< Ezekieli 35 >
1 Yehova anandiyankhula kuti:
Hina Gode da nama amane sia: i,
2 “Iwe mwana wa munthu, yangʼana phiri la Seiri; yankhula moliyimba mlandu ndipo
“Dunu egefe! Idome fi ilima fofada: ma!
3 awawuze anthu a kumeneko kuti zimene ndikuyankhula Ine Ambuye Yehova ndi izi: Inu anthu a ku mapiri a Seiri ndikudana nanu. Ndidzatambasula dzanja langa kulimbana nanu, ndipo ndidzasandutsa dziko lanu kukhala chipululu.
Na, Ouligisudafa Hina Gode, Na sia: ilima alofele olelema, amane, ‘Idome goumi! Na da dilia ha lai. Na da dili gugunufinisimu.
4 Mizinda yanu ndidzayisandutsa mabwinja, ndipo dziko lanu lidzasanduka chipululu. Zikadzachitika izi mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Na da dilia moilai amola soge huluane wadela: lesimu. Amasea, dilia da Na da Hina Gode dawa: mu.
5 “Munali adani a Israeli nthawi zonse, ndipo munkalola kuti Aisraeli aphedwe pa nkhondo pa nthawi ya mavuto awo, pa nthawi imene chilango chawo chinafika pachimake.
Dilia da eso huluane Isala: ili fi ilima ha laiwane esalu. Amola Isala: ili fi da ilia dagomusa: se bidi laloba, amo esoga dilia da Isala: ili hame fidi, be udigili Isala: ili fi dunu huluane medole legelalu ba: i.
6 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pali Ine wamoyo, ndithu ndidzakukanthani. Imfa idzakulondolani. Popeza sunadane nako kukhetsa magazi, imfa idzakulondola.
Amaiba: le, Na, Ouligisudafa Fifi Ahoanusu Hina Gode da Na Dioba: le amane sia: sa, ‘Dilia da bogomu. Hobeale masunu da hamedei. Dilia da fane legesu hou hamonanu, amola dilia fane legesu hou amoga bogomu.
7 Phiri la Seiri ndidzalisandutsa chipululu ndipo ndidzapha onse amene amapita nabwerera kumeneko.
Na da Idome agolo soge gugunufinisimu, amola nowa amodili ahoasea, amo medole legemu.
8 Ndidzaza mapiri ake ndi mitembo. Ophedwa pa nkhondo adzagwera pa zitunda zanu, zigwa zanu ndi mʼmitsinje yanu yonse.
Na da goumi huluane amo bogoi da: i hodo amoga dedebolesimu, amola agolo amola fago amoga dunu da gegesu ganodini bogoi, ilia da: i hodo dedebolesimu.
9 Ndidzasandutsa dziko lanu kukhala chipululu mpaka muyaya, ndipo mʼmizinda yanu simudzakhalanso anthu. Zikadzachitika izi mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Na eso huluane agoaiwane dialoma: ne, dili wadela: lesimu amola dilia moilai amo ganodini fa: no, dunu da hamedafa esalebe ba: mu.
10 “Inu munanena kuti, ‘Mitundu iwiri iyi ya anthu, Yuda ndi Israeli, pamodzi ndi mayiko awo omwe idzakhala yathu.’ Munanena chomwechi ngakhale kuti Ine Yehova ndinali momwemo.
Na, Hina Gode da Isala: ili fi amola Yuda fi ela Gode esala. Be dilia da giadofale, amo fi aduna amola ela soge huluane, da dilia soge dialoma: ne sia: i.
11 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pali Ine wamoyo, ndithu ndidzachita nanu monga munachita ndi anthu a ku Yuda ndi Israeli poonetsa mkwiyo wanu, nsanje yanu ndi chidani chanu pa iwo. Ndikadzakulangani mudzandidziwadi pakati panupo.
Amaiba: le, Na, Ouligisudafa Hina Gode, Na da Fifi Ahoanusu Godeba: le, amane sia: sa, ‘Na da dilia ougi hou amola mudasu amola Na fi ilima higasu hou, amoba: le Na da dilima dabe imunu. Amola Na fi dunu ilia da amane dawa: mu. Na da dilima se bidi iabe ea bai da dilia Na fi ilima wadela: le hamoi.
12 Ndipo mudzadziwa kuti Ine Yehova ndinamva mawu anu onse onyoza amene munanena molimbana ndi mapiri a Israeli. Inu munati, ‘Mapiri a Israeli asanduka bwinja, ndipo aperekedwa kwa ife kuti tiwawononge.’
Dilia da higale agoane sia: i, ‘Isala: ili goumi da wadela: lesi dagoi. Amola dilia amo na dagomu da defea, sia: i. Be Na, Hina Gode, da amo sia: nabi. Amola, dilia da Na se dabe iasu ba: sea, amo dawa: mu.
13 Mawu anu amene munayankhula monyada kundinyoza Ine ndinawamva.
Dilia da Nama nimi bagade hidale sia: i. Amola amo hidale gasa fi sia: , Na da nabi.”
14 Ine Ambuye Yehova ndikuti: Dziko lonse lapansi lidzasangalala pamene ndidzakusandutsani bwinja.
Ouligisudafa Hina Gode da amane sia: sa, “Na da dili baligili wadela: lesisia, osobo bagade fifi asi gala huluane da dilia dafai ba: beba: le, nodomu.
15 Monga momwe inu munasangalala pamene anthu anga Aisraeli anagwa, Inenso ndidzakuchitani chimodzimodzi. Udzasanduka bwinja, iwe Phiri la Seiri, iwe ndi dziko lonse la Edomu. Zikadzatero anthu onse adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
Dilia da Isala: ili (Na fi amola Na soge) ea wadela: lesisu ba: beba: le, nodosu, amo defele ilia da dilia dafai ba: beba: le, nodomu. Sie goumi amola Idome soge huluane da baligili wadela: lesi dagoi ba: mu. Amasea, dunu huluanedafa da Na da Hina Gode dawa: mu.”