< Ezekieli 40 >

1 Kumayambiriro a chaka cha 25, cha ukapolo wathu, tsiku la khumi lamwezi, patapita zaka khumi ndi zinayi mzinda wa Yerusalemu utawonongedwa, pa tsiku lomwelo dzanja la Yehova linali pa ine ndipo Iye anapita nane ku Yerusalemu.
Ын анул ал доуэзечь ши чинчиля ал робией ноастре, ла ынчепутул анулуй, ын зиуа а зечя а луний, ла пайспрезече ань дупэ дэрымаря четэций, токмай ын зиуа ачея, а венит мына Домнулуй песте мине ши м-а стрэмутат ын цара луй Исраел.
2 Mʼmasomphenyawo Yehova ananditenga ndi kupita nane ku dziko la Israeli ndipo anandiyika pa phiri lalitali kwambiri, moti ndinaona ngati mzinda.
М-а дус аколо ын ниште ведений думнезеешть ши м-а ашезат пе ун мунте фоарте ыналт; спре мязэзи де ачест мунте ера чева ка о четате зидитэ.
3 Atandifikitsa kumeneko ndinaona munthu wonyezimira ngati mkuwa. Iye anali atayima pa chipata ndipo mʼdzanja lake munali chingwe cha nsalu yabafuta ndi ndodo yoyezera.
М-ам дус аколо ши ятэ кэ аколо ера ун ом а кэруй ынфэцишаре ера ка ынфэцишаря арамей; ел авя ын мынэ о сфоарэ де мэсурат де ин ши о прэжинэ де мэсурат ши стэтя ла поартэ.
4 Munthuyo anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, penyetsetsa ndipo umvetse bwinobwino. Uyikepo mtima wako pa zonse zimene ndikukuonetsa pakuti anakubweretsa kuno kuti uwone zimenezi. Tsono ukawawuze Aisraeli zonse zimene uzione.”
Омул ачела мь-а зис: „Фиул омулуй, привеште ку окий тэй, аскултэ ку урекиле тале ши я аминте ла тоате лукруриле пе каре ци ле вой арэта, кэч ай фост адус аич ка сэ ци ле арэт. Фэ куноскут касей луй Исраел тот че вей ведя.”
5 Ine ndinaona khoma litazungulira mbali zonse za Nyumba ya Mulungu. Mʼdzanja la munthuyo munali bango lopimira limene kutalika kwake kunali kwa mamita atatu. Atayeza chipupacho anapeza kuti kuchindikira kwake kunali mamita atatu, ndiponso kutalika kwake kunalinso mamita atatu.
Ун зид ынконжура Темплул пе динафарэ де жур ымпрежур. Ын мына омулуй ачелуя ера о прэжинэ де мэсурат лунгэ де шасе коць, фиекаре кот авынд о палмэ май мулт декыт котул обишнуит. А мэсурат лэцимя зидулуй, каре ера де о прэжинэ, ши ынэлцимя, каре ера тот де о прэжинэ.
6 Anapita ku chipata chakummawa. Anakwera pa makwerero a nyumbayo, nayeza chiwundo choyamba cha chipatacho; kutalika kwake kunali mamita atatu.
А мерс ла поарта де рэсэрит ши й-а суит трептеле. А мэсурат прагул порций, каре ера лат де о прэжинэ, ши челэлалт праг, каре ера лат де о прэжинэ.
7 Kudutsa chiwundo choyambachi, panali zipinda za alonda zisanu ndi chimodzi, zitatu kudzanja lamanja, zitatu kudzanja lamanzere. Chilichonse chinali cha mamita atatu mulitali mwake, chimodzimodzinso mulifupi mwake. Mipata ya pakati pa zipindazo inali ya mamita awiri ndi theka. Ndipo chiwundo cha pa chipata pafupi ndi khonde lapachipata, chinali mamita atatu.
Фиекаре одае де пазэ ера лунгэ де о прэжинэ ши ларгэ тот де о прэжинэ. Ынтре фиекаре доуэ одэй де пазэ ера ун лок гол де чинч коць. Прагул порций де лынгэ тинда порций динэунтру ера де о прэжинэ.
8 Ndipo iye anayeza khonde la chipata ndipo chinali cha mamita atatu.
А мэсурат ши тинда порций динэунтру; ера де о прэжинэ.
