< Ezara 3 >

1 Utafika mwezi wa chisanu ndi chiwiri Aisraeli atakhala kale mʼmidzi yawo, anthu anasonkhana ku Yerusalemu ndi cholinga chimodzi.
A HIKI mai ka hiku o ka malama, a e noho ana na mamo a Iseraela ma na kulanakauhale, hoakoakoaia ae la na kanaka me he kanaka hookahi la ma Ierusalema.
2 Kenaka Yesuwa mwana wa Yozadaki ndi ansembe anzake pamodzi ndi Zerubabeli mwana wa Sealatieli ndi abale ake anayamba kumanga guwa lansembe la Mulungu wa Israeli. Anatero pofuna kuti aziperekapo nsembe zopsereza monga analembera mʼbuku la Mose, munthu wa Mulungu uja.
Alaila ku ae la o Iesua ke keiki a Iozadaka, a me kona mau hoahanau, na kahuna, a o Zerubabela ke keiki a Sealetiela, a me kona poe hoahanau, hana lakou i ke kuahu no ke Akua o ka Iseraela, e kaumaha aku i na mohaikuni maluna ona, e like me ka palapala ma ke kanawai o Mose ke kanaka no ke Akua.
3 Ndi mantha ndi mantha chifukwa cha anthu a mʼmayikomo, iwo anamanga guwalo pa maziko ake akale, ndipo anapereka nsembe zopsereza kwa Mulungu pa guwapo mmawa ndi madzulo.
A kau aku la lakou i ke kuahu maluna o kona mau kahua, no ka mea, ua kau mai ka makau maluna o lakou no na kanaka o na aina e; a kaumaha aku maluna ona i na mohaikuni ia Iehova, i na mohaikuni no kakahiaka a no ke ahiahi.
4 Ankasunga tsiku la chikondwerero cha misasa monga momwe zinalembedwera. Ankaperekanso nsembe za tsiku ndi tsiku monga mwa chiwerengero chake potsata mwambo wake wa tsiku ndi tsiku monga zinalembedwa.
A malama lakou i ka ahaaina kauhalelewa, e like me ka palapala, a kaumaha aku i ka mohaikuni no kela la keia la, me ka helu ana, e like me ka hana mau no kela la keia la.
5 Pambuyo pake, ankapereka nsembe zopsereza, nsembe zopereka pa nthawi ya mwezi watsopano ndi za pa masiku onse a chikondwerero oyikidwa kutamandira Yehova, kudzanso nsembe zaufulu zopereka kwa Yehova.
A mahope o ia mea, i ka mohaikuni hoomau, no na mahina hou a no na ahaaina a pau na Iehova i hoolaaia, a no na mea a pau i mohai oluolu aku ai i ka mohai aloha no Iehova.
6 Kuyambira pa tsiku loyamba la mwezi wachisanu ndi chiwiri, iwo anayambanso kupereka nsembe zopsereza kwa Yehova, ngakhale kuti maziko a Nyumba ya Yehova anali asanamangidwe.
Mai ka la mua o ka hiku o ka malama ko lakou hoomaka ana e kaumaha aku i na mohaikuni ia Iehova. Aka, o ka luakini o Iehova aole i hookumuia.
7 Ndipo anapereka ndalama kwa amisiri a miyala ndi kwa amisiri a matabwa, ndi chakudya, chakumwa ndi mafuta kwa anthu a ku Sidoni ndi a ku Turo, kuti abweretse mitengo ya mkungudza pa nyanja kuchokera ku Lebanoni mpaka ku Yopa. Zonsezi anachita malinga ndi chilolezo chimene analandira kuchokera kwa Koresi, mfumu ya Peresiya.
A haawi aku la lakou i ke kala no ka poe kalai pohaku, a no ka poe paahana; a me ka ai hoi, a me ka mea inu, a me ka aila ua ko Zidona, a na ko Turo, i lawe mai lakou i na laau kedara mai Lebanona mai a ke kai o Iopa, e like me ka mea a Kuro ke alii o Peresia i ae mai ai ia lakou.
