< Ezekieli 29 >

1 Pa tsiku lakhumi ndi chiwiri la mwezi wakhumi, chaka chakhumi, Yehova anandiyankhula kuti:
Kum rha dongkah hla rha hnin hlai nit vaengah BOEIPA ol te kai taengla ha pawk tih,
2 “Iwe mwana wa munthu, tembenukira kwa Farao, mfumu ya Igupto, ndipo unenere modzudzula mfumuyo pamodzi ndi dziko lake.
“Hlang capa aw, Egypt manghai Pharaoh te na maelhmai khueh thil lamtah amah neh Egypt boeih te tonghma thil.
3 Uyiwuze mfumuyo kuti, ‘Ine Ambuye Yehova ndikuti, “‘Ndine mdani wako, iwe Farao mfumu ya Igupto, iwe ngʼona yayikulu yogona pakati pa mitsinje yako. Umanena kuti, ‘Mtsinje wa Nailo ndi wanga; ndinadzipangira ndekha.’
Voek lamtah ka Boeipa Yahovah loh a thui he thui pah. A sokko tuilung ah aka kol tuihnam puei, Egypt manghai Pharaoh nang kam pai thil coeng ne. Amah long tah kai taengah, 'Ka sokko he kai loh kamah kah la ka khueh,’ a ti.
4 Koma ndidzakukola ndi mbedza mʼkamwa mwako ndipo nsomba za mʼmitsinje yako zidzakangamira ku mamba ako. Tsono ndidzakutulutsa mu mtsinje mwakomo pamodzi ndi nsomba zimene zakangamira ku mamba ako.
Thisum, thisum neh na kam ah kan dueh vetih na sokko kah nga te na lip dongah ka ben ni. Na sokko khui lamloh nang kan doek vetih na sokko kah nga boeih khaw na lip dongah kap ni.
5 Ndidzakutaya ku chipululu, iwe pamodzi ndi nsomba zonse za mʼmitsinje yako. Udzagwera pamtetete kuthengo popanda munthu woti akutole kuti akayike maliro ako. Ndidzakusandutsa chakudya cha zirombo za pa dziko lapansi ndi mbalame za mlengalenga.
Namah neh na sokko nga boeih khaw na khuikah khosoek ah kam phap vetih, lohma tlai ah na cungku ni. Nang n'khoem pawt vetih n'coi mahpawh. Diklai mulhing ham neh vaan kah vaa ham nang te cakok la kam paek ni.
6 Motero aliyense amene amakhala mu Igupto adzadziwa kuti Ine ndine Yehova. “‘Iwe unakhala ngati ndodo yabango ku Aisraeli.
Te vaengah Egypt khosa boeih loh BOEIPA kamah ni tila a ming uh ni. Amih te Israel imkhui kah capu conghol la om coeng.
7 Pamene anakugwira unathethekera mʼmanja mwawo ndi kucheka mapewa awo. Pamene anakutsamira, unathyoka ndipo misana yawo inagwedezeka.
Amih loh nang te na kut, kut ah n'tuuk vaengah na paep tih amih kah laengpang boeih na phen pah. Nang dongah a hangdang vaengah nim te na khaem sumsoek tih amih kah cinghen boeih na phit sak.
8 “‘Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti, ndikubweretsera lupanga kuti lidzaphe anthu pamodzi ndi nyama zomwe.
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh he ni a thui. Kai loh nang taengah cunghang kang khuen vetih nang lamkah hlang neh rhamsa khaw ka thup ni.
9 Dziko la Igupto lidzasanduka lopanda anthu. Pamenepo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova. “‘Popeza iwe unati, ‘Mtsinje wa Nailo ndi wanga; ndinawupanga ndine,’
Tedae, 'Sokko te kamah ham tih kamah loh ka saii,’ a ti dongah Egypt khohmuen te khopong neh imrhong la a poeh vaengah BOEIPA kamah he a ming uh bitni.
10 nʼchifukwa chake Ine ndikudana nawe pamodzi ndi mitsinje yakoyo, ndipo ndidzasandutsa dziko la Igupto bwinja kuyambira chipululu cha Migidoli mpaka ku mzinda wa Asiwani, kukafika ku malire a Kusi.
Te dongah namah neh na sokko khaw ka pai thil coeng ne. Egypt kho te Syene Migdol lamloh Kusah khorhi due kholing khopong kah imrhong la ka khueh ni.
11 Palibe phazi la munthu kapena la nyama limene lidzapondepo. Kudzakhala kopanda anthu kwa zaka makumi anayi.
Te longah hlang kho loh paan pawt vetih rhamsa kho long khaw, te longah paan mahpawh. Kum sawmli khuiah khosa om mahpawh.
