< Ezekieli 4 >

1 Mulungu anati, “Iwe mwana wa munthu, tsopano tenga njerwa, uliyike pamaso pako ndipo ujambulepo chithunzi cha mzinda wa Yerusalemu.
“Ngem sika, anak ti tao, mangalaka iti ladrilio ket ikabilmo daytoy iti sangoanam. Ket iti rabaw daytoy, ikur-itmo ti siudad ti Jerusalem.
2 Ndipo uwuzinge mzindawo motere: uwumangire nsanja zowuzinga, uwumbire mitumbira ya nkhondo, uwumangire misasa ya nkhondo ndipo uyike zida zogumulira kuzungulira mzindawo.
Ket mangikabilka iti manglakub iti daytoy, ken mangipatakderka kadagiti sarikedked a maibusor iti daytoy. Mangikabilka iti pagkalay-atan dagiti kabusor ken mangaramidka kadagiti kampo iti aglikmut daytoy. Mangikabilka iti sinan-maso a pagrakrak iti aglawlaw daytoy.
3 Kenaka utenge chiwaya chachitsulo uchiyike ngati khoma lachitsulo pakati pa iwe ndi mzindawo. Uyangʼanitsitse mzindawo ndipo udzakhala wozingidwa ndi nsanja za nkhondo. Choncho umangire nsanja zankhondo. Chimenechi chidzakhala chizindikiro kwa Aisraeli.
Ket mangalaka iti landok a pariok, ket aramatem daytoy a kas landok a bakud iti nagbaetan ti bagim ken ti siudad. Sumangoka a makaung-unget iti siudad, ta malakubto daytoy. Isu a mangikabilka iti manglakub iti daytoy! Agpaayto daytoy a pagilasinan iti balay ti Israel.
4 “Tsono iwe ugonere kumanzere kwako ndipo ndidzayika pa iwe tchimo la Aisraeli. Iwe udzasenza tchimolo masiku onse amene udzagonere mbali imeneyo.
Kalpasanna, agiddaka nga agsikig iti kannigidmo ket lak-amem ti basol ti balay ti Israel; baklayemto ti basolda segun iti bilang dagiti aldaw a nakaiddaka maibusor iti balay ti Israel.
5 Ine ndakuyikira masiku okwana 390 malingana ndi zaka za machimo awo. Umu ndi mmene udzasenzere machimo a Aisraeli.
Tinudinganka iti maysa aldaw a katukad iti tunggal tawen a pannakadusada: 390 nga aldaw! Iti kastoy a wagas, baklayemto ti basol ti balay ti Israel.
6 “Utatha zimenezo udzagonerenso mbali ya kudzanja lamanja, ndipo udzasenza machimo a anthu a ku Yuda masiku makumi anayi, tsiku lililonse kuyimira chaka chimodzi.
Inton maileppasmo dagitoy nga aldaw, iti maikadua a gundaway ket agiddaka a nakasikig iti makannawanmo, ta baklayemto ti basol ti balay ti Juda iti las-ud ti uppat a pulo nga aldaw. Tinudinganka iti maysa nga aldaw iti tunggal tawen.
7 Tsono udzayangʼanitsitse nsanja za nkhondo zozinga. Dzanja la mkanjo wako utalikwinya ndi dzanja lako utakweza, udzalosere modzudzula Yerusalemu.
Ket saanmo nga isina ti panagkitam iti pannakalakub ti Jerusalem, a nakalislis ti manggas ti badom ket agipadtokanto iti maibusor iti siudad.
8 Ine ndidzakumanga ndi zingwe kotero kuti sudzatha kutembenukira uku ndi uku mpaka utatsiriza masiku akuzingidwa ako.
Ta kitaem! parparautanka tapno saanka a makaballikid agingga a maileppasmo dagiti aldaw a pananglakubmo.
