< Ezekieli 1 >

1 Tsiku lachisanu la mwezi wachinayi, chaka cha makumi atatu, ine ndinali pakati pa amʼndende mʼmbali mwa mtsinje wa Kebara. Tsono kumwamba kunatsekuka ndipo ndinaona maonekedwe a Mulungu mʼmasomphenya.
Ke len aklimekosr in malem akakosr in yac aktolngoul, nga Ezekiel, sie mwet tol, wen natul Buzi, wi mwet Jew ma sruoh su muta sisken Infacl Chebar in acn Babylonia. Kusrao ikakla ac nga liye sie aruruma ke God.
2 Pa tsiku lachisanu la mwezi, chaka chachisanu Yehoyakini ali mʼndende,
(Yac aklimekosrla tukun utukla Tokosra Jehoiachin nu ke sruoh.)
3 Yehova anayankhula ndi wansembe Ezekieli, mwana wa Buzi, mʼmbali mwa mtsinje wa Kebara mʼdziko la Ababuloni. Dzanja la Yehova linali pa iye kumeneko.
Ingo, sisken Infacl Chebar in acn Babylonia, nga tuh lohng ke LEUM GOD El kaskas nu sik, ac nga pulakin ku lal oan fuk.
4 Ndinayangʼana ndipo ndinangoona mphepo yamkuntho ikubwera kuchokera kumpoto. Panali mtambo waukulu wozunguliridwa ndi kuwala ndipo moto unali lawilawi kuchokera mu mtambowo. Pakati pa motowo pankaoneka ngati mkuwa wonyezimira.
Nga ngetak ac liye sie fohru tuku epang me. Sarom uh sarmelik liki sie pukunyeng lulap, ac yen nukewa rauneak arulana saromrom. Yen ma sarom uh sarmelik we, oasr sie ma saromrom oana osra bronze.
5 Mʼkatikati mwa motowo munali zinthu zinayi zamaonekedwe a nyama. Thupi lawo limaoneka ngati la munthu
Infulwen paka sac nga liye ma orekla akosr su moul, su oana luman mwet,
6 koma chilichonse chinali ndi nkhope zinayi ndiponso mapiko anayi.
tusruktu kais sie selos oasr muta akosr ac posohksok akosr.
7 Miyendo yake inali yowongoka; mapazi ake anali a ziboda ngati phazi la mwana wangʼombe. Ndipo zibodazo zinkawala ngati mkuwa wonyezimira.
Nialos suwohs, ac falkalos oana falken cow mukul uh, su saromrom oana bronze aksaromromyeyukla.
8 Mʼmunsi mwa mapiko awo kumbali zonse zinayi, nyamazo zinali ndi manja a munthu. Zonse zinayi zinali ndi nkhope ndi mapiko,
Sayen muta akosr ac posohksok akosr, oasr pac kais sie poun mwet ye posohksok kaclos.
9 ndipo mapiko awowo anakhudzana. Chilichonse chimapita molunjika kutsogolo; sizimatembenuka pamene zimayenda.
Kais sie ma moul inge elos foralik ac asroelik luo sin posohksok kaclos in akupasrila orala maspang se. Ke elos ac mukuila elos ac tukeni mukuiyak, a manolos tiana forla.
10 Nkhope zawo zimaoneka motere: Chilichonse chinali ndi nkhope ya munthu, ndipo mbali ya kumanja chilichonse chinali ndi nkhope zinayi zosiyana motere: nkhope ya munthu, nkhope ya mkango ku dzanja lamanja, nkhope ya ngʼombe ku dzanja lamanzere, ndipo kumbuyo kwake nkhope ya chiwombankhanga.
Kais sie ma moul akosr inge oasr muta akosr kac su tiana oana sie: mutun mwet se nget nu meet, mutun lion nget nu layot, mutun cow mukul nget nu lasa, ac mutun eagle nget nu tok.
11 Ndi mʼmene zinalili nkhope zawo. Mapiko awo anali otambasukira mmwamba. Chamoyo chilichonse chinali ndi mapiko awiri okhudzana ndi mapiko a chinzake. Chinalinso ndi mapiko ena awiri ophimbira thupi lake.
Luo posohksok ke kais sie ma moul inge asrosrelik in apusralila nu ke ma soko siska lac lac, ac posohksol lula elos sang afinya manolos.
12 Zamoyozo zinkayenda molunjika kutsogolo. Kulikonse kumene mzimu umazitsogolera kupita, nazonso zimapita kumeneko, osatembenuka pamene zikupita.
Kais soko ma moul inge nget nu ke eng akosr lun faclu, ouinge u sac ku in fahsr nu yen nukewa, ac tia enenu in forla.
13 Pakati pa zamayozo panali chinthu chooneka ngati makala oyaka kapena miyuni yoyaka. Moto umayendayenda pakati pa zamayozo; wowala kwambiri, ndipo mphenzi zimatuluka pakati pawo.
Inmasrlon ma moul inge oasr ma se oana sukan sul soko su mukuiwot mukuime pacl nukewa, ac e kac uh ngutyak, pusrukla sarom.
14 Zamoyozo zinkathamanga uku ndi uko ngati kungʼanima kwa mphenzi.
Ma moul inge yuwot yume, wi na mui lun sarom uh.
15 Pamene ndinali kuyangʼana zamoyozo, ndinangoona mikombero ndipo pansi pambali pa chamoyo chilichonse panali mkombero umodzi.