8 Tsono mu chaka chachiwiri atabwera ku Yerusalemu, ku malo akale a Nyumba ya Yehova, mwezi wachiwiri Zerubabeli mwana wa Sealatieli, Yesuwa mwana wa Yozadaki pamodzi ndi abale awo onse, ansembe, Alevi ndi onse amene anabwera ku Yerusalemu kuchokera ku ukapolo, anayamba kugwira ntchito. Iwo anasankha Alevi a zaka zoyambira makumi awiri kuti aziyangʼanira ntchito ya kumanga Nyumba ya Yehova.
A i ka lua o ka makahiki o ko lakou hele ana mai i ka hale o ke Akua ma Ierusalema, i ka lua o ka malama, i hoomaka ai o Zerubabela ke keiki a Sealetiela, a o Iesua ke keiki a Iozadaka, a me ke koena o ko lakou poe hoahanau na kahuna, a me ua Levi, a me ka poe a pau i hele mai, mai ke pio ana mai a Ierusalema; a hoonoho i na Levi, mai ka iwakalua o na makahiki a i keu aku, i nana lakou i ka hana o ka hale no Iehova.
9 Yesuwa ndi ana ake aamuna kudzanso abale ake, Kadimieli ndi ana ake (ana a Yuda) onse pamodzi anasenza udindo woyangʼanira antchito ku Nyumba ya Mulungu, kuphatikizanso ana a Henadadi komanso Alevi, ana awo ndi abale awo.
Ku pu ae la o Iesua me kana poe keiki, a me kona poe hoahanau, o Kademiela a me kana mau keiki, no na keiki a Iuda, e nana aku maluna o ka poe paahana ma ka hale o ke Akua; o na keiki hoi a Henadada, me ka lakou poe keiki, a me ko lakou mau hoahanau, o na Levi.
10 Amisiri omanga nyumba atamanga maziko a Nyumba ya Yehova, ansembe anabwera akuyimba malipenga, atavala zovala zaunsembe. Ndipo Alevi, zidzukulu za Asafu, anadza akuyimba matambolini ndi kutenga udindo wawo wotamanda Yehova, potsata malangizo a Davide mfumu ya Aisraeli.
A i ka wa i hookumu ai ka poe hana hale i ka luakini o Iehova, hoonoho lakou i na kahuna i kahikoia me na pu, a me na Levi, na keiki a Asapa, me na kimehala, e hoolea aku ia Iehova, e like me ka mea a Davida ke alii o ka Iseraela i kauoha ai.
11 Iwo ankayimba motamanda ndi mothokoza Yehova nyimbo iyi: “Yehova ndi wabwino; chikondi chake pa Israeli ndi chamuyaya.” Ndipo anthu onse ankafuwula kwambiri kumutamanda Yehova, chifukwa maziko a Nyumba ya Yehova anali kumangidwa.
A mele aku lakou me ka hoolea ana, a me ka hoomaikai ana ia Iehova; No ka mea, he maikai oia, a he mau loa kona aloha i ka Iseraela. A hooho ae la na kanaka a pau me ka hooho nui, i ko lakou hoolea ana ia Iehova no ka hookumu ana i ka hale o Iehova.
12 Koma ambiri mwa ansembe, Alevi ndiponso atsogoleri amabanja, akuluakulu amene anaona Nyumba ya Yehova yakale, analira mokweza pamene anaona maziko a nyumbayi akumangidwa. Komanso ena ambiri ankafuwula mosangalala.
Aka, nui na kahuna, a me na Levi, a me ka poe koikoi o na makua, o na mea kahiko, na mea i ike i ka hale mua, i ka hookumu ana o keia hale imua o ko lakou maka, auwe iho la lakou me ka leo nui; a nui no hoi ka poe i hooho me ka leo kiekie no ka olioli.
13 Choncho panalibe amene ankatha kusiyanitsa liwu lofuwula mokondwerera ndi liwu la anthu olira, chifukwa anthuwo ankafuwula kwambiri. Ndipo liwu lofuwulalo limamveka kutali.
Nolaila aole i hiki i na kanaka ke hookaawale i ka leo o ka hooho olioli ana a me ka leo o ka uwe ana o na kanaka; no ka mea, ua hooho na kanaka me ka hooho nui, a ua loheia ka leo ma kahi loihi.

< Ezara 3 >