< Ezekieli 6 >
1 Yehova anandipatsa uthenga uwu kuti,
Dimteng kaniak ti sao ni Yahweh a kunana,
2 “Iwe mwana wa munthu, yangʼana ku mapiri a Israeli; yankhula nawo modzudzula
“Anak ti tao, isangom ti rupam kadagiti bantay ti Israel ket agipadtoka kadagitoy.
3 kuti, ‘Inu mapiri a ku Israeli, imvani mawu a Ambuye Yehova. Iye akuwuza mapiri, magomo, mitsinje ndi zigwa kuti: Ine ndizakuthirani nkhondo ndipo ndidzawononga nyumba zanu mʼmene mukupembedzeramo mafano.
Kunaem, 'Banbantay ti Israel, denggenyo ti sao ni Yahweh nga Apo! Kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo kadagiti bantay ken kadagiti turod, kadagiti igid ti waig, ken kadagiti tanap: Denggenyo! Iyegko ti kampilan maibusor kadakayo, ket dadaelekto dagiti nangangato a lugaryo.
4 Maguwa anu ansembe adzagumulidwa ndipo maguwa anu ofukizira lubani adzaphwanyidwa; ndipo ndidzapha anthu anu pamaso pa mafano anu.
Ket mabaybay-anto dagiti altaryo ken madadaelto dagiti adigiyo, ket ibellengkonto dagiti natay a tattaoyo iti sangoanan dagiti didiosenda.
5 Ine ndidzagoneka mitembo ya Aisraeli pamaso pa mafano awo, ndipo ndidzamwaza mafupa anu mozungulira maguwa anu ansembe.
Iwalangkonto dagiti bangkay dagiti tattao ti Israel iti sangoanan dagiti didiosenda, ken maiwarawaranto dagiti tulangyo iti aglawlaw dagiti altaryo.
6 Konse kumene mumakhala, mizinda yanu idzasanduka bwinja. Nyumba zanu zopembedzera mafano zidzagumulidwa kotero kuti maguwa anu adzawonongedwa ndi kusakazidwa, mafano anu adzaphwanyidwa ndi kuwonongedwa. Maguwa anu ofukizirapo lubani adzagwetsedwa pansi ndipo zonse zimene munapanga zidzatheratu.
Sadinoman a pagnaedanyo, dagiti siudad ket madadaelto ken dagiti nangangato a lugar ket mabaybay-anto, isu a dagiti altaryo ket madadael ken mabaybay-anto. Ket madadael ken mapukawto dagitoy, maputedto dagiti adigiyo ken mapunasto dagiti nagbannoganyo.
7 Anthu anu adzaphedwa pakati panu, ndipo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’
Adunto dagiti natay iti nagtetengngaanyo, ket maammoanyonto a Siak ni Yahweh!
8 “Komabe ndidzasiya ena pangʼono opulumuka ku nkhondo. Iwowa ndidzawamwazira ku mayiko ena pakati pa anthu a mitundu ina.
Ngem mangibatiakto iti dadduma kadakayo, ken addanto sumagmamano a makalisi iti kampilan kadagiti nasion, inton naiwarawarakayo iti entero a pagilian.
9 Pamenepo opulumuka mwa inu adzandikumbukira ku mayiko kumene anatengedwa ukapolo. Ndidzawamvetsa chisoni chifukwa cha kusakhulupirika kwawo ndi kundipandukira kuja ndiponso chifukwa kuti anayika mtima wawo pa mafano. Choncho adzachita okha manyazi chifukwa cha zoyipa zimene ankachita ndi miyambo yonyansa imene ankatsata.
Ket dagidiay makalibas, malagipdakto kadagiti nasion a nakaipananda kas balud, a nagladingitak gapu iti saan a napudno a pusoda a nangtallikud kaniak ken gapu ta dagiti didiosenda ti pinilida a nagdaydayawan. Ket makitanto kadagiti rupada ti pannakadurmenda kadagiti bagbagida gapu iti kinadakesda ken gapu kadagiti amin a makarimon a naaramidda.
10 Ndipo iwo adzadziwa kuti ndine Yehova ndi kuti sindinkawaopseza chabe pamene ndinanena kuti ndidzawawononga.
Iti kasta, maammoandanto a Siak ni Yahweh. Daytoy ti makagapu a kinunak nga iyegko kadakuada daytoy a pagdaksanda.
11 “Ambuye Yehova akuti: Womba mʼmanja mwako ndipo uponde mapazi ako pansi mwamphamvu ndipo ufuwule kuti, ‘Mayo!’ chifukwa cha zonyansa ndi zoyipa zonse zimene Aisraeli achita, pakuti adzaphedwa ndi lupanga, njala ndi mliri.
Kastoy ti kuna ni Yahweh nga Apo: Itipatyo dagiti imayo ken agtabbugakayo! Kunaenyo, “Asikami pay!” gapu kadagiti makarimon nga aramid iti balay ti Israel! Ta mataydanto babaen iti kampilan, nakaru a panagbisin ken didigra.
12 Amene ali kutali adzafa ndi mliri, ndipo amene ali pafupi adzafa pa nkhondo, ndipo amene adzapulumuke ndi kusaphedwa adzafa ndi njala. Kotero ndidzakwaniritsa ukali wanga pa iwo.
Ti adda iti adayo ket matayto babaen iti didigra, ken ti adda iti asideg ket matayto babaen iti kampilan. Dagidiay mabati ken makalasat ket mataydanto iti nakaro a panagbisin; iti kastoy a wagas a maipalak-amko ti kasta unay a pungtotko kadakuada.
13 Ndipo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, pamene anthu awo adzagona atafa pakati pa mafano awo mozungulira maguwa awo ansembe, pamwamba pa magomo ndi mapiri onse, pansi pa mtengo uliwonse watambalala ndi wa thundu uliwonse wamasamba ambiri, kumalo kumene ankapereka nsembe zonunkhira kwa mafano awo onse.
Ket maammoanyonto a Siak ni Yahweh, inton maiwalang dagiti natay kadakuada iti ayan dagiti didiosenda, iti aglawlaw dagiti altarda, iti tunggal nangangato a turod—kadagiti amin a tuktok ti bantay, ken iti tunggal sirok ti nalangto a kayo ken iti dakkel a puon ti kayo a lugo—dagiti lugar a pagpupuoranda kadagiti insenso nga agpaay kadagiti amin a didiosenda.
14 Choncho ndidzawalanga ndi mkono wanga ndi kusandutsa dziko kukhala bwinja. Dziko lonse kumene akukhala kuyambira ku chipululu mpaka ku mzinda wa Ribula ndidzalisandutsa bwinja. Pamenepo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
Ipakitakto ti pannakabalinko ket pagbalinekto a langalang ti daga ket awan serserbina, manipud iti let-ang agingga idiay Dibla, iti amin a lugar a pagnanaedanda. Ket maammoandanto a Siak ni Yahweh.”