< Ezekieli 15 >
1 Yehova anayankhulanso nane kuti,
In k meni je prišla Gospodova beseda, rekoč:
2 “Iwe mwana wa munthu, kodi mtengo wamphesa umapambana bwanji mtengo wina uliwonse? Nthambi zake zimapambana bwanji nthambi ina iliyonse.
»Človeški sin: ›Kaj je trta boljša kakor katerokoli drevo ali kakor mladika, ki je med gozdnimi drevesi?
3 Mtengo umene uja nʼkupangira chiyani? Kodi anthu angathe kupangira chikhomo chokolekapo zinthu zawo?
Mar bo vzet njen les, da bi opravljal katerokoli delo? Ali bodo možje od nje vzeli klin, da bi nanj obesili katerokoli posodo?
4 Taonani, ndi nkhuni chabe zosonkhera moto. Ukaponyedwa pa moto monga nkhuni ndi kuyaka mbali zonse ndi kusanduka makala, kodi ungagwiritsidwe ntchito ina iliyonse?
Glej, vržena je v ogenj za gorivo. Ogenj pogoltne oba njena konca in njena sreda je ožgana. Ali je primerna za kakršnokoli delo?
5 Ngati pamene unali wosapsa sukanatheka kuwugwiritsa ntchito, nanga bwanji utapserera ndi moto, adzawugwiritsa ntchito bwanji?
Glej, ko je bila cela, ni bila primerna za nobeno delo. Kako veliko manj bo vendar ta primerna za kakršnokoli delo, ko jo je požrl ogenj in je ožgana?‹
6 “Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, ‘Mtengo wamphesa ndidzawuponya mʼmoto monga ndimachitira ndi mitengo ina ya ku nkhalango. Momwemonso ndidzachita ndi anthu a ku Yerusalemu.
Zato tako govori Gospod Bog: ›Kakor je trta med gozdnimi drevesi, ki sem jo izročil ognju za gorivo, tako bom izročil prebivalce Jeruzalema.
7 Ndidzawalanga pamenepo ngakhale iwo atuluka pa moto, motowo udzawatenthabe. Ndipo pamene ndidzatsutsana nawo, mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Svoj obraz bom naravnal zoper njih. Šli bodo iz enega ognja, pa jih bo pogoltnil drug ogenj. In spoznali boste, da jaz sem Gospod, ko svoj obraz naravnam zoper njih.
8 Ine ndidzasandutsa dziko kukhala chipululu chifukwa anthu akhala osakhulupirika, akutero Ambuye Yehova.’”
Deželo bom naredil zapuščeno, ker so zagrešili prekršek, ‹ govori Gospod Bog.«