9 Anayeza khonde ndipo linali mamita anayi. Mphuthu zake zinali mita imodzi kuchindikira kwake. Khonde lamʼkati lapachipata linali kumapeto kwenikweni pafupi ndi Nyumba ya Mulungu.
А мэсурат апой тинда порций; ера де опт коць ши стылпий ей ерау де дой коць. Тинда порций ера спре партя динэунтру.
10 Mʼkati mwa chipata chakummawa munali zipinda za alonda zitatu mbali iliyonse. Zitatu zonsezo zinali zofanana, ndipo khonde la pakati pa zipindazo linali lofanana.
Одэиле де пазэ але порций де рэсэрит ерау ын нумэр де трей де о парте ши трей де чялалтэ; тоате трей авяу ачеяшь мэсурэ ши стылпий де фиекаре парте авяу тот ачеяшь мэсурэ.
11 Kenaka anayeza chipata cholowera; mulifupi mwake munali mamita asanu ndipo mulitali mwake munali mamita asanu ndi limodzi ndi theka.
А мэсурат апой лэрӂимя дескизэтурий порций, каре ера де зече коць, ши лунӂимя порций, каре ера де трейспрезече коць.
12 Kutsogolo kwa chipinda chilichonse cha alonda kunali khoma lalifupi lotalika theka la mita, ndipo mbali iliyonse ya zipinda za alondazo inali yotalika mamita atatu.
Ынаинтя одэилор де пазэ ера ун лок гол де ун кот де о парте ши де чялалтэ; фиекаре одае де пазэ авя шасе коць де о парте ши шасе коць де чялалтэ.
13 Ndipo anayeza kutalika kwa mulifupi mwa chipata cholowera, kuchokera ku khoma lakumbuyo la chipinda chimodzi mpaka ku khoma la chipinda china; kuchokera ku chitseko mpaka ku chitseko china. Kutalika kwake kunali mamita khumi ndi awiri ndi theka.
А мэсурат поарта де ла акоперишул уней одэй де пазэ, пынэ ла акоперишул челейлалте; ынтре челе доуэ дескизэтурь каре ерау фацэ ын фацэ ера о лэциме де доуэзечь ши чинч де коць.
14 Anayezanso khonde lamʼkati ndipo linali la mamita makumi atatu. Ndipo mozungulira khondelo munali bwalo. Muyesowu sukuphatikiza khonde loyangʼanana ndi bwalo.
А мэсурат тинда порций ши а гэсит доуэзечь де коць; тинда дэдя ынтр-о курте, де жур ымпрежурул порций.
15 Kuchokera pa chipata cholowera mpaka ku mapeto a khonde la chipata, kutalika kwake kunali mamita 27.
Локул динтре поарта де ла интраре ши тинда порций динэунтру ера лунг де чинчзечь де коць.
16 Makoma a zipinda ndiponso makoma a pakati pa zipindazo anali ndi mazenera. Khonde lamʼkati linalinso ndi mazenera mʼkati mwake. Pa makoma onsewo anajambulapo zithunzi za kanjedza.
Ла одэиле де пазэ ши ла стылпий лор динэунтрул порций де жур ымпрежур ерау ниште ферестре ынгрэдите; ферестре ерау ши ынэунтру ын тинзиле порций де жур ымпрежур, яр пе стылпь ерау сэпате рамурь де финичь.
17 Kenaka munthuyo anandilowetsa mʼbwalo lakunja, ndipo ndinaona zipinda zina ndi msewu wa miyala wozungulira bwalo lonse. Zipinda zonse zinali makumi atatu ndipo zinkayangʼana msewuwo.
М-а дус ын куртя де афарэ, унде се афлау одэй ши ун калдарым де жур ымпрежур; пе калдарымул ачеста ерау трейзечь де одэй.
18 Utali wa mulifupi mwa msewuwo unkayenda mamita 27 kufanana ndi utali wa chipata cholowera. Uwu unali msewu wa mʼmunsi.
Калдарымул ера лынгэ порць ши ера де-а лунгул порцилор: ачеста ера калдарымул де жос.
19 Tsono, anayeza kutalika kwa bwalo kuyambira chipata cholowera choyamba mpaka polowera pa chipata chakunja cha bwalo la mʼkati. Kutalika kwake kunali mamita makumi asanu.
А мэсурат лэцимя де ла поарта де жос пынэ ла партя де афарэ а курций динэунтру ши авя о сутэ де коць ла рэсэрит ши ла мязэноапте.
