< Ezekieli 8 >
1 Tsiku lachisanu la mwezi wachisanu ndi chimodzi, mʼchaka chachisanu ndi chimodzi, ndinakhala mʼnyumba mwanga pamodzi ndi akuluakulu a ku Yuda. Tsono mphamvu za Ambuye Yehova zinandifikira.
Ngomnyaka wesithupha, ngenyanga yesithupha ngosuku lwesihlanu, lapho ngangihlezi endlini yami labadala bakoJuda behlezi phambi kwami, isandla sikaThixo Wobukhosi sehlela phezu kwami khonapho.
2 Nditayangʼana ndinangoona chinthu chooneka ngati munthu. Kuchokera pamene pamaoneka ngati chiwuno chake kumatsika mʼmunsi anali ngati moto, ndipo kuchokera mʼchiwuno kukwera mmwamba amaoneka mowala ngati mkuwa wonyezimira.
Ngakhangela, ngabona ulutho olwalulesimo somuntu. Kusukela kokwakungathi lukhalo lwakhe kusiya phansi wayenjengomlilo, njalo kusukela lapho kusiya phezulu ukubonakala kwakhe kwakhazimula njengensimbi evuthayo.
3 Iye anatambasula chinthu chooneka ngati dzanja ndipo anagwira tsitsi la pamutu panga. Nthawi yomweyo Mzimu unandikweza mlengalenga. Tsono ndikumachita ngati ndikuona Mulungu kutulo, Mzimu uja unapita nane ku Yerusalemu nundiyika pa khomo la chipata chamʼkati choyangʼana kumpoto. Kumeneko kunali fano limene limaputa mkwiyo wa Mulungu.
Welula okwakukhanya angathi yisandla wangibamba ngenwele zekhanda lami. UMoya wangiphakamisela phezulu phakathi komhlaba lezulu, kwathi ngemibono kaNkulunkulu wangisa eJerusalema, ekungeneni kwesango langasenyakatho yeguma langaphakathi, lapho okwakumi khona isithombe esibangela ubukhwele.
4 Kumeneko ndinaona ulemerero wa Mulungu wa Israeli ngati momwe ndinaonera mʼmasomphenya mʼchigwa muja.
Njalo khonapho phambili kwami kwakulenkazimulo kaNkulunkulu ka-Israyeli, njengasembonweni engawubona egcekeni.
5 Tsono Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, tayangʼana kumpoto.” Choncho ndinayangʼana kumpoto ndipo ndinaona pa khomo la chipata pafupi ndi guwa lansembe ndinaona fano loputa mkwiyo wa Mulungu lija.
Wasesithi kimi, “Ndodana yomuntu, khangela ngasenyakatho.” Ngakho ngakhangela, kwathi entubeni esenyakatho kwesango le-alithari ngabona lesisithombe sobukhwele.
6 Ndipo Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi ukuona zimene akuchitazi, zonyansa zazikulu zimene Aisraeli akuchita kuno, zinthu zondichotsa Ine kumalo anga opatulika? Koma iwe udzaona zinthu zimene zili zonyansa kwambiri.”
Wasesithi kimi, “Ndodana yomuntu, uyakubona yini abakwenzayo, izinto ezenyanyekayo kakhulu indlu ka-Israyeli ezenzayo lapha, izinto ezizangixotshela khatshana lendawo yami engcwele? Kodwa wena uzabona izinto ezenyanyekayo kakhulukazi kulalezi.”
7 Kenaka Iye anandipititsa ku khomo lolowera ku bwalo la Nyumba ya Mulungu. Nditayangʼanitsitsa ndinangoona dzenje pa khomapo.
Emva kwalokho wangisa entubeni yeguma. Ngakhangela, ngabona imbobo emdulini.
8 Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, tsopano bowola pa khomapo.” Ndinabowoladi pa khomapo ndipo ndinapezapo khomo.
Wasesithi kimi, “Ndodana yomuntu, khathesi gubha umduli.” Ngakho ngawugubha umduli ngasengibona umnyango khona.
9 Ndipo Yehova anandiwuza kuti, “Lowa, ndipo ona zinthu zonyansa zimene akuchita pamenepa.”
Wasesithi kimi, “Ngena ubone izinto ezimbi lezenyanyekayo abazenzayo lapha.”
10 Motero Ine ndinalowa ndi kuyangʼana, ndipo ndinaona pa makoma onse zithunzi za zinthu zosiyanasiyana zokwawa pansi, za nyama zonyansa ndiponso za mafano onse amene Aisraeli ankapembedza.