12 Ndidzasandutsa dziko la Igupto kukhala chipululu ngati zipululu za mayiko ena. Kwa zaka makumi anayi mizinda yakenso idzakhala yopasuka pakati pa mizinda yopasuka. Ndipo ndidzathamangitsira Aigupto pakati pa mitundu ya anthu ndi kuwabalalitsira mʼmayiko.
Egypt khohmuen te khopong la ka khueh vaengah diklai hman ah pong ni. A khopuei rhoek khaw khopuei rhoek lakli ah a khah vetih kum sawmli khopong la om ni. Egypt te namtom taengla ka taek ka yak vetih amih te diklai ah ka haeh ni.
13 “‘Komabe Ine Ambuye Yehova ndikuti: Pakutha pa zaka makumi anayi ndidzasonkhanitsa Aigupto onse kuchokera ku mayiko amene ndinawabalalitsirako.
Tedae ka Boeipa Yahovah loh he ni a thui. Kum sawmli a thok vaengah Egypt te ka taek ka yak nah pilnam taeng lamloh pahoi ka coi ni.
14 Ndidzachotsa Aiguptowo ku ukapolo ndipo ndidzawabwezera ku Patirosi kumene anachokera. Kumeneko iwo adzakhala ufumu wotsika.
Egypt thongtla te ka mael puei vetih amih te amah tuikong khohmuen kah Parthros khohmuen la ka bal sak ni. Te vaengah tlarhoel ram la pahoi om uh ni.
15 Udzakhala ufumu wotsika kwambiri kupambana maufumu ena onse ndipo sudzadzitukumula pakati pa mitundu ina. Ndidzawufowoketsa kwambiri kotero kuti sudzathanso kulamulira mitundu ya anthu.
Ram tom lakah tlarhoel la om vetih namtom soah koep cungphoek mahpawh. Amih te ka muei sak daengah ni namtom soah a taemrhai pawt eh.
16 Aisraeli sadzadaliranso Aigupto. Koma kuti chilango chawo chidzawakumbutsa tchimo lawo lija lofunafuna thandizo kuchokera ku Igupto. Pamenepo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Ambuye Yehova.’”
Te vaengah a taengla amamih hooi uh tih thaesainah aka poek rhoek kah pangtungnah la Israel imkhui he om voel mahpawh. Te phoeiah Kai he, ka Boeipa Yahovah ni tila a ming uh bitni,” a ti.
17 Pa tsiku loyamba la mwezi woyamba, chaka cha 27, Yehova anandiyankhula kuti:
Kum kul kum rhih, hla lamhma hnin at dongla a om vaengah BOEIPA ol kai taengla ha pawk tih,
18 “Iwe mwana wa munthu, kale Nebukadinezara mfumu ya Babuloni inagwiritsa ntchito ankhondo ake kukathira nkhondo mzinda wa Turo, mpaka munthu aliyense anachita dazi chifukwa chosenza katundu, ndipo ananyuka pa phewa. Komabe ngakhale iyeyo, kapena gulu lake lankhondo sanaphulepo kanthu pa ntchito yonse imene anayigwira polimbana ndi mzindawo.
“Hlang capa aw, Babylon manghai Nebukhanezar loh Tyre te a caem kah thohtatnah a len neh a thohtat sak coeng. A lu khaw boeih tlong tih laengpang boeih thool coeng. Tedae amah ham neh a caem ham thapang om hae pawh. Tyre lamkah thohtatnah lamloh a taengah a thohtat sak.
19 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti, Ine ndidzapereka Igupto kwa Nebukadinezara mfumu ya Babuloni, ndipo iyo idzatenga chuma chake ndi kuchifunkha ngati malipiro a gulu lake lankhondo.
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh he ni a thui. Kai loh Babylon manghai Nebukhanezar taengah Egypt khohmuen ka paek coeng he. Te vaengah a hlangping te a khuen pah vetih a kutbuem khaw a buem pah ni. A maeh te a poelyoe pah vetih a caem ham thapang la om ni.
20 Ndamupatsa Nebukadinezara Igupto ngati mphotho ya kulimbika kwake chifukwa iyo ndi gulu lake lankhondo anandigwirira ntchito, akutero Ambuye Yehova.
A taengah a thohtat te khaw kai ham a saii uh dongah, a thaphu la anih te Egypt khohmuen ka paek. He tah ka Boeipa Yahovah kah olphong ni.
21 “Pa nthawi imeneyo ndidzapereka mphamvu yatsopano pa Aisraeli, ndipo ndidzatsekula pakamwa pako, iwe, Ezekieli kuti uthe kuyankhula pakati pawo. Pamenepo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”
Te khohnin ah Israel imkhui ham ki cawn ni. Te vaengah nang te amih lakli ah ka ongnah ka paek vetih BOEIPA kamah he m'ming uh ni,” a ti.

< Ezekieli 29 >