20 Kenaka munthuyo anayeza mulitali ndi mulifupi mwa chipata chimene chimayangʼana kumpoto, chotulukira kunja.
А мэсурат лунӂимя ши лэцимя порций де мязэноапте а курций де афарэ.
21 Zipinda za alonda zimene zinalipo zitatu mbali iliyonse, makoma ake ndi khonde zinali ndi muyeso wofanana ndi wachipata choyamba chija. Kutalika kwake kunali mamita 27 ndipo mulifupi mwake munali mamita 13.
Одэиле ей де пазэ, ын нумэр де трей де о парте ши трей де алта, стылпий ши тинда ей авяу ачеяшь мэсурэ ка поарта динтый: чинчзечь де коць ын лунӂиме ши доуэзечь ши чинч де коць ын лэциме.
22 Mipata yake, khonde lake ndi zojambula za kanjedza zinali ndi miyeso yofanana ndi za chipata chakummawa. Chipatacho chinali ndi makwerero asanu ndi awiri ndipo kotsirizira kwa chipatacho kunali khonde.
Ферестреле ей, тинда ей, финичий ей авяу ачеяшь мэсурэ ка поарта де рэсэрит; те суяй ла еа пе шапте трепте, яр тинда ей ера ын партя динэунтру.
23 Panalinso chipata cholowera ku bwalo lamʼkati chofanana ndi chakummawa chimene chimayangʼanana ndi chipata chakumpoto, chofanana ndi cha mbali ya kummawa. Anachiyeza kuchokera ku chipata china mpaka ku chipata china. Kutalika kwake kunali mamita makumi asanu.
Ла куртя динэунтру ера о поартэ, ын фаца порций де мязэноапте ши ын фаца порций де рэсэрит; а мэсурат о сутэ де коць де ла о поартэ пынэ ла чялалтэ.
24 Ndipo munthuyo anapita nane ku mbali yakummwera ndipo ndinaona chipata chakummwera. Iye anayeza mphuthu zake ndi khonde ndipo zinali ndi miyeso yofanana ndi ya zina zija.
М-а дус ын партя де мязэзи, унде се афла поарта де ла мязэзи. Й-а мэсурат стылпий ши тинда, каре авяу ачеяшь мэсурэ.
25 Mʼzipinda za chipata cholowera chimenechi ndi mʼkhonde lake munali mipata yofanana ndi ya mʼzipinda zina. Mulitali mwake munali mamita 27, mulifupi mwake munali mamita 13.
Поарта ачаста ши тинда ей авяу ферестре де жур ымпрежур, ка ши челелалте ферестре, ши поарта ера лунгэ де чинчзечь де коць ши латэ де доуэзечь ши чинч де коць.
26 Chipatacho chinali ndi makwerero asanu ndi awiri ndi khonde kotsirizira kwake. Chipindacho chinali ndi zojambula za kanjedza ku mbali zonse za makoma.
Ла еа те суяй пе о скарэ де шапте трепте, яр тинда ей ера ын партя динэунтру; пе стылпь ера кыте ун финик де фиекаре парте.
27 Bwalo lamʼkati linalinso ndi chipata kummwera. Munthuyo analiyeza kuchokera ku chipata chimenechi mpaka ku chipata chakunja. Kutalika kwake kunali mamita makumi asanu.
Куртя динэунтру авя о поартэ ынспре мязэзи; а мэсурат де ла о поартэ пынэ ла чялалтэ спре мязэзи о сутэ де коць.
28 Ndipo munthu uja anandilowetsa mʼbwalo lamʼkati kudzera ku chipata chakummwera. Anayeza chipatachi ndipo chinali chofanana ndi zinzake zija.
М-а дус ын куртя динэунтру, пе поарта де мязэзи. А мэсурат поарта де мязэзи ши а гэсит кэ авя ачеяшь мэсурэ.
29 Zipinda zake za alonda, makoma ake ndi khonde lake zinali zofanana ndi zina zija. Chipata cholowera ndi khonde lake zinali ndi mipata mʼmbali zonse. Mulitali mwake munali mamita 27 ndipo mulifupi munali mamita 13.
Одэиле ей де пазэ, стылпий ши тинда ей авяу ачеяшь мэсурэ. Поарта ачаста ши тинда ей авяу ферестре де жур ымпрежур ши поарта ера лунгэ де чинчзечь де коць ши латэ де доуэзечь ши чинч де коць.
