya, okwabhalisa kanye laye amadoda alikhulu lamatshumi amahlanu;
4 Elihunai mwana wa Zerahiya, wa fuko la Pahati-Mowabu. Pamodzi ndi iyeyu panalinso anthu ena 400.
abesizukulwane sikaPhahathi-Mowabi: kwakungu-Eliyehonayi indodana kaZerahiya oweza lamadoda angamakhulu amabili;
5 Sekaniya, mwana wa Yahazieli wa fuko la Zatu. Pamodzi ndi iyeyu panalembedwanso anthu 300.
abesizukulwane sikaZathu, kwakunguShekhaniya indodana kaJahaziyeli, oweza lamadoda angamakhulu amathathu;
6 Ebedi, mwana wa Yonatani wa fuko la Adini. Pamodzi naye analembedwanso anthu ena makumi asanu.
abesizukulwane sika-Adini, kwakungu-Ebhedi indodana kaJonathani, oweza lamadoda angamatshumi amahlanu;
7 Yesaiya, mwana wa Ataliya wa fuko la Elamu. Pamodzi naye panali anthu ena 70.
abesizukulwane sika-Elamu, kwakunguJeshaya indodana ka-Athaliya, oweza lamadoda angamatshumi ayisikhombisa;
8 Zebadiya, mwana wa Mikayeli wa fuko la Sefatiya. Pamodzi naye panalinso anthu 80.
abesizukulwane sikaShefathiya, kwakunguZebhadiya indodana kaMikhayeli, oweza lamadoda angamatshumi ayisificaminwembili;
9 Obadiya, mwana wa Yehieli wa fuko la Yowabu. Pamodzi naye panalinso anthu 218.
abesizukulwane sikaJowabi, kwakungu-Obhadaya indodana kaJehiyeli, oweza lamadoda angamakhulu amabili aletshumi lasificaminwembili;
10 Selomiti mwana wa Yosifiya wa fuko la Bani. Pamodzi ndi iyeyu panalinso anthu 160.
abesizukulwane sikaBhani, kwakunguShelomithi indodana kaJosifiya, oweza lamadoda alikhulu lamatshumi ayisithupha,
11 Zekariya, mwana wa Bebai wa fuko la Babai. Pamodzi naye analembedwanso anthu 28.
abesizukulwane sikaBhebhayi, kwakunguZakhariya indodana kaBhebhayi, oweza lamadoda angamatshumi amabili lasificaminwembili;
12 Yohanani, mwana wa Hakatani wa fuko la Azigadi. Pamodzi naye panalinso anthu 110.
abesizukulwane sika-Azigadi, kwakunguJohanani indodana kaHakathani, oweza lamadoda alikhulu letshumi;
13 Atsogoleri a fuko la Adonikamu, anthu amene anabwera pambuyo pake mayina awo anali Elifeleti, Yeiyeli ndi Semaya. Pamodzi ndi iwowa panalinso anthu 60.
abesizukulwane sika-Adonikhamu, abokucina, kwakungu-Elifelethi, uJuweli loShemaya, beza lamadoda angamatshumi ayisithupha;
14 Atsogoleri a fuko la Bigivai anali Utai ndi Zakuri. Pamodzi ndi iwowa panali anthu 70.
abesizukulwane sikaBhigivayi, kwakungu-Uthayi loZakhuri, abeza lamadoda angamatshumi ayisikhombisa.
15 Anthu onse ndinawasonkhanitsa ku mtsinje umene umapita mpaka ku Ahava, ndipo kumeneko tinagona mʼmisasa masiku atatu. Nditayangʼana pakati pa anthu ndi ansembe, ndinapeza kuti panalibe Alevi.
Ngababuthanisa eMgelweni wamanzi agelezela ku-Ahava, samisa khona okwensuku ezintathu. Ngathi sengihlola phakathi kwabantu labaphristi, kangitholanga loyedwa wamaLevi khona.
16 Choncho ndinayitana atsogoleri awa: Eliezara, Arieli, Semaiya, Elinatani, Yaribu, Elinatani, Natani, Zekariya ndi Mesulamu, pamodzi ndi aphunzitsi awiri, Yoyaribu ndi Elinatani,
Yikho ngasengibiza u-Eliyezari, lo-Ariyeli, loShemaya, lo-Elinathani, loJaribi, loNathani, loZakhariya loMeshulami ababengabakhokheli, loJoyaribi lo-Elinathani ababengabantu abafundileyo,
17 ndipo ndinawatuma kwa Ido, mtsogoleri wa malo otchedwa Kasifiya. Ine ndinawawuza zoti akanene kwa Ido ndi kwa abale ake, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu ku Kasifiyako, kuti atitumizire anthu odzatumikira ku Nyumba ya Mulungu.
ngabathumela ku-Ido, lezihlobo zakhe, izinceku zethempelini eKhasifiya, ukwenzela ukuthi basilethele izikhonzi zendlu kaNkulunkulu.
