< Ezekieli 13 >
1 Yehova anayankhulanso nane kuti,
LEUM GOD El kaskas nu sik
2 “Iwe mwana wa munthu unenere modzudzula aneneri a Israeli amene akunenera za kukhosi kwawo. Uwawuze iwowa kuti, ‘Imvani mawu a Yehova!’
ac fahk, “Kom, mwet sukawil moul la, fahk kas in lain mwet palu lun Israel su sifacna kinauk kas in palu lalos. Fahkang nu selos elos in lohng na kas lun LEUM GOD.”
3 Ambuye Yehova akuti, ‘Tsoka kwa aneneri opusa amene amangonenera zopeka ngakhale kuti sanaone kanthu konse!’
Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk: “We nu sin mwet palu lalfon ingan! Elos sifacna orala nunak in akkeyalos, ac kinauk aruruma lalos.
4 Iwe Israeli, aneneri ako ali ngati nkhandwe pa mabwinja.
Mwet Israel, mwet palu lowos uh wangin sripalos. Elos oana kosro lemnak ma muta ke acn musalla in siti uh.
5 Simunakwere khoma kuti mukakonze mʼmene munagumuka, kuti Aisraeli adziteteze kolimba pa nkhondo pa tsiku la Yehova.
Elos tiana taran acn ma mokukla ke kalkal uh, ku aksasuyela pot we. Ouinge ac fah wangin ma loangeyen Israel in pacl in mweun ke len lun LEUM GOD.
6 Masomphenya awo ndi achabe ndipo kuwombeza kwawo ndi kwabodza. Iwo amati, ‘Yehova akutero,’ pomwe Yehova sanawatume. Komabe iwo amayembekezera kuti zimene ayankhulazo zichitikadi.
Aruruma lalos uh tia pwaye, ac kas in palu lalos uh kikiap. Elos fahk mu elos fahkak kas luk, a nga tia supwalos. Elos nunku mu kas lalos inge ac akpwayeyuk.
7 Koma Ine ndikuti masomphenya anu ngachabechabe ndi zimene mwawombedzazo nʼzabodza. Mumanena kuti, ‘Akutero Yehova,’ pamene sindinayankhule nʼkomwe.
Nga fahk nu selos: Aruruma ma kowos liye uh tia pwaye, ac kas in palu lowos uh kikiap. Kowos fahk mu ma luk pa kas ingan, tuh nga soenna kaskas nu suwos!”
8 “Tsono Ine Ambuye Wamphamvuzonse ndikukutsutsani chifukwa cha zoyankhula zanu zonama ndi masomphenya anu abodzawo. Ndikutero Ine Yehova.
Ouinge LEUM GOD Fulatlana El fahk nu selos, “Mweyen kas lowos uh tia pwaye, ac aruruma lowos uh kikiap, nga lain kowos.
9 Ndidzalanga aneneri amene amanenera zabodza za zinthu zimene amati anaziona mʼmasomphenya. Sadzakhala nawo mʼbwalo la anthu anga ndipo mayina awo sadzalembedwa mu kawundula wa nzika za Israeli. Sadzalowa nawo mʼdziko la Israeli. Pamenepo mudzadziwa kuti Ine ndine Ambuye Yehova.
Nga akola in kalyei kowos, mwet palu su liye aruruma kikiap ac fahkak kas in palu tia pwaye. Ke mwet luk uh ac tukeni in orek pwapu, kowos ac fah tia wi. Ac fah tia simla inewos inmasrlon mwet Israel. Kowos ac fah tiana folokla nu in facl Israel. Na kowos ac fah etu lah nga pa LEUM GOD Fulatlana.
10 “Popeza kuti aneneri asocheretsa anthu anga pomanena kuti, ‘Kuli mtendere’ pamene mtendere palibe; ndiponso anthu akamanga khoma iwo nʼkumalipaka njereza,
Mwet palu elos kiapu mwet luk ke elos fahk mu ma nukewa wona, sruk tiana wo! Mwet luk uh etoak pot na munas, na mwet palu tuku fasrela.
11 choncho ufotokozere amene alipaka njerezawo kuti khomalo lidzagwa. Mvula idzagwa mwamphamvu, kudzagwa matalala akuluakulu, ndipo kudzawomba mphepo yamkuntho.
Fahkang nu sin mwet palu an lah pot lalos uh ac mokukla. Nga ac supwala af matol, ac tultul in af ma oana eot ac putat nu fac, ac eng upa ac fah fungulya.
12 Pamene khomalo lagwa, kodi anthu sadzakufunsani kuti, ‘Kodi njereza yemwe munapaka uja ali kuti?’
Ouinge pot sac ac raki, na mwet nukewa ac fah siyuk, ‘Mwe mea in fasriyukla?’”
13 “Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti: Mwa ukali ndidzakunthitsa mphepo ya mkuntho. Ndidzagwetsa matalala akuluakulu ndili ndi ukali ndipo ndidzavumbwitsa mvula yamphamvu ndi mkwiyo mpaka khomalo litawonongeka kotheratu.
Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk: “Ke sripen kasrkusrak luk, nga ac supwala eng upa ac af matol ac tultul in af upa in tuh kunausla pot sac.
14 Ndidzagwetsa khoma limene munalipaka njerezalo. Ndidzaligumuliratu mpaka pansi kotero kuti maziko ake adzaoneka. Khomalo likadzagwa, inu mudzawonongekamo; ndipo mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Nga akola ngan kunausya pot sac ma elos fasrela, ac rakinya tuh pwelung uh fah mwesisla. Pot sac ac fah raki ac unikowosi nukewa. Na mwet nukewa fah etu lah nga pa LEUM GOD.”
15 Kotero ndidzagwiritsa ntchito mkwiyo wanga pa khomali ndi pa amene analipaka njereza. Pambuyo pake ndidzakuwuzani kuti, ‘Khoma lagwa pamodzi ndi amene analipaka njereza.
“Pot sac, ac elos su fasrela ah, fah pulakin fulen kasrkusrak luk. Na nga fah fahk nu suwos lah pot sac wanginla, oayapa elos su fasrela —
16 Agwanso aneneri a Yerusalemu amene ankalosa za Yerusalemu nʼkumati anaona mʼmasomphenya za mtendere wa Yerusalemu pamene mtendere kunalibe konse, akutero Ambuye Wamphamvuzonse.’
aok, mwet palu ma tuh fahk mu ma nukewa in Jerusalem wona, ke tiana wo.” LEUM GOD Fulatlana pa fahk ma inge.
17 “Tsono iwe mwana wa munthu, yankhulapo pa nkhani za akazi amene ali pakati pa anthu ako. Iwo amanenera zopeka za mʼmutu mwawo. Tsono adzudzule.
LEUM GOD El fahk, “Mwet sukawil, inge ngetla liye mutan inmasrlon mwet lom su kinauk kas in palu lalos. Lainulos
18 Uwawuze kuti, ‘Ambuye Yehova akuti: Tsoka kwa akazi amene amasoka zithumwa zapamkono, amenenso amasoka nsalu za kumutu za anthu. Kodi mufuna kukola mitima ya anthu anga, inuyo nʼkupulumutsa moyo wanu?
ac fahkang nu selos ma LEUM GOD Fulatlana El fahk inge: “We nu suwos mutan, su twani mwe lohlpo inutnut lun mwet nukewa, ac oayapa susu nuknuk inutnut tuh in oasr ku lalos fin moul lun mwet ngia. Kowos lungse in oasr ku lowos in nununku moul ac misa fin mwet luk uh, ac kowos orekmakin ku se inge tuh in wo nu suwos sifacna.
19 Ponamiza anthu anga amene amamva za mabodza anu, inu mwapha anthu amene sanayenera kufa ndipo mwasiya ndi moyo amene sanayenera kukhala ndi moyo.
Kowos pilesreyu ye mutun mwet luk tuh kowos in eis kutu srisrik barley ac ipin bread na ekasr. Kowos uniya mwet su tia fal in misa, ac sruokya moul lun mwet su tia fal in moul. Ke kowos oru ouinge kowos kiapwela mwet luk, ac elos lulalfongi kowos.”
20 “‘Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti: Ine ndikudana ndi zithumwa zanu zimene mumakokera nazo mitima ya anthu ngati mbalame. Ndidzazingʼamba kudzichotsa pa mikono yanu. Choncho ndidzapulumutsa miyoyo ya anthu amene munawakola ngati mbalame.
Pa inge ma LEUM GOD Fulatlana El fahk: “Nga srunga mwe lohlpo ma kowos orala in nununku moul ac misa lun mwet. Nga ac sacla liki pouwos, ac aksukosokyela mwet su tuh muta ye ku lowos.
21 Ndidzangʼamba nsalu zanu za matsengazo ndi kupulumutsa anthu anga mʼmanja mwanu, ndipo simudzakhalanso ndi mphamvu yowakolera. Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.
Nga ac tulakunla susu nuknuk liki sifowos, ac aksukosokyela mwet luk uh liki ku lowos nwe tok. Na kowos fah etu lah nga pa LEUM GOD.
22 Popeza kuti munatayitsa mtima anthu olungama ngakhale sindinafune kuti ataye mtima; ndipo munalimbitsa anthu oyipa kuti asaleka machimo awo motero sakutha kupulumutsa moyo wawo,
“Kas kikiap lowos uh akmunasyela mwet wo, su nga tia lungse in sun mwe keok. Kowos pirik na mwet koluk uh in tia tui ke orekma koluk, pwanang elos tia konauk inkanek in moul.
23 choncho inu simudzaonanso masomphenya abodza kapena kuwombeza. Ine ndidzapulumutsa anthu anga mʼmanja mwanu. Ndipo pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’”
Inge, aruruma kikiap ac kas in palu sutuu lowos uh safla. Nga ac molela mwet luk liki ye ku lowos, na kowos fah etu lah nga pa LEUM GOD.”