< Ezekieli 15 >
1 Yehova anayankhulanso nane kuti,
A palavra de Yahweh veio até mim, dizendo:
2 “Iwe mwana wa munthu, kodi mtengo wamphesa umapambana bwanji mtengo wina uliwonse? Nthambi zake zimapambana bwanji nthambi ina iliyonse.
“Filho do homem, o que é a árvore da videira mais do que qualquer árvore, o ramo de videira que está entre as árvores da floresta?
3 Mtengo umene uja nʼkupangira chiyani? Kodi anthu angathe kupangira chikhomo chokolekapo zinthu zawo?
Será que a madeira será tirada dela para fazer qualquer coisa? Os homens pegarão um alfinete dela para pendurar algum vaso nela?
4 Taonani, ndi nkhuni chabe zosonkhera moto. Ukaponyedwa pa moto monga nkhuni ndi kuyaka mbali zonse ndi kusanduka makala, kodi ungagwiritsidwe ntchito ina iliyonse?
Eis que ela é lançada no fogo como combustível; o fogo devorou ambas as extremidades, e o meio dela é queimado. É rentável para qualquer trabalho?
5 Ngati pamene unali wosapsa sukanatheka kuwugwiritsa ntchito, nanga bwanji utapserera ndi moto, adzawugwiritsa ntchito bwanji?
Eis que, quando estava inteiro, era adequado para nenhum trabalho. Quanto menos, quando o fogo o devorou, e foi queimado, será ainda adequado para qualquer trabalho?”.
6 “Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti, ‘Mtengo wamphesa ndidzawuponya mʼmoto monga ndimachitira ndi mitengo ina ya ku nkhalango. Momwemonso ndidzachita ndi anthu a ku Yerusalemu.
Portanto, o Senhor Javé diz: “Como a madeira de videira entre as árvores da floresta, que eu dei ao fogo para combustível, assim eu darei aos habitantes de Jerusalém.
7 Ndidzawalanga pamenepo ngakhale iwo atuluka pa moto, motowo udzawatenthabe. Ndipo pamene ndidzatsutsana nawo, mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Eu colocarei meu rosto contra eles”. Eles sairão do fogo, mas o fogo ainda os devorará. Então vocês saberão que eu sou Yahweh, quando eu colocar meu rosto contra eles.
8 Ine ndidzasandutsa dziko kukhala chipululu chifukwa anthu akhala osakhulupirika, akutero Ambuye Yehova.’”
Eu tornarei a terra desolada, porque eles agiram infielmente”, diz o Senhor Javé.