< Ezara 8 >
1 Nawa mayina a atsogoleri a mabanja amene anabwera nane kuchokera ku Babuloni nthawi ya ulamuliro wa mfumu Aritasasita:
Pa inge inen sifen sou su muta in sruoh in Babylonia ac welul Ezra folokla nu Jerusalem ke pacl Artaxerxes el tokosra fulat:
2 Geresomu wa fuko la Finehasi; Danieli wa fuko la Itamara; Hatusi
Gershom ke fwil natul Phinehas Daniel ke fwil natul Ithamar Hattush, wen natul Shecaniah, ke fwil natul David
3 mwana wa Sekaniya wa fuko la Davide; Zekariya wa fuko la Parosi. Pamodzi ndi iyeyu panalembedwa anthu ena 150;
Zechariah ke fwil natul Parosh wi mwet 150 ke sou lulap lal (simisyukla inen mwet in sou lalos ke sramsram matu)
4 Elihunai mwana wa Zerahiya, wa fuko la Pahati-Mowabu. Pamodzi ndi iyeyu panalinso anthu ena 400.
Eliehoenai, wen natul Zerahiah, ke fwil natul Pahath Moab, wi mukul 200
5 Sekaniya, mwana wa Yahazieli wa fuko la Zatu. Pamodzi ndi iyeyu panalembedwanso anthu 300.
Shecaniah, wen natul Jahaziel, ke fwil natul Zattu, wi mukul 300
6 Ebedi, mwana wa Yonatani wa fuko la Adini. Pamodzi naye analembedwanso anthu ena makumi asanu.
Ebed, wen natul Jonathan, ke fwil natul Adin, wi mukul 50
7 Yesaiya, mwana wa Ataliya wa fuko la Elamu. Pamodzi naye panali anthu ena 70.
Jeshaiah, wen natul Athaliah, ke fwil natul Elam, wi mukul 70
8 Zebadiya, mwana wa Mikayeli wa fuko la Sefatiya. Pamodzi naye panalinso anthu 80.
Zebadiah, wen natul Michael, ke fwil natul Shephatiah, wi mukul 80
9 Obadiya, mwana wa Yehieli wa fuko la Yowabu. Pamodzi naye panalinso anthu 218.
Obadiah, wen natul Jehiel, ke fwil natul Joab, wi mukul 218
10 Selomiti mwana wa Yosifiya wa fuko la Bani. Pamodzi ndi iyeyu panalinso anthu 160.
Shelomith, wen natul Josiphiah, ke fwil natul Bani, wi mukul 160
11 Zekariya, mwana wa Bebai wa fuko la Babai. Pamodzi naye analembedwanso anthu 28.
Zechariah, wen natul Bebai, ke fwil natul Bebai, wi mukul 28
12 Yohanani, mwana wa Hakatani wa fuko la Azigadi. Pamodzi naye panalinso anthu 110.
Johanan, wen natul Hakkatan, ke fwil natul Azgad, wi mukul 110
13 Atsogoleri a fuko la Adonikamu, anthu amene anabwera pambuyo pake mayina awo anali Elifeleti, Yeiyeli ndi Semaya. Pamodzi ndi iwowa panalinso anthu 60.
Eliphelet, Jeuel, ac Shemaiah ke fwil natul Adonikam, wi mukul 60, (elos folokla ke sie pacl tok)
14 Atsogoleri a fuko la Bigivai anali Utai ndi Zakuri. Pamodzi ndi iwowa panali anthu 70.
Uthai ac Zaccur ke fwil natul Bigvai, wi mukul 70
15 Anthu onse ndinawasonkhanitsa ku mtsinje umene umapita mpaka ku Ahava, ndipo kumeneko tinagona mʼmisasa masiku atatu. Nditayangʼana pakati pa anthu ndi ansembe, ndinapeza kuti panalibe Alevi.
Nga orani u nufon sac nu pe inyoa soko ma sasla nu Ahava, ac kut aktuktuk we len tolu. Nga konauk lah oasr mwet tol in u sac, a wangin mwet Levi.
16 Choncho ndinayitana atsogoleri awa: Eliezara, Arieli, Semaiya, Elinatani, Yaribu, Elinatani, Natani, Zekariya ndi Mesulamu, pamodzi ndi aphunzitsi awiri, Yoyaribu ndi Elinatani,
Nga sapla suli eu sin mwet kol lalos: Eliezer, Ariel, Shemaiah, Elnathan, Jarib, Elnathan, Nathan, Zechariah, ac Meshullam, oayapa luo mwet luti: Joiarib ac Elnathan.
