< Ezekieli 44 >
1 Munthu uja anabwerera nane ku chipata chakunja kwa malo opatulika, chomwe chimayangʼana kummawa. Chipatacho chinali chotseka.
Тогава Той ме върна по пътя на външната порта на светилището, която гледа към изток; и тя бе затворена.
2 Yehova anandiwuza kuti, “Chipata ichi chikhale chotseka, chisatsekulidwe. Wina asalowerepo chifukwa Yehova, Mulungu wa Israeli walowera pomwepa.
И Господ ми рече: Тая порта ще бъде затворена, няма да се отвори, и никой човек да не влезе през нея; защото Господ Израилевият Бог е влязъл през нея; затова, тя ще бъде затворена.
3 Kalonga yekha angathe kukhala mʼmenemo ndi kumadya chakudya pamaso pa Yehova. Iye adzalowere pa njira ya ku khonde lamʼkati ndi kutulukiranso njira yomweyo.”
А князът, който като княз ще седне в нея, за да яде хляб пред Господа, той ще влезе през пътя на предверието на тая порта, и през същия път ще излезе.
4 Kenaka munthuyo anandidzeretsa pa chipata chakumpoto ndipo tinafika kumaso kwa Nyumba ya Mulungu. Nditapenyetsetsa ndinangoona ulemerero wa Yehova utadzaza mʼNyumba ya Mulungu, ndipo ndinadzigwetsa pansi chafufumimba.
Тогава ме заведе по пътя на северната порта срещу дома; и като погледнах, ето, Господният дом бе пълен с Господната слава; и паднах на лицето си.
5 Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, samala bwino ndipo uyangʼanitsitse ndi kumvetsa bwino zonse zimene ndikuwuze zokhudza malamulo ndi malangizo a Nyumbayi. Usamalitse za amene angalowe ndi kutuluka mʼNyumbayi.
И Господ ми рече: Сине човешки, внимавай в сърцето си, погледни с очите си, и чуй с ушите си всичко, което ти казвам за всичките наредби на Господния дом, и за всичките му закони; и забележи добре входа на дома, с всичките изходи и светилището.
6 Uwuze mtundu wopanduka wa Israeli kuti Ine Ambuye Yehova ndikuti: Inu Aisraeli, andikwana machitidwe anu onyansawo!
И кажи на бунтовниците, сиреч, на Израилевия дом: Така казва Господ Иеова: Доме Израилев, нека ви са доволно всичките мерзости, които извършихте,
7 Munalowetsa alendo osachita mdulidwe mu mtima ndi mʼthupi momwe mʼNyumba yanga ndipotu anayipitsa Nyumba yanga. Pamene inu munkandipatsa chakudya changa ndi magazi omwe kuwonjezera pa zonyansa zanu zonse ndiye kuti munaphwanya pangano langa.
дето въведохте инородци, с необрязано сърце и необрязана плът, да бъдат в светилището Ми та да го мърсят, дори в Моя дом, и дето, когато принасяте хляба Ми, тлъстината и кръвта, престъпихте завета Ми, в прибавка на всичките ви други мерзости.
8 Mʼmalo moti muzisamalira zinthu zanga zopatulika, mwayika alendo kuti aziyangʼanira malo anga opatulika.
И не сте изпълнили службата на светите Ми неща, но сте поставили за себе си стражари над службата в светилището ми.
9 Ambuye Wamphamvuzonse akuti: Palibe mlendo wosachita mdulidwe mu mtima ndi mʼthupi ngakhalenso mlendo amene amakhala pakati pa Aisraeli amene adzalowe mʼmalo anga opatulika.
Така казва Господ Иеова: От всичките инородци, които са между израилтяните, никой инородец с необрязано сърце, и необрязана плът да не влиза в светилището Ми.
10 “Ndiponso Alevi amene anandisiya kutali pa nthawi imene Israeli anasochera potsata mafano, adzalangidwa chifukwa cha tchimo lawo.
Но и левитите, които се отдалечиха от мене, когато заблуждаваше Израил, който заблуди от Мене и отиде след идолите си, те ще носят беззаконието си.