18 Chifukwa cha kutikomera mtima kwa Mulungu wathu, Ido anatitumizira munthu wanzeru, Serabiya, wa fuko la Mahili, mwana wa Levi, mwana wa Israeli, pamodzi ndi ana ake aamuna ndi abale ake, anthu 18.
Ngoba isandla somusa sikaNkulunkulu sasiphezu kwethu, basilethela uSherebhiya, indoda emadodeni, owesizukulwane sikaMahili indodana kaLevi, indodana ka-Israyeli, lamadodana kaSherebhiya labafowabo, amadoda alitshumi lasificaminwembili;
19 Anatitumiziranso Hasabiya ndi Yesaiya wa fuko la Merari pamodzi ndi abale ake ndi adzukulu ake, anthu makumi awiri.
loHashabhiya, kanye loJeshaya owesizukulwane sikaMerari, kanye labafowabo labantwababo, bonke babengamadoda angamatshumi amabili.
20 Panalinso anthu ena 220 mwa anthu ogwira ntchito mʼNyumba ya Mulungu amene Davide ndi nduna zake anawasankha kuti azitumikira Alevi. Anthu onsewa analembedwa potsata mayina awo.
Bona beza lezinceku zethempelini ezingamakhulu amabili lamatshumi amabili ezazimiswe nguDavida lezinduna zakhe ukuncedisa abaLevi. Bonke babhalwa phansi amabizo abo.
21 Ku mtsinje wa Ahava, ndinalengeza kuti anthu onse asale zakudya, adzichepetse pamaso pa Mulungu wathu ndi kupempha kuti atiyendetse bwino ife ndi ana athu, ndi kuteteza katundu wathu yense.
Khonapho, ekhunjini loMgelo we-Ahava, ngamemezela ukuzila ukudla, ukuze sizehlise phambi kukaNkulunkulu wethu simcele asiphe uhambo oluhle, thina labantwabethu, lempahla zethu zonke.
22 Ine ndinali ndi manyazi kupempha mfumu kuti atipatse asilikali oyenda pansi ndi ena okwera pa akavalo kuti atiteteze kwa adani athu pa ulendo wathuwu popeza tinali titawuza kale mfumu kuti “Yehova amateteza aliyense amene amamudalira, koma amakwiyira onse amene amamukana.”
Ngaba lenhloni ukucela enkosini amabutho labagadi bamabhiza ukuthi basivikele ezitheni endleleni ngoba inkosi sasiyitshele sathi, “Isandla somusa sikaNkulunkulu wethu siphezu kwakhe lowo okhangele kuye, kodwa ulaka lwakhe olukhulu luyavutha kulabo abamfulathelayo.”
23 Choncho tinasala zakudya ndi kupemphera kwa Mulungu wathu kuti atiteteze ndipo Iye anamva pemphero lathu.
Ngakho sazila ukudla, samncenga uNkulunkulu wethu ngakho lokhu, wawuphendula umkhuleko wethu.
24 Tsono ndinasankha atsogoleri a ansembe khumi ndi awiri awa, Serebiya, Hasabiya ndi abale awo khumi
Ngasengisehlukanisa kwabanye abaphristi abalitshumi lambili abangabakhokheli, ndawonye loSherebhiya, loHashabhiya labalitshumi labafowabo,
25 ndipo ndinawayezera siliva ndi golide, ndiponso ziwiya ndi zopereka za ku Nyumba ya Mulungu wathu zimene mfumu ndi alangizi ake, nduna zake ndi Aisraeli onse amene anali kumeneko anazipereka.
ngabalinganisela umnikelo wesiliva legolide lempahla ezaziyizipho ezasisuka enkosini, labacebisi bayo, lezikhulu zayo labako-Israyeli bonke ababekhona lapho, siyisipho sendlu kaNkulunkulu.
26 Nditayeza zonse, ndinapereka mʼmanja mwawo, matani 22 asiliva, ziwiya zasiliva zolemera makilogalamu 70, ndiponso makilogalamu 3,400 a golide,
Ngabalinganisela amathalenta angamakhulu ayisithupha lamatshumi amahlanu esiliva, impahla zesiliva ezilobunzima obungamathalenta alikhulu, amathalenta alikhulu egolide,
27 mbale zagolide makumi awiri zolemera makilogalamu asanu ndi atatu ndi theka ndiponso ziwiya ziwiri zamkuwa wosalala, wonyezimira bwino ngati golide wamtengowapatali.
imiganu yegolide engamatshumi amabili kuthiwa intengo yayo ingaba ngamadariki ayinkulungwane, lezitsha ezimbili ezethusi elilolongiweyo eliligugu njengegolide.
