< Ezekieli 35 >

1 Yehova anandiyankhula kuti:
BOEIPA ol he kai taengla ha pawk bal tih,
2 “Iwe mwana wa munthu, yangʼana phiri la Seiri; yankhula moliyimba mlandu ndipo
“Hlang capa aw, Seir tlang te na maelhmai khueh thil lamtah tonghma thil lah.
3 awawuze anthu a kumeneko kuti zimene ndikuyankhula Ine Ambuye Yehova ndi izi: Inu anthu a ku mapiri a Seiri ndikudana nanu. Ndidzatambasula dzanja langa kulimbana nanu, ndipo ndidzasandutsa dziko lanu kukhala chipululu.
Ka Boeipa Yahovah loh a thui he a taengah thui pah. Kai loh Seir tlang nang te kam pai thil. Nang taengla ka kut kan thueng vetih nang te khopong neh rhaerhap la kang khueh ni.
4 Mizinda yanu ndidzayisandutsa mabwinja, ndipo dziko lanu lidzasanduka chipululu. Zikadzachitika izi mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Na khopuei te imrhong ka khueh vetih namah te khopong la na om vaengah kai he BOEIPA la nan ming bitni.
5 “Munali adani a Israeli nthawi zonse, ndipo munkalola kuti Aisraeli aphedwe pa nkhondo pa nthawi ya mavuto awo, pa nthawi imene chilango chawo chinafika pachimake.
Nang ham kumhal kah thunkha thunhling la om ham neh thaesainah a tloihsoi tue kah a rhainah tue ah tah Israel ca rhoek te cunghang kut ah na lun.
6 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pali Ine wamoyo, ndithu ndidzakukanthani. Imfa idzakulondolani. Popeza sunadane nako kukhetsa magazi, imfa idzakulondola.
Te dongah kai tah hingnah ni tite ka Boeipa Yahovah kah olphong ni. Na thii ham ka saii vetih thii loh namah n'hloem ni. A thii pawt te na hmuhuet dongah thii. oh namah n'hloem ni.
7 Phiri la Seiri ndidzalisandutsa chipululu ndipo ndidzapha onse amene amapita nabwerera kumeneko.
Seir tlang te khopong phoeikah khopong la ka khueh vetih te lamkah aka voei aka bal khaw ka saii pueng ni.
8 Ndidzaza mapiri ake ndi mitembo. Ophedwa pa nkhondo adzagwera pa zitunda zanu, zigwa zanu ndi mʼmitsinje yanu yonse.
A tlang te a rhok ka hah sak ni. Na som neh na kolrhawk khaw, na sokca boeih te cunghang dongah a rhok la cungku uh ni.
9 Ndidzasandutsa dziko lanu kukhala chipululu mpaka muyaya, ndipo mʼmizinda yanu simudzakhalanso anthu. Zikadzachitika izi mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Nang te kumhal kah khopong la kang khueh tih na khopuei kah khosa loh kho a sak pawt vaengah kai he BOEIPA la nan ming uh bitni.
10 “Inu munanena kuti, ‘Mitundu iwiri iyi ya anthu, Yuda ndi Israeli, pamodzi ndi mayiko awo omwe idzakhala yathu.’ Munanena chomwechi ngakhale kuti Ine Yehova ndinali momwemo.
'Namtom rhoi neh khohmuen rhoi khaw ka taengah om vetih m'pang uh bitni,’ na ti sitoe cakhaw BOEIPA om lah lahko te.
11 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pali Ine wamoyo, ndithu ndidzachita nanu monga munachita ndi anthu a ku Yuda ndi Israeli poonetsa mkwiyo wanu, nsanje yanu ndi chidani chanu pa iwo. Ndikadzakulangani mudzandidziwadi pakati panupo.
Te dongah kai tah hingnah ni tite ka Boeipa Yahovah kah olphong ni. Na thintoek tarhing neh na thatlainah tarhing ah kan saii ni. Na hmuhuetnah neh amih na saii dongah nang lai kan tloek vaengkah bangla amih taengah ka phoe ni.
12 Ndipo mudzadziwa kuti Ine Yehova ndinamva mawu anu onse onyoza amene munanena molimbana ndi mapiri a Israeli. Inu munati, ‘Mapiri a Israeli asanduka bwinja, ndipo aperekedwa kwa ife kuti tiwawononge.’
Te vaengah kai he BOEIPA la nan ming bitni. Nang kah kokhahnah cungkuem te ka yaak coeng. Israel tlang rhoek te na voek vaengah tah, “Pong tah pong uh tih kaimih taengah cakkoi la tloeng uh coeng, ' na ti.
13 Mawu anu amene munayankhula monyada kundinyoza Ine ndinawamva.
Na ka nen tah kai taengah na khuet van tih na ol neh kai taengah na rhoekoe aih khaw kamah loh ka yaak ta.
14 Ine Ambuye Yehova ndikuti: Dziko lonse lapansi lidzasangalala pamene ndidzakusandutsani bwinja.
Ka Boeipa Yahovah loh he ni a. thui. Diklai pum ko a hoe vaengah nang te khopong kang khueh ni.
15 Monga momwe inu munasangalala pamene anthu anga Aisraeli anagwa, Inenso ndidzakuchitani chimodzimodzi. Udzasanduka bwinja, iwe Phiri la Seiri, iwe ndi dziko lonse la Edomu. Zikadzatero anthu onse adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
Israel imkhui kah rho a pong vaengkah te na kohoenah van dongah nang te kan saii ni. Seir tlang neh Edom pum te khopong la boeih na om vaengah kai he BOEIPA la a ming uh bitni,” a ti.

< Ezekieli 35 >