11 Adzangokhala atumiki chabe mʼmalo anga opatulika. Azidzayangʼanira zipata za Nyumba ya Mulungu ndi kugwira ntchito kumeneko. Azidzapha nyama za nsembe zopsereza ndi za nsembe zina za anthu. Choncho azidzayimirira pamaso pa anthu nʼkumawatumikira.
Но пак, те ще бъдат служители в светилището Ми, да надзирават върху портите на дома и да служат в дома; те ще колят всеизгарянията и жертвите на людете, и те ще стоят пред тях, за да им слугуват.
12 Iwowa ankatumikira anthu popembedza mafano awo, ndipo anachititsa Aisraeli kugwa mu uchimo. Nʼchifukwa chake Ine ndikulumbira kuti iwowa ayenera kulangidwa chifukwa cha machimo awo. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.
Понеже им слугуваха пред идолите им, и станаха спънка за увличане Израилевия дом в беззаконие, затова Аз дигнах ръката Си против тях, казва Господ Иеова; и те ще носят беззаконието си.
13 Iwo sayenera kufika pafupi ndi Ine ndi kunditumikira ngati ansembe, kapena kuyandikira chilichonse cha zinthu zanga zopatulika, kapenanso zopereka zanga zopatulika kwambiri. Iwo adzachititsidwa manyazi chifukwa cha machitidwe awo onyansa.
И няма да се приближават при мене, за да ми свещенодействуват, нито да се приближават при нищо от светите ми неща, нито при пресветите; но ще носят срама си и мерзостите, които извършиха.
14 Komabe ndidzawayika kuti aziyangʼanira Nyumba yanga ndi kutumikira pa ntchito zake zonse zoyenera kuti zigwiridwe mʼmenemo.
Обаче, ще ги поставя стражари над службата на дома за всичката му прислуга, и за всичко, което ще се върши в него.
15 “Koma ansembe, a fuko la Levi, a banja la Zadoki amene ankatumikira mokhulupirika ku malo anga opatulika pa nthawi imene Aisraeli anasochera ndi kundisiya Ine; iwowa adzasendera kwa Ine kudzanditumikira. Adzafika pamaso panga kuti apereke nsembe za mafuta ndi magazi. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.
А левитските свещеници, Садоковите потомци, които извършваха службата на светилището Ми, когато израилтяните заблуждаваха от Мене, те нека се приближават при Мене, за да Ми служат, и нека стоят пред Мене да Ми принасят тлъстината и кръвта, казва Господ Иеова.
16 Okhawa ndiwo adzalowe ku malo anga opatulika ndi kudzayandikira tebulo langa kuti adzanditumikire. Amenewa okha ndiwo adzasamalire zinthu zanga.
Те нека влизат в светилището Ми, и те нека се приближават при трапезата, за да Ми служат, и те нека извършват службата Ми.
17 “Pamene alowa ku zipata za bwalo lamʼkati azivala zovala zabafuta. Asamavale chovala china chilichonse cha ubweya wankhosa pamene akutumikira pa zipata za bwalo la mʼkati kapena kunja kwa Nyumba ya Mulungu.
И когато влизат в портите на вътрешния двор нека обличат ленени дрехи; да няма нищо вълнено на тях, докато служат в портите на вътрешния двор и в дома.
18 Azivala nduwira za bafuta ndi kabudula wabafuta mʼkati. Asavale chilichonse chowachititsa thukuta.
Нека имат ленени гъжви на главите си, нека имат и ленени гащи на кръста си; да не опасват нищо, което причинява пот.
19 Pamene atuluka ndi kupita ku bwalo lakunja kumene kuli anthu, azivula zovala zimene amatumikira nazo, ndipo azisiye zovalazo mu zipinda zopatulika. Pambuyo pake avale zovala zina, kuopa kuti angapatsireko kuyera anthu enawo ndi zovala zawozo.
А когато излизат във външния двор, във външния двор към людете, нека събличат дрехите, с които са служили, и като ги слагат в светите стаи нека обличат други дрехи, за да не освещават людете с одеждите си.
