< Ezara 5 >
1 Nthawi imeneyo aneneri Hagai ndi Zekariya, mwana wa Ido, ankayankhula kwa Ayuda okhala mʼdziko la Yuda ndi mu Yerusalemu mʼdzina la Mulungu wa Israeli, amene anali nawo.
Te vaengah tonghma Haggai neh tonghma Iddo capa Zekhariah te tonghma rhoi. Amih rhoi tah a soah Israel Pathen ming a phuk thil Judah neh Jerusalem kah Yahudi tonghma rhoek ni.
2 Pambuyo pake Zerubabeli mwana wa Sealatieli ndi Yesuwa mwana wa Yozadaki ananyamuka nakayambanso kumanga Nyumba ya Mulungu mu Yerusalemu. Ndipo aneneri a Mulungu anali nawo pamodzi, kuwathandiza.
Te vaengah Shaeltiel capa Zerubbabel neh Jozadak capa Jeshua te thoo tih Jerusalem kah Pathen im sak ham te a tong uh. Pathen tonghma rhoek khaw amih rhoi taengah om tih amih rhoi te a bom uh.
3 Pa nthawi imeneyo Tatenai, bwanamkubwa wa chigawo cha patsidya pa Yufurate pamodzi ndi Setari-Bozenai ndi anzawo anapita kwa iwo ndi kukawafunsa kuti, “Anakulolani ndani kuti mumangenso Nyumba imeneyi ndi kutsiriza khoma lake?”
Te vaeng tue ah amih taengla sok paem boei Tattenai, Shetharboznai neh a hui rhoek te cet. Te phoeiah amih te, “He im sak ham neh he imbang coeng ham nangmih taengah saithainah aka pae te unim?
4 Anawafunsanso kuti, “Kodi anthu amene akumanga nyumbayi mayina awo ndani?”
He im aka sa hlang rhoek ming te amih taengah ka thui uh bal coeng,” a ti uh.
5 Koma Mulungu wawo amayangʼanira atsogoleri Ayuda, motero kuti anthu aja anaganiza kuti asawaletse kumanga Nyumbayo mpaka atalembera mfumu Dariyo kalata ndi kulandira yankho lake.
Tedae amih kah Pathen mik loh Yahudi a hamca rhoek a om thil dongah Darius taengla hlangcal pawk tih te ham te ca a mael hlan hil amih te paa sak pawh.
6 Iyi ndi kalata imene Tatenai bwanamkubwa wa dera la patsidya pa Yufurate, ndiponso Setari-Bozenai ndi anzake, akazembe amene anali mʼchigawo cha patsidya pa Yufurate, anatumiza kwa mfumu Dariyo
Sok paem boei Tattenai, Shetharboznai neh a hui rhoek, sok paem kah boei rhoek loh Darius manghai taengla ca tlaep te a pat.
7 Analemba kalatayo motere: Kwa mfumu Dariyo: Mukhale ndi mtendere wonse.
Anih taengla ol a pat uh vaengah a khui ah he tlam he a daek. Darius manghai taengah ngaimongnah boeih om saeh.
8 Amfumu mudziwe kuti ife tinapita ku dziko la Yuda ku Nyumba ya Mulungu wamkulu. Nyumbayo ikumangidwa ndi miyala ikuluikulu ndipo akuyala matabwa pa makoma. Ntchitoyi ikugwiridwa mwachangu ndipo ikuyenda bwino kwambiri mwautsogoleri wawo.
Judah paeng kah boeilen Pathen im la ka caeh te manghai taengah mingpha saeh. Te te lung nu a sak uh tih thoh khuiah thing neh a pae. Imsak he tluem tluem a saii tih a kut dongah bi khaw song.
9 Ndipo tinawafunsa atsogoleriwo kuti, “Anakulolezani kuti mumangenso Nyumbayi ndi kutsiriza makoma ake ndani?”
A hamca rhoek te ka dawt tangloeng bal tih amih te, “He im sak ham neh imbang he coeng ham nangmih taengah saithainah aka pae te unim?” ka ti uh.
