< Ezekieli 19 >

1 “Imba nyimbo ya madandawulo, kuyimbira akalonga a ku Israeli.
Wena-ke, phakamisa isililo ngezikhulu zakoIsrayeli,
2 Uzinena kuti, “‘Amayi ako anali ndani? Anali ngati mkango waukazi! Iwo unabwatama pakati pa mikango yayimuna; unkalera ana ake pakati pa misona.
uthi: Uyini unyoko? Isilwanekazi; salala phakathi kwezilwane, sakhulisa imidlwane yaso phakathi kwezilwane ezintsha.
3 Unalera mmodzi mwa ana ake, ndipo mwanayo anasanduka mkango wamphamvu. Unaphunzira kugwira nyama, ndipo unayamba kudya anthu.
Sakhulisa omunye wemidlwane yaso, waba libhongo, wafunda ukudabula impango, wadla abantu.
4 Anthu amitundu anamva za mkangowo, ndipo tsiku lina unagwa mʼmbuna mwawo. Iwo anawukoka ndi ngowe kupita nawo ku dziko la Igupto.
Izizwe zasezisizwa ngawo, wabanjwa emgodini wazo, zawusa elizweni leGibhithe ngamaketane.
5 “‘Amayi aja ataona kuti mwana ankamukhulupirira uja wagwidwa ndi kuti chiyembekezo chake chapita padera, amayiwo anatenganso mwana wina namusandutsa mkango wamphamvu.
Kwathi sibona ukuthi sesilindile, lokuthi ithemba laso selibhubhile, sathatha omunye wemidlwane yaso, sawenza waba libhongo.
6 Unkayendayenda pakati pa mikango inzake, pakuti tsopano unali mkango wamphamvu. Unaphunzira kugwira nyama ndipo unayamba kudya anthu.
Wahamba waya le lale phakathi kwezilwane, waba libhongo, wafunda ukudabula impango, wadla abantu.
7 Unagwetsa malinga awo, ndikuwononga mizinda yawo. Onse a mʼdzikomo anachita mantha chifukwa cha kubangula kwake.
Wazazi inqaba zabo, wachitha imizi yabo; ilizwe laselisiba yinkangala, lokugcwala kwalo, ngomsindo wokubhonga kwawo.
8 Pamenepo mitundu ya anthu, makamaka ochokera madera ozungulira, inabwera kudzalimbana nawo. Anawutchera ukonde wawo, ndipo tsiku lina unagwera mʼmbuna mwawo.
Izizwe zasezisima zimelene lawo inhlangothi zonke zivela ezabelweni, zendlala imbule lazo phezu kwawo; wabanjwa emgodini wazo.
9 Anawukoka ndi ngowe nawuponya mʼchitatanga. Anabwera nawo kwa mfumu ya ku Babuloni ndipo mfumuyo inawuponya mʼndende ndi cholinga choti liwu lake lisamamvekenso ku mapiri a Israeli.
Zawufaka ekhejini ngamaketane, zawusa enkosini yeBhabhiloni, zawuletha ezinqabeni, ukuze ilizwi lawo lingabe lisezwakala phezu kwezintaba zakoIsrayeli.
10 “‘Amayi ako anali ngati mpesa mʼmunda wamphesa wodzalidwa mʼmbali mwa madzi. Unabereka bwino ndipo unali ndi nthambi zambiri chifukwa cha kuchuluka kwa madzi.
Unyoko unjengevini egazini lakho, elihlanyelwe ngasemanzini; laba lezithelo ligcwele izingatsha ngenxa yamanzi amanengi.
11 Nthambi zake zinali zolimba, zoyenera kupangira ndodo yaufumu. Unatalika nusomphoka pakati pa zomera zina. Unkaoneka bwino chifukwa cha kutalika kwake, ndi nthambi zake zambiri.
Lalilezinti eziqinileyo ezaba zintonga zababusayo, njalo ubude balo babuphakeme phakathi kwengatsha eziqatha, libonakala ngobude balo ngokwanda kwengatsha zalo.
12 Koma unazulidwa mwaukali ndipo unagwetsedwa pansi. Unawuma ndi mphepo ya kummawa, zipatso zake zinayoyoka; nthambi zake zolimba zinafota ndipo moto unapsereza mtengo wonse.
Kodwa lasitshunwa ngokuthukuthela, laphoselwa emhlabathini, lomoya wempumalanga womisa isithelo salo; izinti zalo eziqinileyo zephuka zoma; umlilo waziqeda.
13 Ndipo tsopano anawuwokeranso ku chipululu, dziko lowuma ndi lopanda madzi.
Khathesi selihlanyelwe enkangala, emhlabathini otshileyo lowomileyo.
14 Moto unatulukanso mu mtengomo ndi kupsereza nthambi ndi zipatso zake. Palibe nthambi yolimba inatsala pa mtengowo yoyenera kupangira ndodo yaufumu. Imeneyi ndi nyimbo yachisoni ndipo yasanduka nyimbo ya pa maliro.’”
Umlilo usuphume oluthini lwezingatsha zalo, waqeda isithelo salo, ukuze lingabi loluthi oluqinileyo lube yintonga yokubusa. Lesi yisililo, njalo sizakuba yisililo.

< Ezekieli 19 >