30 (Khonde lililonse la makonde atatu a zipata zolowera bwalo lamʼkati aja linali la mamita ozungulira mʼbwalo lamʼkati anali mamita 13 mulitali mwake, mamita awiri ndi theka mulifupi mwake).
(Де жур ымпрежур ерау тинде лунӂь де доуэзечь ши чинч де коць ши лате де чинч коць.)
31 Khonde lake linayangʼanana ndi bwalo lakunja. Pa mphuthu pake anajambulapo zithunzi za kanjedza mbali zonse ziwiri, ndipo linali ndi makwerero asanu ndi atatu.
Тинда порций дэдя ын куртя де афарэ; пе стылпий ей ерау финичь ши опт трепте пентру суит ла поартэ.
32 Kenaka munthuyo anapita nane ku bwalo la mʼkati mbali ya kummawa, ndipo anayeza chipata cholowera; chinali chofanana ndi zinzake zina zija.
М-ам дус апой ын куртя динэунтру, пе интраря де рэсэрит. А мэсурат поарта ши а гэсит кэ авя ачеяшь мэсурэ.
33 Zipinda zake za alonda, makoma ake ndi khonde lake zinali zofanana ndi zina zija. Chipata cholowera ndi khonde lake chinali ndi mipata mʼmbali zonse. Mulitali mwake munali mamita 27 ndipo mulifupi mwake munali mamita 13.
Одэиле ей де пазэ, стылпий ей ши тинда ей авяу ачеяшь мэсурэ. Поарта ачаста ши тинда ей авяу ши еле ферестре де жур ымпрежур, лунӂь де чинчзечь де коць ши лате де доуэзечь ши чинч.
34 Khonde lake linayangʼanana ndi bwalo lakunja. Pa mphuthu pake anajambulapo zithunzi za kanjedza mbali zonse ziwiri, ndipo linali ndi makwerero asanu ndi atatu.
Тинда ей дэдя ын куртя де афарэ; де фиекаре парте ерау финичь пе стылпь ши опт трепте пентру суит ла поартэ.
35 Kenaka anapita nane ku chipata chakumpoto ndipo anachiyeza. Chinali chofanana ndi zina zija.
М-а дус ла поарта де мязэноапте. А мэсурат-о ши а гэсит ачеяшь мэсурэ.
36 Zipinda zake za alonda, makoma ake ndiponso khonde lake zinali zofanana ndi zina zija, ndipo chinalinso ndi mipata mbali zonse ziwiri. Mulitali mwake munali mamita 27 ndipo mulifupi mwake munali mamita 13.
Ши еа авя одэй де пазэ, стылпь, тиндэ ши ферестре де жур ымпрежур; ера лунгэ де чинчзечь де коць ши латэ де доуэзечь ши чинч де коць.
37 Khonde lake limayangʼanana ndi bwalo lakunja. Pa mphuthu zake anajambulapo zithunzi za kanjedza mbali zonse ziwiri, ndipo linali ndi makwerero asanu ndi atatu.
Тинда ей дэдя ын куртя де афарэ; де фиекаре парте ерау чинч финичь пе стылпий ей ши опт трепте пентру суит ла поартэ.
38 Panali chipinda ndipo khomo lake linali pafupi ndi khonde la chipata cholowera chamʼkati. Mʼchipinda mʼmenemo ankatsukira nyama ya nsembe yopsereza.
Ера о одае каре се дескидя спре тинда порций; аколо требуяу спэлате ардериле-де-тот.
39 Pa khonde la chipatacho panali matebulo awiri, lina kuno lina uko. Ankapherapo nsembe zopsereza, nsembe zopepesera machimo ndi nsembe zopepesera kupalamula.
Ын тинда порций ерау де фиекаре парте доуэ месе, пе каре требуяу ынжунгияте ардеря-де-тот, жертфа де испэшире ши жертфа пентру винэ.
40 Panali matebulo anayi, awiri a iwo anali kunja kwa khoma la khonde pafupi ndi makwerero olowera pa chipata chakumpoto ndi awiri enawo anali mbali inayo ya makwerero.
Ынтр-уна дин пэрциле де афарэ, кум те суй ла интраря порций де мязэноапте, ерау доуэ месе; ши ын чялалтэ парте, спре тинда порций, ерау ярэшь доуэ месе.
41 Choncho ku mbali imodzi ya chipata kunali matebulo anayi, ndiponso ku mbali inayo kunali matebulo anayi. Onse pamodzi anali matebulo asanu ndi atatu. Pa matebulopo ankapherapo nyama za nsembe zopsereza.