17 ndipo ndinawatuma kwa Ido, mtsogoleri wa malo otchedwa Kasifiya. Ine ndinawawuza zoti akanene kwa Ido ndi kwa abale ake, ogwira ntchito ku Nyumba ya Mulungu ku Kasifiyako, kuti atitumizire anthu odzatumikira ku Nyumba ya Mulungu.
Nga supwalosla nu yorol Iddo, su leumi acn Casiphia, in siyuk sel ac mwet kasru lal su orekma ke Tempul, tuh elos in supwama mwet in kulansap nu sin God in Tempul.
18 Chifukwa cha kutikomera mtima kwa Mulungu wathu, Ido anatitumizira munthu wanzeru, Serabiya, wa fuko la Mahili, mwana wa Levi, mwana wa Israeli, pamodzi ndi ana ake aamuna ndi abale ake, anthu 18.
Ke lungkulang lun God, elos supwalma Sherebiah, sie mwet fas, su mwet Levi se in fwil natul Mahli; ac mukul singoul oalkosr sin wen natul ac tamulel lal welul tuku.
19 Anatitumiziranso Hasabiya ndi Yesaiya wa fuko la Merari pamodzi ndi abale ake ndi adzukulu ake, anthu makumi awiri.
Elos oayapa supwalma Hashabiah ac Jeshaiah ke fwil natul Merari, wi mwet longoul sin mwet laltal.
20 Panalinso anthu ena 220 mwa anthu ogwira ntchito mʼNyumba ya Mulungu amene Davide ndi nduna zake anawasankha kuti azitumikira Alevi. Anthu onsewa analembedwa potsata mayina awo.
Sayen mwet inge, oasr luofoko longoul mwet orekma ke Tempul su mwet matu lalos tuh srisrngiyuki sel Tokosra David ac mwet pwapa lal tuh elos in kasru mwet Levi. Simisyukla inelos kais sie.
21 Ku mtsinje wa Ahava, ndinalengeza kuti anthu onse asale zakudya, adzichepetse pamaso pa Mulungu wathu ndi kupempha kuti atiyendetse bwino ife ndi ana athu, ndi kuteteza katundu wathu yense.
Ingo sisken Inyoa Ahava, nga sapkin tuh kut nukewa in lalo ac akpusiselye kut ye mutun God lasr, ac siyuk sel tuh Elan kol kut ke fahsr lasr ac lisringkuti ac tulik natusr ac ma lasr nukewa.
22 Ine ndinali ndi manyazi kupempha mfumu kuti atipatse asilikali oyenda pansi ndi ena okwera pa akavalo kuti atiteteze kwa adani athu pa ulendo wathuwu popeza tinali titawuza kale mfumu kuti “Yehova amateteza aliyense amene amamudalira, koma amakwiyira onse amene amamukana.”
Nga lukun mwekin in siyuk sin tokosra fulat ke sie u in mwet mweun ma kasrusr fin horse in karingin kut ke fufahsryesr lasr liki kutena mwet lokoalok, mweyen nga fahk nu sel tari lah God lasr El akinsewowoyalos nukewa su lulalfongi El, a El lain ac kalyei kutena su forla lukel.
23 Choncho tinasala zakudya ndi kupemphera kwa Mulungu wathu kuti atiteteze ndipo Iye anamva pemphero lathu.
Ouinge kut lalo ac pre tuh God Elan karingin kut, ac El topuk pre lasr.
24 Tsono ndinasankha atsogoleri a ansembe khumi ndi awiri awa, Serebiya, Hasabiya ndi abale awo khumi
Inmasrlon mwet tol su fulat, nga tuh sulella Sherebiah, Hashabiah, ac mwet singoul saya.
25 ndipo ndinawayezera siliva ndi golide, ndiponso ziwiya ndi zopereka za ku Nyumba ya Mulungu wathu zimene mfumu ndi alangizi ake, nduna zake ndi Aisraeli onse amene anali kumeneko anazipereka.
Na nga pauniya silver, gold ac ahlu in kulansap ma tokosra fulat, mwet pwapa ac mwet fulat lal oayapa mwet Israel nukewa elos tuh sang in orekmakinyuk in Tempul, ac nga sang nu sin mwet tol.
26 Nditayeza zonse, ndinapereka mʼmanja mwawo, matani 22 asiliva, ziwiya zasiliva zolemera makilogalamu 70, ndiponso makilogalamu 3,400 a golide,
Pa inge ma nga sang nu selos: silver — ton 25 100 ahlu silver, kufwen mwe orekma — paun 150 gold — paun 7,500
27 mbale zagolide makumi awiri zolemera makilogalamu asanu ndi atatu ndi theka ndiponso ziwiya ziwiri zamkuwa wosalala, wonyezimira bwino ngati golide wamtengowapatali.
