< Ezekieli 26 >
1 Pa chaka cha khumi ndi chimodzi, tsiku loyamba la mwezi, Yehova anandiyankhula kuti:
Kum hlai at dongkah hla khat dongla a om vaengah kai taengla BOEIPA ol ha pawk tih,
2 “Iwe mwana wa munthu, anthu a ku Turo ananyogodola Yerusalemu kuti ‘Hii! Uja amene anali chipata choloweramo anthu a mitundu ina wawonongeka. Zitseko zake zatsekukira ife. Tidzalemera popeza wasanduka bwinja.’
Hlang capa aw, Tyre loh Jerusalem te, 'Ahuei, pilnam kah thohkhaih po coeng tih kai taengla ha mael coeng. Te dongah la anih a khah vaengah kai ka hah bitni,’ a ti.
3 Nʼchifukwa chake, Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ndidzakulangani, inu anthu a ku Turo. Ndidzakuyitanirani anthu a mitundu ina kuti adzakulangeni monga momwe mafunde amawombera pa Nyanja.
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh he ni a. thui. Kai lohTyre nang kam pai thil coeng tih namtom te nang taengah tuipuei tuiphu aka cet bangla muep kang khuen ni he.
4 Anthuwo adzawononga makoma a Turo ndi kugwetsa nsanja zake. Ndidzapala dothi lake ndipo ndidzamusandutsa thanthwe losalala.
Te vaengah Tyre vongtung te a phae uh vetih a rhaltoengim khaw a koengloeng uh ni. A pum dongkah laipi te ka kuet pah vetih anih te thaelpang aka tlaai la ka khueh ni.
5 Udzakhala poyanikapo makoka pakati pa nyanja. Ine Ambuye Yehova ndayankhula zimenezo. Udzasanduka chofunkha cha anthu a mitundu ina.
Te vaengah tuipuei laklung kah yaehtaboeih a yaalnah la poeh ni. Ka Boeipa Yahovah kah olphong he ka thui coeng dongah namtom ham maeh la poeh ni.
6 Anthu okhala ku mtunda adzasakazidwa ndi lupanga. Pamenepo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
A canu rhoek te khohmuen kah cunghang loh a ngawn vaengah BOEIPA kamah te m'ming uh bitni.
7 “Ine Ambuye Yehova ndikuti: Iwe Turo, ndidzakubweretsera Nebukadinezara, mfumu ya ku Babuloni mfumu ya mafumu, kuchokera kumpoto pamodzi ndi akavalo ndiponso magaleta, anthu okwera pa akavalo ndi gulu lalikulu la ankhondo.
Te dongah ka Boeipa Yahovah loh he ni a. thui. Manghai rhoek manghai tlangpuei lamkah Babylon manghai Nebukhanezar te marhang neh, leng neh, marhang caem neh, hlangping neh pilnam boeiping neh Tyre taengla ka thoeng sak coeng he.
8 Anthu okhala ku mtunda adzawapha ndi lupanga. Adzapanga mitumbira yankhondo ndi kukukwezera zishango kuti alimbane nawe.
Na canu rhoek te khohmuen ah cunghang neh a ngawn ni. Nang te buep n'to thil vetih nang te tanglung n'lun thil uh phoeiah nang te photlinglen m'bai thil ni.
9 Adzagwetsa makoma ako ndi zida zogumulira khoma ndi kugwetsa nsanja zako ndi nkhwangwa zake.
Na vongtung te a khongmawt neh pet a tung thil vetih na rhaltoengim te a cunghang neh a phil ni.
10 Akavalo ake adzakhala ochuluka kwambiri kotero kuti adzakukwirira ndi fumbi lawo. Makoma ako adzagwedezeka ndi mdidi wa akavalo, ngolo ndi magaleta pamene iye adzalowa pa zipata monga mmene amalowera mu mzinda umene makoma ake agwetsedwa.
A marhang cako lamkah laipi loh nang m'vuei ni. Marhang caem neh humhae neh leng ol ah na vongtung khaw tuen ni. Na vongka lamloh a moe ham vaengah khopuei khuirhai bangla ueth coeng.
11 Akavalo ake adzapondaponda mʼmisewu yako yonse ndi ziboda zawo. Adzapha anthu ako ndi lupanga. Mizati yako yolimba idzagwetsedwa.
A marhang khomae loh na tol boeih a taelh ni. Na pilnam te cunghang neh a ngawn vetih na sarhi kaam khaw diklai la bung ni.
12 Iwo adzafunkha chuma chako ndipo adzalanda zinthu zako za malonda. Adzagwetsa makoma ako ndi kuwononga nyumba zako zabwino. Adzaponya miyala yako, matabwa ako ndi dothi lako mʼnyanja.
