< Ezekieli 22 >

1 Yehova anandiyankhula nati:
Hina Gode da nama amane sia: i,
2 “Iwe mwana wa munthu, kodi udzaweruza mzinda uwo wa anthu akupha anzawo? Tsono uwudzudzule chifukwa cha machitidwe ake onse onyansa
“Dunu egefe! Yelusaleme da fane legesu dunu amoga nabaiba: le, di da ema fofada: musa: momagebela: ? E da noga: le dawa: ma: ne, ea wadela: i hou amo ema bu olelema.
3 ndipo unene kuti, ‘Ambuye akuti: Iwe mzinda umene wadzigwetsa wekha mʼtsoka pa kukhetsa magazi pakati pako ndi kudziyipitsa popanga mafano,
Yelusaleme fi ilima, Na, Ouligisudafa Hina Gode, Na sia: ilima olelema, amane, ‘Dilia da dilila: fi dunu bagohame medole lelegei dagoiba: le, amola ogogosu ‘gode’ ilima dilia hou ledo hamoma: ne, nodone sia: ne gadoiba: le, dilia wadela: mu eso da mana.
4 wapezekatu wolakwa chifukwa cha magazi amene wakhetsa, ndipo wadziyipitsa chifukwa cha mafano amene wapanga. Choncho wachepetsa masiku ako, ndipo zaka zako zafika kumapeto. Nʼchifukwa chake ndalola kuti anthu a mitundu ina akunyoze ndiponso kuti anthu a mayiko onse akuseke.
Dilia da amo medole legesu hou hamobeba: le, amola ogogosu ‘gode’ loboga hamoiba: le dilila: hou ledo hamoiba: le, dilima wadela: mu eso da gadenene doaga: i dagoi. Amaiba: le, Na da eno fifi asi gala dilima lalasogole oufesega: ma: ne, logo doasi dagoi.
5 Mayiko amene ali pafupi ndi mayiko omwe ali kutali adzakunyoza, iwe mzinda wa mbiri yoyipa, wodzaza ndi chiwawa.
Dilima gadenene fifi asi gala, amola badilia fifi asi gala da dilia sema hame nabasu hou ba: beba: le, dilima ba: sola: le oufesega: sa.
6 “‘Taona momwe aliyense wa atsogoleri a Israeli amagwiritsira mphamvu zake kupha anthu.
Isala: ili ouligisu dunu huluane da ilila: gasa da defele dawa: beba: le, medole legesu hou hamonanebe.
7 Mu mzindamo anthu amanyoza abambo ndi amayi awo. Iwo amapondereza alendo ndi kuzunza ana amasiye ndi akazi amasiye.
Yelusaleme amo ganodini, mano huluane da ilia edalalima hame nodosa. Dilia da ga fi ilima ogogosa. Amola, dilia da didalo amola guluba: mano ilima da: da: losa.
8 Wanyoza zinthu zanga zopatulika ndi kuyipitsa Masabata anga.
Dilia da hadigidafa sogebi amoma hame nodosa, amola Sa: bade sema hame hamosa.
9 Mwa iwe muli anthu onenera anzawo zabodza kuti aphedwe. Mwa iwe mulinso amene amadyera zansembe pa mapiri a chipembedzo. Enanso amachita zonyansa.
Dilia mogili da eno dunu, ilia bogoma: ne se bidi lama: ne, ilia hou ogogole sia: sa. Dilia mogili da ohe amo ogogosu ‘gode’ ilima gobele sali, amo ea hu naha. Mogili da ilia wadela: i hanai gumimusa: dawa: lala.
10 Mwa iwe muli ena ogonana ndi akazi a abambo awo, muli enanso amene amavuta akazi pamene ali woyipitsidwa ndi msambo.
Mogili ilia da ilia eda ea uda amo gilisili golasa. Mogili da uda da sioi fisia, ilima gasa fili lelele logesa.
11 Ena amachita chigololo ndi akazi a anzawo, ndipo ena, mopanda manyazi, amayipitsa mkazi wa mwana wawo. Palinso ena amene amayipitsa alongo awo, ana aakazi a abambo awo.
Mogili da inia uda adole laha. Mogili da ilila: nawi amola gawia adole lasa.