9 “Tsono tenga tirigu ndi barele, nyemba ndi mphodza, mapira ndi mchewere; ndipo uyike zonsezi mʼmbale imodzi ndipo upange buledi wako. Uzidya pa masiku 390 amene udzakhala ukugonera mbali imodzi.
Mangalaka iti trigo, sebada, bubukel, patani, miho ken espelta; paglalaokem dagitoy iti maysa a pagkargaan ket manglutoka iti tinapay a kanemto segun iti bilang dagiti aldaw nga agiddaka a nakasikig. Ta kanemto daytoy iti las-ud ti 390 nga aldaw!
10 Uyeze theka la kilogalamu la chakudyacho kuti uzidya tsiku lililonse kamodzi kokha.
Daytoyto ti kanem a taraonmo: duapulo a siklo kada aldaw. Mangankanto iti maituding a pannanganmo.
11 Uyezenso zikho ziwiri zamadzi ndipo uzimwa tsiku ndi tsiku.
Ken uminomkanto iti dua a baso. Inumemto daytoy iti maituding a pannanganmo.
12 Uzidya chakudya chako ngati momwe amadyera keke ya barele. Uzidzaphika chakudyacho anthu akuona pogwiritsa ntchito ndowe ya munthu ngati nkhuni.”
Kanemto daytoy a kas kadagiti bibingka a naaramid iti sebada, ngem lutoemto daytoy iti imatangda babaen iti namaga a rugit ti tao!”
13 Yehova anati, “Chimodzimodzi anthu a Israeli adzadya chakudya chodetsedwa ku mayiko achilendo kumene Ine ndidzawapirikitsira.”
Ta kuna ni Yahweh, “Ti kayat a sawen daytoy a narugitto ti tinapay a kanen dagiti tattao ti Israel, kadagiti nasion a pangiwarawaraakto kadakuada.”
14 Koma ine ndinati, “Zisatero, Ambuye Yehova! Ine sindinadziyipitsepo pa zachipembedzo. Kuyambira ubwana wanga mpaka tsopano, sindinadyepo kanthu kalikonse kopezeka katafa kapena kophedwa ndi zirombo za kutchire. Palibe nyama yodetsedwa pa zachipembedzo imene inalowa pakamwa panga.”
Ngem kinunak, “Saan, Yahweh nga Apo! Saanak a pulos a nagbalin a narugit! Saanak pay a pulos a nangan iti aniaman a natay wenno aniaman a pinatay dagiti ayup, manipud kinaagtutubok nga agingga ita, ken awan pay ti immuneg a narugit a karne iti ngiwatko!”
15 Iye anati, “Chabwino, ndidzakulola kuti uphike buledi wako ndi ndowe za ngʼombe mʼmalo mwa ndowe za munthu.”
Isu a kinunana kaniak, “Kitaem! inikkanka kadagiti takki ti baka imbes a rugit ti tao tapno mailutom ti tinapaymo iti rabaw ti takki ti baka.”
16 Pambuyo pake anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, anthu a ku Yerusalemu ndidzawachepetsera chakudya. Anthuwo adzadya chakudya chochita kuyeza ndipo azidzadya mwa nkhawa. Azidzamwanso madzi ochita kuyeza ndiponso mwa mantha.
Kinunana pay kaniak, “Anak ti tao, kitaem! Isardengkon ti panangtedko iti taraon iti Jerusalem, ket madandanagandanto a mangan iti tinapay bayat a maibunbunong daytoy ken agpigergerda nga umin-inom iti danum bayat a maibunbunong daytoy.
17 Ndidzachita zimenezi kuti adzasowe chakudya ndi madzi. Choncho adzachita nkhawa akumapenyana ndipo adzatheratu ndi kuwonda chifukwa cha machimo awo.”
Gapu ta agkurangdanto iti taraon ken danum, maupaydanto iti kabsatda ket kasla marunawda gapu iti kinadakesda.”

< Ezekieli 4 >