< Ezekieli 2 >

1 Iye anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, imirira kuti ndiyankhule nawe.”
Telle fut la vision de l’image de la gloire du Seigneur; et je vis; et je tombai sur ma face, et j’entendis la voix de quelqu’un parlant. Et il me dit: Fils d’un homme, tiens-toi sur tes pieds, et je te parlerai.
2 Pamene ankayankhula nane, Mzimu wa Mulungu unalowa mwa ine ndipo unandiyimiritsa, ndipo ndinamva Iye akundiyankhula.
Et il entra en moi un esprit, après que le Seigneur m’eut parlé, et il m’établit sur mes pieds; et j’entendis quelqu’un me parlant,
3 Iye anati, “Iwe mwana wa munthu, Ine ndikukutuma kwa Aisraeli, mtundu wa anthu owukira umene wandiwukira Ine; Iwo ndi makolo awo akhala akundiwukira Ine mpaka lero lino.
Et disant: Fils d’un homme, moi je t’envoie vers les fils d’Israël, vers ces nations apostates qui se sont retirées de moi; eux et leurs pères ont violé mon alliance jusqu’à ce jour.
4 Ndikukutuma kwa anthu okanika ndiponso nkhutukumve. Ndikukutuma kuti akawawuze zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena.
Et ce sont des enfants à la face dure, au cœur indomptable, ceux auxquels moi je t’envoie; et tu leur diras: Voici ce que dit le Seigneur Dieu:
5 Kaya akamva kaya sakamvera, pakuti iwo ndi anthu opanduka, komabe adzadziwa kuti mneneri ali pakati pawo.
Pour voir si par hasard ils écouteront, et si par hasard ils y manqueront; parce que c’est une maison qui m’exaspère; et ils sauront qu’un prophète a été au milieu d’eux.
6 Tsono iwe mwana wa munthu, usachite nawo mantha kapena kuopa zimene azikanena. Usachite mantha, ngakhale minga ndi mkandankhuku zikuzinge ndipo ukukhala pakati pa zinkhanira. Usachite mantha ndi zimene akunena kapena kuopsedwa ndi nkhope zawo, popeza anthuwa ndi awupandu.
Toi donc, fils d’un homme, ne les crains point, n’appréhende pas leurs discours, parce que des incrédules et des destructeurs sont avec toi, et que tu habites avec des scorpions; ne crains pas leurs paroles, n’aie pas peur de leurs visages; parce que c’est une maison qui m’exaspère.
7 Ukawawuze ndithu mawu anga, kaya akamva kaya sakamva. Paja anthuwa ndi awupandu.
Tu leur diras donc mes paroles, pour voir si par hasard ils écouteront, et s’ils y manqueront, parce qu’ils m’irritent sans cesse.
8 Koma iwe mwana wa munthu, mvetsera zimene ndikukuwuza. Usakhale wowukira ngati iwowo. Tsono yasama pakamwa pako kuti udye chimene ndikukupatsa.”
Mais toi, fils d’un homme, écoute tout ce que je te dis; ne m’exaspère pas comme cette nation m’exaspère sans cesse; ouvre la bouche et mange tout ce que moi je te donne.
9 Nditayangʼana ndinangoona dzanja litaloza ine, litagwira mpukutu wolembedwa.
Et je vis, et voilà que fut envoyée vers moi une main dans laquelle était un livre roulé; et elle déploya devant moi ce livre qui était écrit au dedans et au dehors; et là étaient écrites des lamentations, un chant et malheur.
10 Anawufunyulura pamaso panga. Mpukutu wonse unali wolembedwa kuseri nʼkuseri. Ndipo mawu amene analembedwa mʼmenemo anali a madandawulo, maliro ndi matemberero.

< Ezekieli 2 >