28 Kenaka ndinawawuza kuti, “Inu ndi opatulika a Yehova, ndiponso mphatso zonsezi ndi zopatulika. Siliva ndi golideyu ndi zopereka zaufulu kwa Yehova, Mulungu wa makolo anu.
Ngathi kubo, “Lina kanye lempahla lezi lingcwelisiwe eNkosini. Isiliva legolide kungumnikelo wokuzithandela kuThixo, uNkulunkulu wabokhokho benu.
29 Muzisamale bwino mpaka mutaziyeza pamaso pa atsogoleri a ansembe ndi Alevi ndi akulu a mabanja a Israeli mʼzipinda za mʼNyumba ya Mulungu ku Yerusalemu.”
Kulindeni ngonanzelelo lize liyokulinganisa emakamelweni endlu kaThixo eJerusalema phambi kwabakhokheli babaphristi lamaLevi labayizinhloko zezimuli zako-Israyeli.”
30 Choncho ansembe ndi Alevi analandira zonse zoyezedwa zija, siliva, golide pamodzi ndi ziwiya kuti apite nazo ku Nyumba ya Yehova ku Yerusalemu.
Kwathi-ke abaphristi labaLevi basemukela isiliva legolide lempahla ezingcwele ezazilinganisiwe ukuze zisiwe endlini kaNkulunkulu wethu eJerusalema.
31 Pa tsiku la khumi ndi chiwiri la mwezi woyamba, tinachoka ku mtsinje wa Ahava kupita ku Yerusalemu. Ndipo Mulungu wathu anali nafe, ndipo anatiteteza kwa adani athu makamaka otibisalira pa njira.
Ngosuku lwetshumi lambili lwenyanga yokuqala saphakama sasuka eMgelweni we-Ahava saqonda eJerusalema. Isandla sikaNkulunkulu wethu sasiphezu kwethu, wasivikela ezitheni lasezigebengwini indlela yonke.
32 Tinafika ku Yerusalemu, komwe tinapumula masiku atatu.
Ngakho safika eJerusalema, saphumula khona okwensuku ezintathu.
33 Pa tsiku la chinayi lake, mʼNyumba ya Mulungu wathu, tinayeza siliva ndi golide ndi ziwiya zija nʼkuzipereka mʼmanja mwa Meremoti mwana wa wansembe Uriya. Pamodzi ndi iyeyo panali Eliezara mwana wa Finehasi ndiponso Alevi awa: Yozabadi mwana wa Yesuwa ndi Nowadiya mwana wa Binuyi.
Ngosuku lwesine sangena endlini kaNkulunkulu salinganisa isiliva legolide lempahla zonke ezingcwelisiweyo sazibeka ezandleni zikaMeremothi indodana ka-Uriya umphristi. U-Eliyezari indodana kaFinehasi laye wayekhona, labaLevi oJozabhadi indodana kaJeshuwa loNowadiya indodana kaBhinuwi.
34 Zonsezi anaziwerenga ndi kuziyeza ndipo analemba kulemera kwa chinthu chilichonse.
Konke kwakukhona ngenani lakho langesisindo, kwathi isisindo sonke salotshwa phansi ngasonaleso isikhathi.
35 Pamenepo anthu amene anatengedwa ukapolo aja anabwerera, anapereka nsembe zopsereza kwa Mulungu wa Israeli: ngʼombe zazimuna khumi ndi ziwiri, kuperekera Aisraeli onse, nkhosa zazimuna 96, ana ankhosa 77, ndiponso mbuzi zazimuna khumi ndi ziwiri ngati nsembe yopepesera machimo. Zonsezi zinali nsembe yopsereza zopereka kwa Yehova.
Yikho izithunywa ezabuya ebugqilini zenza umnikelo wokutshiswa kuNkulunkulu ka-Israyeli: inkunzi ezilitshumi lambili ezika-Israyeli wonke, inqama ezingamatshumi ayisificamunwemunye lesithupha, amawundlu amaduna angamatshumi ayisikhombisa lesikhombisa kanye lomnikelo wesono oyizimpongo ezilitshumi lambili. Konke lokhu kwakungumnikelo wokutshiswa kuThixo.
36 Iwo anaperekanso chidziwitso cha mfumu chija kwa akuluakulu a mfumu ndi kwa akazembe a mʼdera la Patsidya pa Yufurate. Pamenepo iwo anathandiza Ayuda ndiponso ntchito za pa Nyumba ya Mulungu.
Bathi njalo bethula imilayo yenkosi kuzikhulu zenkosi lakubabusi bangaphetsheya kweYufrathe, okwathi-ke bona bancedisa abantu kanye lasendlini kaNkulunkulu.

< Ezara 8 >