< Ezekieli 15 >

1 Yehova anayankhulanso nane kuti,
Кувынтул Домнулуй мь-а ворбит астфел:
2 “Iwe mwana wa munthu, kodi mtengo wamphesa umapambana bwanji mtengo wina uliwonse? Nthambi zake zimapambana bwanji nthambi ina iliyonse.
„Фиул омулуй, че аре лемнул де вицэ май мулт декыт орьче алт лемн, вицеле-де-вие май мулт декыт челе че сунт принтре копачий дин пэдуре?
3 Mtengo umene uja nʼkupangira chiyani? Kodi anthu angathe kupangira chikhomo chokolekapo zinthu zawo?
Я оаре чинева дин лемнул ачеста ка сэ факэ врео лукраре? Фаче чинева дин ел вреун кырлиг де атырнат чева ын ел?
4 Taonani, ndi nkhuni chabe zosonkhera moto. Ukaponyedwa pa moto monga nkhuni ndi kuyaka mbali zonse ndi kusanduka makala, kodi ungagwiritsidwe ntchito ina iliyonse?
Ятэ кэ есте пус пе фок сэ ардэ. Дупэ че ый арде фокул челе доуэ капете ши мижлокул, май поате фи ел бун де чева?
5 Ngati pamene unali wosapsa sukanatheka kuwugwiritsa ntchito, nanga bwanji utapserera ndi moto, adzawugwiritsa ntchito bwanji?
Ятэ, кынд ера ынтрег, ну се путя фаче нимик дин ел. Ку кыт май пуцин акум, дупэ че л-а мистуит ши л-а арс фокул, с-ар май путя фаче врео лукраре дин ел?
6 “Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, ‘Mtengo wamphesa ndidzawuponya mʼmoto monga ndimachitira ndi mitengo ina ya ku nkhalango. Momwemonso ndidzachita ndi anthu a ku Yerusalemu.
Де ачея, аша ворбеште Домнул Думнезеу: ‘Ка лемнул де вицэ динтре копачий дин пэдуре, пе каре-л пун пе фок сэ-л ард, аша вой да ши пе локуиторий Иерусалимулуй.
7 Ndidzawalanga pamenepo ngakhale iwo atuluka pa moto, motowo udzawatenthabe. Ndipo pamene ndidzatsutsana nawo, mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Ымь вой ынтоарче Фаца ымпотрива лор; ау ешит дин фок, дар фокул ый ва арде де тот. Ши вець шти кэ Еу сунт Домнул кынд Ымь вой ынтоарче Фаца ымпотрива лор.
8 Ine ndidzasandutsa dziko kukhala chipululu chifukwa anthu akhala osakhulupirika, akutero Ambuye Yehova.’”
Вой префаче цара ынтр-ун пустиу, пентру кэ ау фост некрединчошь’”, зиче Домнул Думнезеу.

< Ezekieli 15 >