Ngakho ngangena phakathi ngakhangela, ngabona indawo yonke emidulini kufanekiswe inhlobo zezinto zonke ezihuquzelayo lezinyamazana ezenyanyekayo kanye lezithombe zonke zasendlini ka-Israyeli.
11 Patsogolo pa zimenezi panayima akuluakulu makumi asanu ndi awiri a Aisraeli, ndipo Yaazaniya mwana wa Safani anali atayima pakati pawo. Aliyense wa iwo anali ndi chofukizira lubani mʼdzanja lake ndipo utsi wa fungo lokoma la lubani unkafuka.
Phambi kwazo kwakumi abadala bendlu ka-Israyeli abangamatshumi ayisikhombisa, loJazaniya indodana kaShafani emi phakathi kwabo. Omunye lomunye wayephethe udengezi lokutshisela impepha ngesandla, luthunqa intuthu elephunga elimnandi elempepha.
12 Tsono Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi waona zimene akuluakulu a Aisraeli akuchita mu mdima, aliyense akupembedza fano lakelake mʼnyumbamo? Iwo akuti, ‘Yehova sakutiona; Yehova walisiya dziko!’
Wathi kimi, “Ndodana yomuntu, ukubonile yini okwenziwa ngabadala bendlu ka-Israyeli emnyameni, omunye lomunye esendaweni yokukhonzela isithombe sakhe? Bathi, ‘UThixo kasiboni; uThixo uselilahlile ilizwe.’”
13 Iye anandiwuzanso kuti, ‘Iwe udzawaonanso akuchita zinthu zonyansa kwambiri.’”
Wabuye wathi, “Uzababona besenza izinto ezenyanyeka okudlula lokho.”
14 Kenaka anapita nane pa khomo la ku khomo la chipata cha Nyumba ya Mulungu choyangʼana kumpoto, ndipo kumeneko ndinaona akazi ena atakhala pansi, akulira mulungu wawo wotchedwa Tamuzi.
Emva kwalokho wangisa ekungeneni kwesango lasenyakatho kwendlu kaThixo, ngabona abesifazane behlezi khona belilela uThamuzi.
15 Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi ukuziona zimenezi? Iwe udzaona zinthu zimene zili zonyansa kwambiri kuposa izi.”
Wasesithi kimi, “Uyakubona lokhu na, ndodana yomuntu? Uzabona izinto ezenyanyeka kakhulu kulalokhu.”
16 Kenaka Iye anapita nane mʼkati mwa bwalo la Nyumba ya Yehova. Kumeneko ku khomo lolowera ku Nyumba ya Yehova pakati pa khonde ndi guwa lansembe, panali amuna 25. Anafulatira Nyumba ya Mulungu wa Yehova ndipo nkhope zawo zinaloza kummawa, ndipo ankapembedza dzuwa choyangʼana kummawa.
Wasengisa egumeni lendlu kaThixo elingaphakathi, njalo khonapho ekungeneni kwethempeli, phakathi komkhandlu le-alithari, kwakulamadoda ayengaba ngamatshumi amabili lanhlanu. Ayekhothamele phansi elangeni empumalanga, efulathele ithempeli likaThixo. Ubuso bawo bukhangele empumalanga.
17 Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi waziona zimenezi? Kodi nʼchinthu chopepuka kuti anthu a ku Yuda azichita zonyansa zimene akuchitazi pano? Kodi afike mpaka pomafalitsa za ndewu mʼdziko lonse? Iwotu akuwutsa ukali wanga. Akundipsetsa mtima ndi zochita zawo!
Wathi kimi, “Sewake wakubona lokhu na ndodana yomuntu? Kuyinto encane na ukuthi indlu kaJuda yenze izinto ezenyanyekayo abazenza lapha? Kumele ilizwe baligcwalise futhi ngodlakela, njalo bangithukuthelise kokuphela na? Bakhangele bebeka ugatsha empumulweni yabo!
18 Choncho Ine ndidzawalanga ndili wokwiya. Sindidzawamvera chisoni kapena kuwaleka. Ngakhale atandifuwulira mʼmakutu mwanga sindidzawamvera.”
Ngakho ngizabaphatha ngentukuthelo; angiyikuba lesihawu kubo ngibayekele. Lanxa sebeklabalalela ezindlebeni zami, kangiyikubalalela.”