20 ahlu gold — paun 16 tafu 2 ahlu bronze wowo — lupan molo uh oana molin ahlu gold.
28 Kenaka ndinawawuza kuti, “Inu ndi opatulika a Yehova, ndiponso mphatso zonsezi ndi zopatulika. Siliva ndi golideyu ndi zopereka zaufulu kwa Yehova, Mulungu wa makolo anu.
Nga fahk nu selos, “Kowos mutal ye mutun LEUM GOD lun mwet matu lowos, ac oayapa ahlu silver ac gold su itukyang nu sel ke insewowo, ma inge mutal pac.
29 Muzisamale bwino mpaka mutaziyeza pamaso pa atsogoleri a ansembe ndi Alevi ndi akulu a mabanja a Israeli mʼzipinda za mʼNyumba ya Mulungu ku Yerusalemu.”
Kowos karinganang akwoya nwe ke kowos sun Tempul. Kowos pauniya ma inge infukil lun mwet tol, ac sang nu sin mwet kol lun mwet tol ac mwet Levi, ac nu sin mwet kol lun Israel in Jerusalem.”
30 Choncho ansembe ndi Alevi analandira zonse zoyezedwa zija, siliva, golide pamodzi ndi ziwiya kuti apite nazo ku Nyumba ya Yehova ku Yerusalemu.
Ke ma inge mwet tol ac mwet Levi elos eis ac fosrngakin silver, gold, ac kufwen mwe orekma, ac elos usla nu in Tempul Jerusalem.
31 Pa tsiku la khumi ndi chiwiri la mwezi woyamba, tinachoka ku mtsinje wa Ahava kupita ku Yerusalemu. Ndipo Mulungu wathu anali nafe, ndipo anatiteteza kwa adani athu makamaka otibisalira pa njira.
Len se aksingoul luo ke malem se meet pa kut mukuiyak liki Inyoa Ahava in som nu Jerusalem. God lasr El wi kut ac karingin kut liki mwet lokoalok ac liki mwet su akola in kasriki kut inkanek ah.
32 Tinafika ku Yerusalemu, komwe tinapumula masiku atatu.
Ke kut sun acn Jerusalem, kut muta mongla len tolu.
33 Pa tsiku la chinayi lake, mʼNyumba ya Mulungu wathu, tinayeza siliva ndi golide ndi ziwiya zija nʼkuzipereka mʼmanja mwa Meremoti mwana wa wansembe Uriya. Pamodzi ndi iyeyo panali Eliezara mwana wa Finehasi ndiponso Alevi awa: Yozabadi mwana wa Yesuwa ndi Nowadiya mwana wa Binuyi.
Na len se akakosr kut som nu ke Tempul, pauniya silver, gold, ac kufwen mwe orekma, na kut sang nu sel Meremoth mwet tol, wen natul Uriah. Mwet tolu welul pa: Eleazar wen natul Phinehas, ac mwet Levi luo, Jozabad wen natul Jeshua, ac Noadiah wen natul Binnui.
34 Zonsezi anaziwerenga ndi kuziyeza ndipo analemba kulemera kwa chinthu chilichonse.
Ma nukewa oaoala ac paunyuki, ac simla in pacl sac pacna.
35 Pamenepo anthu amene anatengedwa ukapolo aja anabwerera, anapereka nsembe zopsereza kwa Mulungu wa Israeli: ngʼombe zazimuna khumi ndi ziwiri, kuperekera Aisraeli onse, nkhosa zazimuna 96, ana ankhosa 77, ndiponso mbuzi zazimuna khumi ndi ziwiri ngati nsembe yopepesera machimo. Zonsezi zinali nsembe yopsereza zopereka kwa Yehova.
Na mwet nukewa su foloko liki sruoh elos use mwe sang lalos tuh in mwe kisa firir nu sin God lun Israel. Elos sang cow mukul 12 ke Israel nufon, wi sheep mukul 96, ac sheep fusr 77. Elos oayapa sang nani 12 mwe aknasnasyalos liki ma koluk. Ma inge nukewa mwe kisa firir nu sin LEUM GOD.
36 Iwo anaperekanso chidziwitso cha mfumu chija kwa akuluakulu a mfumu ndi kwa akazembe a mʼdera la Patsidya pa Yufurate. Pamenepo iwo anathandiza Ayuda ndiponso ntchito za pa Nyumba ya Mulungu.
Elos oayapa usla leta se ma tokosra fulat el tuh sang nu selos ac sang nu sel governor ac mwet pwapa lun acn Roto-in-Euphrates, na mwet inge elos oru pac kasru lalos nu sin mwet uh ac nu ke alu in Tempul.