12 Mwa iwe muli anthu amene amalandira ziphuphu kuti aphe anzawo; ena amachita katapira ndi kupeza phindu loposera muyeso; enanso amapeza phindu mwachinyengo poopseza anzawo. Ndipo mwandiyiwala Ine, akutero Ambuye Yehova.
Mogili da bidi lamusa: , dunu medole legesa. Mogili da fa: no dabema: ne muni bu lama: ne, eno dunuma iasea, ilia amo muni bagade baligiwane bu laha. Amola ilia eno dunuma da: da: lobeba: le, muni bagade gagusa. Ilia da Na gogolei dagoi.” Ouligisu Hina Gode da sia: i dagoi.
13 “‘Koma Ine ndachita kuwomba mʼmanja kuti phuu nʼkudabwa chifukwa cha phindu lachinyengo limene mwapeza ndiponso chifukwa cha kuphana kumene kumachitika pakati panu.
“Na da Na loboga dilia wamolasu dunu amola medole legesu dunu banenesimu.
14 Kodi mtima wako udzakhala wolimbabe kapena manja ako adzakhalabe amphamvu ndikadzatsiriza kukulanga iwe? Ine Yehova ndayankhula, ndipo ndidzazichitadi.
Na da dilima se ia dagosea, dilia da gasa hamedei ba: mu. Dilia da gasa hameba: le, dilia lobo gaguia gadomu hamedei ba: mu. Na, Hina Gode, da sia: i dagoi. Amola, Na da ogogosu hame dawa:
15 Ndidzakubalalitsani pakati pa anthu a mitundu ina ndi kukumwazirani ku mayiko onse. Umu ndi mmene ndidzachotsere zoyipa zako.
Na da dilia wadela: i hamobe dagolesima: ne, Na da dili fifi asi gala fi huluane amo ganodini esaloma: ne, dili afagogolesimu.
16 Udzanyozedwa pamaso pa anthu a mitundu ina. Pambuyo pake udzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’”
Amola eno fifi asi gala da dilima mae nodone, banenesimu. Be dilia da Na da Hina Gode amo dafawaneyale dawa: mu.”
17 Yehova anandiyankhula nati:
Hina Gode da nama amane sia: i,
18 “Iwe mwana wa munthu, Aisraeli asanduka chinthu cha chabechabe kwa Ine. Onse ali ngati mkuwa, chitini, chitsulo ndi mtovu zotsala mʼngʼanjo atayeretsa siliva.
“Dunu egefe! Isala: ili dunu da Nama hamedei liligi agoai. Ilia da fedege agoane, silifa da gobesu lalu amo ganodini adoba: ma: ne gobesea, isui ouli amo dialebe agoai ba: sa.
19 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: ‘Pakuti nonse mwasanduka chinthu cha chabechabe, Ine ndidzakusonkhanitsani mu Yerusalemu.
Amaiba: le, Na, Ouligisudafa Hina Gode, da wali ilia da amo isui ouli defele, hamedei liligi, ilima adosa. Na da ili huluane gilisili, Yelusalemega oule misunu.
20 Monga momwe anthu amasonkhanitsira siliva, mkuwa, chitsulo, mtovu ndi chitini mʼngʼanjo ndi kusonkhetsa moto kuti azisungunule, motero Inenso ndidzakusonkhanitsani ndili wokwiya ndi waukali, ndipo ndidzakuyikani mʼkati mwa mzinda, ndikukusungunurani.
Dunu da igi (amo ganodini da silifa, gula, balase, lede amola dini gala) amo gilisili, gobesu laluga gaguli maha, amo defele Na da Isala: ili dunu oule misunu. Amola, lalu da amo liligi daeabe defele, Na ougi bagadedafa da ili daeamu.
21 Ndidzakusonkhanitsani mu mzindamo ndi kukoleza moto wa mkwiyo wanga, ndipo inu mudzasungunuka mu mzindamo.
Dafawane! Na da ili gagadole, Yelusaleme amoma oule misini, ili hagudu lalu didili, Na ougiga ili daeamu.
22 Monga siliva amasungunulidwa mʼngʼanjo, kotero inunso mudzasungunuka mʼkati mwa mzinda ndipo Inu mudzadziwa kuti Ine Yehova ndakukwiyirani.’”
Dunu ilia da silifa amo lalu gobesu amo ganodini silifa daeabe, amo defele Na da ili Yelusaleme ganodini daeamu. Amasea, ilia da Hina Gode Ea ougi nabaha, amo noga: le dawa: mu.”