Ke nga ngetang nu ke ma orekla moul akosr inge, nga liyauk wheel akosr pusralla infohk uh, kais sie wheel oan sisken kais soko selos.
16 Maonekedwe a mikomberoyo anali ngati mwala wonyezimira. Mikombero yonse inali yofanana ndipo mapangidwe awo anali ngati wongolowanalowana.
Wheel inge kewa oana sie — kais sie selos saromrom oana luman wek saok uh, ac kais sie wheel oasr pac sie wheel pitukelik loac.
17 Mikombero ija poyenda inkatha kupita mbali iliyonse yomwe zamoyozo zinayangʼana popanda kutembenuka.
Ouinge wheel uh ku in mukui nu ke eng akosr inge kewa.
18 Marimu a mikomberoyo anali aatali ndi ochititsa mantha ndipo marimu onse anayi anali ndi maso ponseponse.
Sisken acn raun ke wheel inge nwanala ke atronmuta.
19 Zamoyozo zinkati zikamayenda, mikomberoyo imayendanso mʼmbali mwake; ndipo zamoyozo zinkati zikamakwera mmwamba, mikomberoyo imakweranso.
Pacl nukewa ma moul inge ac mukuila, na wheel inge ac mukuiyak pac, ac ma moul inge fin sohkak liki faclu, na wheel inge ac wi pac sohkak.
20 Kulikonse kumene mzimu wake unkazitsogolera, zamoyozo zinkapita komweko. Ndipo mikombero ija inkapita nawo pamodzi popeza kuti mzimu wa zamoyozo ndiwo umayendetsa mikombero ija.
Ma moul inge som nu yen nukewa elos lungse som nu we, ac wheel inge ac wi pacna, mweyen ma moul uh pa leum faclos.
21 Zamoyo zija zinkati zikamayenda mikombero imayendanso. Zamoyozo zimati zikayima, nayonso mikombero inkayima. Zamoyozo zinkati zikawuluka, mikomberonso imawuluka nazo pamodzi chifukwa mzimu wa zamoyo zija ndiwo umayendetsa mikombero ija.
Ouinge pacl nukewa ma moul inge mukuila ku tui ku sohkak nu yen engyeng uh, na wheel inge ac oru oapana.
22 Pamwamba pa mitu ya zamoyozo panali chinthu chonga thambo, lowala ndipo kunyezimira kwake ngati galasi loyangʼanitsa ku dzuwa, loyalidwa pamwamba pa mitu yake.
Lucng liki sifen ma moul inge, oasr sie ma raun oana luman sie pol lulap oankiyuki, orekla ke crystal na saromrom.
23 Zamoyozo zinatambalitsa mapiko ake mʼmunsi mwa thambo lija, mapiko ake ena kumakhudzana, mapiko awiri kumaphimba thupi lake.
Ma moul inge tu ye ma raun sac, ac kais sie selos asroela luo sin posohksok lal ah nu ke ma moul ma tu siskal kewa. Posohksok luo ngia el sang afinya manol.
24 Pamene zamoyo zimayenda ndimamva phokoso la mapiko ake, ngati mkokomo wa madzi ambiri, ngati liwu la Wamphamvuzonse, ngati phokoso la gulu lankhondo. Zimati zikayima zinkagwetsa mapiko ake.
Ke pacl elos sohksok, nga lohng pusren posohksok lalos uh oana ngirngir lun noa tok uh, ku oana pusren un mwet mweun lulap, ku oana pusren God Kulana. Ac ke pacl elos ac tui tila sohk, elos ac orani posohksok lalos,
25 Ndipo panamveka mawu kuchokera pamwamba pa thambo la pa mitu ya zamoyo zija. Nthawi iyi nʼkuti zamoyozo zitayima ndi kugwetsa pansi mapiko ake.
tusruktu srakna oasr pusra se tuku lucng liki ma raun se fin sifalos.
26 Pamwamba pa thambo la pa mitu yake panali chinthu chimene chimaoneka ngati mpando waufumu wopangidwa ndi mwala wa safiro, ndipo pamwamba pa mpando waufumuwo panali chinthu chooneka ngati munthu.
Lucng liki ma raun sac oasr ma se oan we oana luman tron se orekla ke eot sapphire, ac oasr sie ma su muta fin tron sac su oana luman mwet se.
27 Ndinaona kuti mmwamba mwa chiwuno chake munali ngati chitsulo chowala konsekonse ngati moto. Mʼmunsi mwa chiwuno chake munalinso ngati moto wokhawokha. Kuwala kwa mphamvu kunamuzungulira munthuyo.
Infulwalyak nu lucng oana bronze saromrom infulwen sie e, ac infulwali nu ten oana luman firirrir lun e uh. Acn nukewa rauneak arulana kalem,
28 Kuwalako kunali ndi maonekedwe a utawaleza mʼmitambo tsiku limene kwagwa mvula. Umu ndi mmene ulemerero wa Yehova umaonekera. Pamene ndinawuona ndinagwa pansi ndipo ndinamva mawu akundiyankhula.
ac tuhn nukewa ke lelakem uh oasr kac. Kalem se inge, su arulana saromrom, akkalemye lah LEUM GOD El oasr we. Ke nga liye ma se inge, nga putati ac oankiyuki infohk uh. Na nga lohng pusra se kaskas.

< Ezekieli 1 >