10 Tinawafunsanso mayina a atsogoleri awo, kuti tikalemba mayina atsogoleriwo tidzakudziwitseni kuti muwadziwe.
Nang taengah mingpha sak ham amih te a ming khaw ka dawt uh. Amih lu soah hlang rhoek ming te khaw ka daek uh hamla.
11 Yankho limene anatipatsa ndi ili: “Ife ndife atumiki a Mulungu wa kumwamba ndi wa dziko lapansi, ndipo tikumanganso Nyumba imene mfumu ina yamphamvu ya Israeli inamanga ndi kuyitsiriza zaka zambiri zapitazo.
Tedae ol te kaimih taengla ham mael uh tih amamih te, “Kaimih tah vaan neh diklai Pathen kah a tueihyoeih rhoek ni. Im a sak he hlamat kum a yet lamloh sak tangtae om coeng. Israel kah manghai boeilen loh a sak tih a coeng.
12 Koma chifukwa chakuti makolo athu anakwiyitsa Mulungu wakumwamba, Iye anawapereka kwa Nebukadinezara Mkalideya, mfumu ya Babuloni, amene anawononga Nyumbayi ndi kutenga anthu onse kupita nawo ku ukapolo ku Babuloni.
Tedae a pa rhoek loh vaan Pathen te a veet uh lamloh amih te Khalden kah Babylon manghai Nebukhadnezzar kut ah a paek. Te vaengah im he a khaih tih pilnam he Babylon la a khuen.
13 “Komabe chaka choyamba cha Koresi, mfumu ya ku Babuloni, mfumu Koresiyo anapereka lamulo lakuti Nyumba ya Mulunguyi imangidwenso.
Babylon manghai Cyrus kah kah kum ah tah manghai Cyrus loh Pathen im he sak hamla saithainah a paek.
14 Ndipo ziwiya zagolide ndi zasiliva za ku Nyumba ya Mulungu zimene Nebukadinezara anazitenga mʼNyumba ya Mulungu ku Yerusalemu ndi kukaziyika mʼnyumba ya milungu ya ku Babuloni, anakazichotsa ku nyumba ya milungu ya ku Babuloniko ndi kuzipereka kwa Sesibazara, amene mfumu inamusankha kukhala bwanamkubwa.
Pathen im kah hnopai pataeng sui neh cak khaw Jerusalem bawkim lamkah te, Nebukhadnezzar loh a loh tih Babylon kah bawkim la a khuen. Te te Cyrus manghai loh Babylon bawkim lamkah a loh. Te phoeiah a ming Sheshbazzar la a khue tih boei la a khueh taengah a paek uh.
15 Tsono mfumuyo inamuwuza kuti, ‘Tenga ziwiyazi ukaziyike mʼNyumba ya Mulungu ku Yerusalemu. Ndipo Nyumba ya Mulunguyo ikamangidwenso pa maziko ake akale.’
Te phoeiah anih te, “Hnopai he khuen lamtah cet laeh. Te Jerusalem kah bawkim ah khueh laeh. Pathen im khaw amah hmuen ah sa saeh,” a ti nah.
16 “Choncho Sesibazarayo anabwera ndi kumanga maziko a Nyumba ya Mulunguyo mu Yerusalemu. Kuyambira tsiku limenelo mpaka lero yakhala ikumangidwa ndipo sinathebe.”
Sheshbazzar cet tangloeng tih Jerusalem kah Pathen im te khoengim a tloeng. Te lamlong tah tahae hil a sak uh dae coeng uh pawh.
17 Nʼchifukwa chake ngati chingakukomereni amfumu, pachitike kafukufuku mʼnyumba yaufumu mosungira chuma ndi mabuku okhudza mbiri ya Babuloni kuti tione ngati mfumu Koresi inalamuladi za kumanganso Nyumba ya Mulungu mu Yerusalemu. Kenaka amfumu mutiwuze zomwe zikukondweretsani kuti mugamule pa nkhani imeneyi.
Manghai ham khaw a ngaih coeng mak atah Babylon manghai kah cabu im kah te pahoi thoelh saeh. Jerusalem ah Pathen im sak hamla manghai Cyrus lamloh saithainah a paek te a om khaming. Te dongah manghai kah a ngaihnah mah kaimih taengla ham pat saeh.