23 Yehova anandiyankhulanso nati,
Hina Gode da nama bu amane sia: i,
24 “Iwe mwana wa munthu, uza dziko la Israeli kuti, ‘Iwe ndiwe dziko losayeretsedwa, ndiponso losavumbidwa ndi mvula chifukwa cha mkwiyo wanga.’
“Dunu egefe! Isala: ili dunu amo ilia soge da ledo bagade, hadigi hame, amo ilima sia: ma. Amaiba: le, Na da ougili, ilima se imunu.
25 Atsogoleri ake mu mzindamo ali ngati mkango wobangula pogwira nyama. Apha anthu, alanda chuma ndi zinthu za mtengowapatali, ndiponso asandutsa amayi ambiri kukhala amasiye.
Ilia ouligisu dunu da laione wa: me amo da ohe ilia fai amo enoga lasa: besa: le, gesenebe agoai gala. Ilia dunu eno medole legesa, ilia soge amola muni amo ilia hanai defele laha. Amalu, didalo bagohame esalebe ba: sa.
26 Ansembe ake amaphwanya lamulo langa ndi kuyipitsa zinthu zanga zopatulika. Sasiyanitsa pakati pa zinthu zopatulika ndi zinthu wamba. Saphunzitsa anthu kusiyana kwa zinthu zoyenera pa chipembedzo ndi zinthu zosayenera. Sasamalira za kusunga masabata anga. Motero Ine ndimanyozedwa pakati pawo.
Gobele salasu ouligisu dunu da Na sema fili, hadigi liligi amoma hame dawa: digisa. Ilia da hadigi liligi amola ledo liligi, amo afafamusa: hame dawa: Ilia da foloai amola ledo da hisu hame olelesa. Amola ilia da Sa: bade eso sema amoma higasa. Amaiba: le, Isala: ili dunu da Nama hame nodosa.
27 Atsogoleri ake ali ngati mimbulu yokhadzula nyama; amakhetsa magazi ndi kupha anthu kuti apeze phindu loyipa.
Eagene ouligisu dunu da wufi gasonasu wa: me da ilia medole legei ohe liligi dodosa: sa, amo defele hamosa. Ilia muni bagade lamusa: , medole legesu hou hamosa.
28 Aneneri ake amabisa zonsezi monga muja amachitira anthu popaka njereza. Amazimphimba ndi zabodza zimene aona mʼmasomphenya awo ndi zonama za mʼmawula awo. Iwo amati, ‘Ambuye Yehova akuti,’ pamene Ine Yehova sindinayankhule.
Ogogosu balofede dunu da dunu ilia gagoi damana ahea: iai ulasuga ulasu defele, amo wadela: i hou dedebosu. Ilia da ogogosu esala ba: su olelesa, amola ogogosu ba: la: lusu hamosa. Ilia da Ouligisu Hina Gode Ea sia: olelelala, ilisu sia: sa. Be Na, Hina Gode, da ilima hamedafa sia: i.
29 Anthu a mʼdzikomo amasautsa anzawo ndi kulanda anthu osowa. Amazunza anthu osauka ndi amphawi. Amavutitsa alendo posawachitira zinthu mwachilungamo.
Bagade gagui dunu da ogogosu amola gegene lasu hou hamosa. Ilia da hame gagui dunu amola ga fi dunu ilima da: da: losa.
30 “Ndinafunafuna munthu pakati pawo woti amange linga, woti ayimirire dziko pamaso panga kundipepesa kuti ndisaliwononge, koma sindinamupeze.
Na da gaga: su dunu, amo da gagoi gadelale sa: i sogebi amo gaga: le, Na soge Na ougiga wadela: mu gadenesa amo gaga: musa: aligima: ne, agoai dunu hogoi helele hame ba: i.
31 Nʼchifukwa chake ndawakwiyira kwambiri. Ndawawonongeratu ndi mkwiyo wanga woyaka ngati moto. Ndawalanga molingana ndi zimene anachita. Akutero Ambuye Yehova.”
Amaiba: le, Na da Na ougi bu hame bugimu. Na ougi da ilima lalu agoane doagala: mu. Na da ilima se imunu. Ilia wadela: le hamoiba: le, Na da ili wadela: lesimu.” Ouligisudafa Hina Gode da sia: i dagoi.

< Ezekieli 22 >