20 “‘Ansembe asamamete mpala kapena kusunga tsitsi lalitali kwambiri, koma azingoliyepula.
И да не бръснат главите си, нито да оставят космите си да растат, но само да стрижат главите си.
21 Wansembe asamwe vinyo pamene ali pafupi kulowa mʼbwalo la mʼkati.
И никой свещеник да не пие вино, когато влиза във вътрешния двор.
22 Iwo asakwatire akazi amasiye kapena osudzulidwa; koma azikwatira anamwali osadziwa mwamuna a fuko la Israeli kapena akazi amasiye a ansembe anzawo.
И да не си вземе за жена вдовица или напусната; но да вземат девица от рода на Израилевия дом, или вдовица овдовяла от свещеник.
23 Ansembe aziphunzitsa anthu anga kusiyanitsa pakati pa zinthu zopatulika ndi zinthu wamba, ndiponso pakati pa zinthu zoyenera ndi zosayenera kuperekedwa nsembe.
И нека учат людете Ми да различават между свето и несвето, и нека ги упътват да разпознават нечисто от чисто.
24 “‘Pakakhala milandu, ansembe azikhala oweruza ndipo agamule milanduyo potsata malamulo anga. Atsate malamulo anga ndi malangizo anga pa za masiku anga onse a chikondwerero. Asamalirenso kuti masiku anga a Sabata akhale oyera.
И в препирните те нека стоят да съдят; според Моите съдби нека ги съдят; и нека пазят законите Ми и повеленията Ми във всичките Ми определени празници; и нека освещават съботите Ми.
25 “‘Wansembe asadziyipitse pokhudza munthu wakufa, pokhapokha ngati wakufayo ndi abambo ake kapena amayi ake, mwana wake wamwamuna kapena wamkazi, mʼbale wake kapena mlongo wake wosakwatiwa.
Да не се допират при мъртъв човек та да се осквернят; обаче за баща или за майка, за син или за дъщеря, за брат или за неженена сестра, за тях бива да се оскверняват.
26 Atatha kuyeretsedwa adikirebe masiku asanu ndi awiri kuti ayere ndithu.
А след като се очисти оскверненият и му минат седем дни,
27 Pa tsiku lomwe akukalowa mʼbwalo la mʼkati la malo opatulika kuti akatumikire, apereke nsembe yopepesera machimo. Ndikutero Ine Ambuye Yehova.
тогава в деня, когато влиза в светилището, във вътрешния двор, за да служи в светилището, нека принася приноса си за грях, казва Господ Иеова.
28 “‘Ansembe asadzakhale ndi cholowa chilichonse ayi. Cholowa chawo ndi Ine. Musadzawapatse chuma mu Israeli; Ine ndidzakhala chuma chawo.
А колкото за наследството им, Аз съм наследството им; да не им давате притежание в Израиля, защото Аз съм притежанието им.
29 Iwo azidzadya nsembe ya chakudya, nsembe yopereka chifukwa cha tchimo ndi nsembe yopepesera machimo. Zinthu zonse zoperekedwa kwa Yehova mu Israeli zidzakhala zawo.
Нека ядат хлебния принос, приноса за грях и приноса за престъпление; и всяко обречено нещо в Израиля да бъде тяхно.
30 Zabwino za zipatso zanu zoyambirira kucha ndiponso mphatso zanu zonse zapadera zidzakhala za ansembe. Inu muziwapatsa chigawo choyamba cha ufa wanu kuti pa nyumba panu pakhale madalitso.
И първенците от всичките първи рожби от всичко, и всеки принос от всичко, от всичките видове на вашите приноси, да бъдат на свещениците; тоже да давате на свещеника първака от тестото си, за да почива благословение на домовете ви.
31 Ansembe sayenera kudya kalikonse kofa kokha, kaya mbalame, kapena nyama. Kapena yochita kujiwa.’”
Свещениците да не ядат никаква мърша или разкъсано от звяр, било птица или животно.