< Ezekieli 35 >

1 Yehova anandiyankhula kuti:
Ilizwi likaThixo lafika kimi lisithi:
2 “Iwe mwana wa munthu, yangʼana phiri la Seiri; yankhula moliyimba mlandu ndipo
“Ndodana yomuntu, khangelisa ubuso bakho eNtabeni iSeyiri; uphrofithe okubi ngayo
3 awawuze anthu a kumeneko kuti zimene ndikuyankhula Ine Ambuye Yehova ndi izi: Inu anthu a ku mapiri a Seiri ndikudana nanu. Ndidzatambasula dzanja langa kulimbana nanu, ndipo ndidzasandutsa dziko lanu kukhala chipululu.
uthi: ‘Nanku okutshiwo nguThixo Wobukhosi: Ngimelane lawe, Ntaba Seyiri, njalo ngizakwelula isandla sami ukumelana lawe ngikwenze ube lugwadule oluphundlekileyo.
4 Mizinda yanu ndidzayisandutsa mabwinja, ndipo dziko lanu lidzasanduka chipululu. Zikadzachitika izi mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Ngizakwenza amadolobho akho abe ngamanxiwa lawe uzachithwa. Lapho-ke uzakwazi ukuthi mina nginguThixo.
5 “Munali adani a Israeli nthawi zonse, ndipo munkalola kuti Aisraeli aphedwe pa nkhondo pa nthawi ya mavuto awo, pa nthawi imene chilango chawo chinafika pachimake.
Ngoba wagcina inzondo yasendulo wanikela ama-Israyeli enkembeni ngesikhathi sosizi lwawo, lapho isijeziso sawo sasesifike ekucineni,
6 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pali Ine wamoyo, ndithu ndidzakukanthani. Imfa idzakulondolani. Popeza sunadane nako kukhetsa magazi, imfa idzakulondola.
ngakho-ke ngeqiniso elinjengoba ngikhona, kutsho uThixo Wobukhosi, ngizakunikela ekuchithekeni kwegazi njalo kuzakulandela.
7 Phiri la Seiri ndidzalisandutsa chipululu ndipo ndidzapha onse amene amapita nabwerera kumeneko.
Ngizakwenza iNtaba iSeyiri ibe lugwadule oluphundlekileyo, njalo ngiqede kuyo bonke abafika bahambe.
8 Ndidzaza mapiri ake ndi mitembo. Ophedwa pa nkhondo adzagwera pa zitunda zanu, zigwa zanu ndi mʼmitsinje yanu yonse.
Ngizagcwalisa izintaba zakho ngababuleweyo; labo ababulawe ngenkemba bazawela phezu kwamaqaqa akho lasezigodini zakho kanye lasezindongeni zakho zonke.
9 Ndidzasandutsa dziko lanu kukhala chipululu mpaka muyaya, ndipo mʼmizinda yanu simudzakhalanso anthu. Zikadzachitika izi mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Ngizakwenza uchitheke okwanininini; amadolobho akho kawayikuhlalwa muntu. Lapho-ke uzakwazi ukuthi mina nginguThixo.
10 “Inu munanena kuti, ‘Mitundu iwiri iyi ya anthu, Yuda ndi Israeli, pamodzi ndi mayiko awo omwe idzakhala yathu.’ Munanena chomwechi ngakhale kuti Ine Yehova ndinali momwemo.
Ngoba wena uthe, “Izizwe lezi ezimbili lamazwe la amabili kuzakuba ngokwethu njalo sizakuthatha,” lanxa mina Thixo ngangikhonapho.
11 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pali Ine wamoyo, ndithu ndidzachita nanu monga munachita ndi anthu a ku Yuda ndi Israeli poonetsa mkwiyo wanu, nsanje yanu ndi chidani chanu pa iwo. Ndikadzakulangani mudzandidziwadi pakati panupo.
Ngakho-ke ngeqiniso elinjengoba ngikhona, kutsho uThixo Wobukhosi, ngizakuphatha ngokufanele ukuthukuthela lobukhwele owakubonakalisayo ekubazondeni kwakho njalo ngizakwenza mina ngazakale phakathi kwabo lapho sengikwahlulela.
12 Ndipo mudzadziwa kuti Ine Yehova ndinamva mawu anu onse onyoza amene munanena molimbana ndi mapiri a Israeli. Inu munati, ‘Mapiri a Israeli asanduka bwinja, ndipo aperekedwa kwa ife kuti tiwawononge.’
Lapho-ke uzakwazi ukuthi mina Thixo sengizizwile zonke izinto ezenyanyekayo owazitshoyo ngezintaba zako-Israyeli. Wathi, “Sezichithiwe njalo sezinikelwe kithi ukuba sizitshwabadele.”
13 Mawu anu amene munayankhula monyada kundinyoza Ine ndinawamva.
Wazikhukhumeza kubi ngami njalo wakhuluma kubi ngami kungekho kuzibamba, njalo ngakuzwa lokho.
14 Ine Ambuye Yehova ndikuti: Dziko lonse lapansi lidzasangalala pamene ndidzakusandutsani bwinja.
Nanku okutshiwo nguThixo Wobukhosi: Kuzakuthi umhlaba wonke uthokoze, mina ngizakwenza uphundleke.
15 Monga momwe inu munasangalala pamene anthu anga Aisraeli anagwa, Inenso ndidzakuchitani chimodzimodzi. Udzasanduka bwinja, iwe Phiri la Seiri, iwe ndi dziko lonse la Edomu. Zikadzatero anthu onse adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
Ngoba wena wathokoza lapho ilifa lendlu ka-Israyeli lichitheka, leyo yiyo indlela engizakuphatha ngayo. Uzaphundleka, wena Ntaba yeSeyiri, wena kanye le-Edomi yonke. Lapho-ke bazakwazi ukuthi mina nginguThixo.’”

< Ezekieli 35 >