Ын челе доуэ пэрць але порций, се афлау астфел патру месе де о парте ши патру месе де чялалтэ, де тоате опт месе, пе каре требуяу ынжунгияте жертфеле.
42 Matebulo anayiwa anali a miyala yosema. Lililonse mulitali mwake linali la masentimita 75, mulifupi mwake linali la masentimita 75, ndipo msinkhu wake unali wa masentimita makumi asanu. Pa matebulopo amayikapo zipangizo zophera nsembe zopsereza ndi nsembe zina.
Ын фаца меселор пентру жертфе, май ерау пентру ардериле-де-тот патру месе де петре чоплите, лунӂь де ун кот ши жумэтате, лате де ун кот ши жумэтате ши ыналте де ун кот; пе меселе ачестя требуяу пусе унелтеле ку каре се жунгияу вителе пентру ардерь-де-тот ши пентру челелалте жертфе.
43 Choncho pa matebulopo ankayikapo nyama za nsembe zopsereza. Mbedza zitatu zazitali ngati chikhatho amazikoleka pa makoma pozungulira ponse.
Пе динэунтру, каса авя де жур ымпрежур первазурь де ун лат де мынэ каре служяу ка месе пентру карня жертфелор.
44 Munthu uja anapita nane mʼkati mwa bwalo ndipo ndinaona zipinda ziwiri. Chimodzi chinali pafupi ndi chipata chakumpoto kuyangʼana kummwera ndi china chinali pafupi ndi chipata chakummwera kuyangʼana kumpoto.
Афарэ дин поарта динэунтру ерау доуэ одэй пентру кынтэрець ын куртя динэунтру: уна ера алэтурь де поарта де мязэноапте ши авя фаца спре мязэзи, чялалтэ ера алэтурь де поарта де мязэзи ши авя фаца спре мязэноапте.
45 Munthuyo anandiwuza kuti, “Chipinda chimene chikuyangʼana kummwera ndi cha ansembe amene amayangʼanira Nyumba ya Mulungu,
Ел мь-а зис: „Одая ачаста динспре мязэзи есте пентру преоций каре ынгрижеск де служба Темплулуй.
46 ndipo chipinda chimene chikuyangʼana kumpoto ndi cha ansembe amene amayangʼanira guwa lansembe. Amenewa ndiwo ana a Zadoki, ndipo ndi okhawo mwa zidzukulu za Levi amene ayenera kutumikira pamaso pa Yehova mʼNyumba ya Mulungu.”
Яр одая динспре мязэноапте есте пентру преоций каре ынгрижеск де служба алтарулуй. Фиий луй Цадок сунт ачея каре, дин фиий луй Леви, се апропие де Домнул, ка сэ-Й служяскэ.”
47 Kenaka munthuyo anayeza bwalo; linali lofanana mbali zonse kutalika kwake, mulitali mwake munali mamita 53, ndipo mulifupi mwake munali mamita 53. Ndipo guwa lansembe linali kutsogolo kwa Nyumba ya Mulungu.
А мэсурат куртя, каре ера ын патру колцурь, лунгэ де о сутэ де коць. Алтарул ера ынаинтя касей.
48 Munthuyo anapita nane pa khonde la Nyumba ya Mulunguyo. Anayeza mphuthu za khondelo ndipo zinali mamita awiri ndi theka mbali zonse. Mulifupi mwa chipatacho munali mamita asanu ndi awiri ndipo mulifupi mwa makoma ake munali mamita awiri mbali zonse.
М-а дус ын тинда касей. А мэсурат стылпий тиндей ши а гэсит чинч коць де о парте ши чинч коць де чялалтэ. Лэцимя порций ера де пайспрезече коць, яр перетеле де пе латуриле порций ера де трей коць де о парте ши де трей коць де чялалтэ.
49 Mulitali mwa khonde munali mamita khumi, mulifupi mwake munali mamita asanu ndi limodzi kuchokera kutsogolo mpaka kumbuyo. Panali makwerero khumi, ndipo mbali zonse kunali nsanamira.
Тинда авя о лунӂиме де доуэзечь де коць ши о лэциме де дойспрезече коць; те суяй ла еа пе зече трепте. Лынгэ стылпь май ерау ши алць стылпь, унул де о парте ши алтул де алта.

< Ezekieli 40 >