Na thadueng a buem uh vetih na hnothungnah te a poelyoe uh ni. Na vongtung te a koengloeng uh vetih na sahnaih im khaw a phil uh ni. Na lungto neh na thing neh na laipi pataeng tui lung la a voeih uh ni.
13 Choncho ndidzathetsa phokoso la nyimbo zanu, ndipo kulira kwa apangwe ako sikudzamvekanso.
Na laa a lilup te ka paa sak vetih na rhotoeng ol khaw ya voel mahpawh.
14 Ndidzakusandutsa thanthwe losalala, ndipo udzakhala malo woyanikapo makoka a nsomba. Sudzamangidwanso, pakuti Ine Yehova ndayankhula, akutero Ambuye Yehova.
Nang te thaelpang aka tlaai la kang khueh vetih yaehtaboeih yaalnah la na poeh ni. BOEIPA kamah loh ka thui coeng dongah na thoh thai voel mahpawh. He tah ka Boeipa Yahovah kah olphong ni.
15 “Ine Ambuye Yehova ndikukuwuza, iwe mzinda wa Turo, kuti zilumba zidzagwedezeka pakumva za kugwa kwako ndiponso poona anthu opweteka akubuwula ndipo anthu akuphedwa pakati pako.
Ka Boeipa Yahovah loh Tyre ham he ni a. thui. Na cungkunah ol dongah pawt nim rhok a kii ham neh na laklung kah ngawnnah dongah ngawn ham vaengah sanglak rhoek a hinghuen?
16 Pamenepo mafumu a mʼmbali mwa nyanja adzatsika pa mipando yawo yaufumu. Adzayika pambali mikanjo yawo ndi kuvala zovala zawo zamakaka. Adzachita mantha ndipo adzakhala pansi akunjenjemera kosalekeza. Adzathedwa nzeru poona zimene zakugwera.
Te vaengah tuipuei khoboei boeih khaw a ngolkhoel dong lamloh suntla uh ni. A hnikul te a rhoe uh vetih a rhaekva himbai te khaw a pit uh ni. Thuennah te a bai uh vetih diklai ah ngol uh ni. Mikhaptok ah lakueng uh vetih na taengah pong uh ni.
17 Pamenepo adzayimba nyimbo yokudandaula ndipo adzati kwa iwe: “‘Nʼkuchita kuwonongeka chotere, iwe mzinda wotchuka, wodzaza ndi anthu a ku nyanja! Unali wamphamvu pa nyanja, iwe ndi nzika zako; unkaopseza anthu onse amene ankakhala kumeneko.
Te vaengah nang ham rhahlung ham phueih vetih nang te, 'Balae tih tuipuei khosa lamloh na milh, tuitunli neh a khuikah khosa rhoek soah khopuei thangthen neh tlungluen la na om ta. Amih a khuikah khosa boeih soah rhihnah a khueh uh ta.
18 Tsopano mayiko a mʼmbali mwa nyanja akunjenjemera chifukwa cha kugwa kwako; okhala pa zilumba nawonso agwidwa ndi mantha aakulu chifukwa cha kugwa kwako.’
Na cungkunah khohnin ah sanglak te lakueng tih na khum lamloh tuipuei kah sanglak rhoek khaw let uh.
19 “Mawu a Ine Ambuye Yehova ndi awa: Ndidzakusandutsa bwinja, ngati mizinda imene anthu sangathe kukhalamo. Ndidzakuphimba ndi madzi ozama a mʼnyanja, madzi amphamvu woti akumize.
Ka Boeipa Yahovah loh he ni a. thui. Khopuei nang te kang khueh vaengah khosa aka om pawh khopuei bangla n'khah ni. Te vaengah nang soah tuidung hang khuen vetih tui len loh nang n'khuk ni.
20 Ndidzakugwetsa pansi kuti ukhale pamodzi ndi anthu amvulazakale amene akutsikira ku manda. Ine ndidzakusunga ku dzenjeko ngati ku bwinja losiyidwa kalekale, pamodzi ndi anthu amene anafa kale motero sudzabwererako kukhala pakati pa anthu amoyo.
Te vaengah nang te tangrhom khuila aka suntla khosuen pilnam taengla kan suntlak sakni. Nang te tangrhom khuila aka suntla khosuen imrhong bangla diklai laedil ah kang om sak ni. Na om pawt daengah ni mulhing khohmuen ah kirhang khaw kam paek eh.
21 Ine ndidzakuthetsa mochititsa mantha, ndipo sudzakhalaponso. Anthu adzakufunafuna, koma sudzapezekanso, akutero Ambuye Yehova.”
Nang te mueirhih kam paek vaengah na om voel mahpawh. N'toem cakhaw kumhal duela koep m'hmu mahpawh. He tah ka Boeipa Yahovah kah olphong ni,” a ti.